01a-basic lt participant manual v2.0 - chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. tiseka...

48
STRATEGIC IMPACT MTSOKHANO WA ATSOGOLERI © V2.0 (2014) CHICHEWA “TENGANI MBALI PA NCHITO YAIKURUSTRATEGIC IMPACT P.O. BOX 830337 RICHARDSON, TX 75083 WWW.TOUCHINGEVERYNATION.COM © Zowonera, Strategic Impact. Pasakhale kusintha kulikonse kwa bukhuli, koma mukhoza kukopera mwaulere ndi kugawa osasintha kanthu. © Copyright, Strategic Impact. No changes may be made to this manual, but you may freely copy and distribute without making changes to content. 1

Upload: vocong

Post on 26-Mar-2018

272 views

Category:

Documents


9 download

TRANSCRIPT

Page 1: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

� """"

STRATEGIC IMPACT!MTSOKHANO WA ATSOGOLERI ©!

V2.0 (2014) CHICHEWA!"

"“TENGANI MBALI PA NCHITO YAIKURU”!

"STRATEGIC IMPACT!P.O. BOX 830337!

RICHARDSON, TX 75083!WWW.TOUCHINGEVERYNATION.COM!

© Zowonera, Strategic Impact.  Pasakhale kusintha kulikonse kwa bukhuli, "koma mukhoza kukopera mwaulere ndi kugawa osasintha kanthu.""

© Copyright, Strategic Impact.  No changes may be made to this manual, but you"may freely copy and distribute without making changes to content.""

�1

Page 2: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

"

"

"

"

"

"

"

"

"

"

"

"

"

"

"

�2

Page 3: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

� ! ZILI MKATIMU!

""" Kalata Yamalonje! 5! ! Strategic Impact 1-Kudziwa za SI! 6! ! Njira 10 Zofikira Dziko Lanu! 7! ! Mapu a Strategic Impact! 8-9! """! ZIPHUNZITSO! 11! ! ! Tsiku Loyamba! ! ! ! ! “Ife ndi Ndani Ndipo Tiripo Chifukwa Chiyani?”! 12! ! ! ! “Kukhudzika pa Khristu ndi Miyoyo Yotayika! 14! ! ! ! “Khalidwe: Ngodya ya Atsogoleri a Chikhristu”! 16! ! ! ! “Masomphenya a Atsogoleri - Fikirani Dziko Lanu Lotaika”! 18! ! ! ! “Kufunika kea Uthenga Wabwino: Chiphunzitso cha Kulalikira”! 20! ! ! ! Chida Cholalikira cha SI! 22! ""! ! Tsiku Lachiwiri! ! ! ! ! “Kodi Utsogoleri ndi Chiyani?”! 26! ! ! ! “Dongosolo [Pulani] Lofikira Dziko Lanu Lotayika (Njira 10)”! 28! ! ! ! “Kudzipereka ku Ntchito Yaikuru”! 30! ! ! ! “Kufunika kwa Kuphunzitsa: Kupanga Ophunzira”! 32! ! ! ! Chida Chophunzitsira cha SI! 33! ""! ! Tsiku Lachitatu! ! ! ! ! “Mawu a Utumiki a SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MPINGO NDI! ! ! ! SUKULU YOCHULUKITSA ATSOGOLERI - KUITANIDWA KULEMBETSA”! 36! ! ! ! Mapu a Utumiki wa SI! 40-41! " " " “Ntchito 1 ya SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO”" 42" ! ! ! “Pangano Logwirana Manja”! 44! ! ! ! Mau a Chikhulupiriro a SI! 46-47! """""" "

�3

Page 4: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""

�4

Page 5: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

� ! MWALANDILIDWA!! ""Abale ndi alongo mwa Khristu,""Mwalandiridwa ku SI utsogoleri wabwino. Tiri okondwa ndi othokoza kuti mwabwera. Gulu lathu lakhala likukupemphererani kwa miyezi pokonzekera chochitika chimenechi.""Munthawi yathu pamodzi, tonse tilalika ndi zotipanikiza za tsiku ndi tsiku za utumiki ndi kusendera chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri ndi kudzala mpingo""Mumva kuchokera kwa abusa ndi atumiki ochokera maiko osiyanasiyana ndi Madera a mphatso osiyana ndi zokumana nazo zosiyanasiyana komabe onsewo ndi mtima woyaka kufalitsa uthenga wabwino wa yesu khristu ndikukwaniritsa ntchito yaikulu. ( Great Commission).""Pemphero lathu nthawi ino ndi lakuti mutsitsimutsidwe ndi mzimu woyera, mudzalandira masomphenya a bwino a moyo wanu ndi utumiki, ndipo musulidwa ndi maphuziro ndi zida kotero kuti ntchito yochulukitsa ophunzira ikhale mbaliimodzi ya moyo wa utumiki wanu ndi utumiki wa iwo amene mukuwatsogolera. Koma pamwamba pa zokhumbazi, ndi khumbo la mtima wathu kuti mukhale ndi kudabwitsa kwakukuru ndi chikondi chozama cha Ambuye wathu ndi mpulumutsi.""Mudzapatsidwa mphamvu m’madera a zosowa zanu, mudzalimbikitsidwa pamene mukaika, ndipo mubvekedwa zida pamene tipilira tonse kulondola Yesu Khristu.""Zikomonso pokhala nafe ndi chaulemu kukhala ndi inu.""Ine wanu wokondedwa,""Gulu la Strategic Impact (SI) "" " " ""

�5

Page 6: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

� "�6

Page 7: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

� "�7

Page 8: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

� """�8

Page 9: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

� ""�9

Page 10: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

"""""""""""""""""""""""""""""""""

�10

Page 11: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

� "

STRATEGIC IMPACT!MTSOKHANO WA ATSOGOLERI ©!

V2.0!""

“TENGANI MBALI PA NCHITO YAIKULU”!"

NDANDANDA WA ZIPHUNZITSO!"

STRATEGIC IMPACT ©!P.O. BOX 830337!

RICHARDSON, TX 75083!! WWW.TOUCHINGEVERYNATION.COM! ! "

�11

Page 12: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

TSIKU LOYAMBA, PHUNZIRO 1!STRATEGIC IMPACT - MTSOKHANO WA ATSOGOLERI!

“IFE NDI NDANI NDIPO TIRIPO CHIFUKWA CHIYANI?”!"KODI NDIFE NDANI: !"1. MASOMPHENYA: Tilipo ndi cholinga chopereka kwa munthu aliyense chiyembekezo

chokhala cha moyo wositha mwa Yesu Khristu. (Mateyu 28:18-20)""""2. CHOLINGA: Timaphunzitsa atsogoleri kuti akachulukitse ophunzira omwe adzayambitse

magulu kapena zochita zobzala mipingo paliponse. (2 Timoteo 2:2)""""3. NJIRA: Timakhazikitsa magulu a atsogoleri m’mizinda ya strategic ya padziko lapansi

kukachulutsa magulu abzale mipingo pakati pa anthu a mtundu uliwonse. (Machtidwe 19:9-10)"""

4. DONGOSOLO: "a. Seminala Yopereka Masomphenya (SYM) - “Oani Ntchito Yaikuru.”!"b. Mtsokhano wa Atsogoleri (MA) - “Tengani Mbali Pa Ntchito Yaikuru.”!

! ! - Ichi ndi chimene tikuchita pamodzi masiku ano.! "c. Sukulu Yachulukitsa Obzala Mipingo (SYOM) - “Phunzirani ndi Kukhala My Ntchito

Yaikuru.”!! ! - Tikuyembekedza kuti aliyense wa inu alembetsa mu sukulu imeneyi.! "

d. Sukulu Yochulutsa Atsogoleri (SYA) - “Tsogolerani ndi Kukhazikitsa Ntchito Yaikuru.”!"e. Msonkhano Wapamwamba Wokkupizira Moto (MWWM) - “Yochulukitsa Ntchito Yaikuru.”!"""

SITILI PANO CHIFUKWA CHIYANI:!1. Strategic Impact Sidzapereka thandizo la ndalama. ""2. Strategic Impact Sidzakumangirani nyumba ya mapemphero.""3. Strategic Impact Sidzakulemetsani ngati kuti tili ndi mayankho onse.""4. Strategic Impact Sidzasintha ziphunzito zanu. ""5. Strategic Impact Sidzadzala mipingo mu dzina limeneli la SI …… Tilipo kukuthandizani INU

kudzala mipingo YANU.""6. Strategic Impact Sidzachita ntchito m’malo mwanu."

�12

Page 13: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

NCHIFUKWA CHIYANI TILIPO - Kutsiriza Dzinthu 6: ""1. Kukula mu ubale wathu ndi Khristu. (2 Petro 3:18)"""""2. Kupindula luso la utsogoleri. """""3. Kuphunzira njira 10 zochulukitsira ophunzira odzala mipingo kufikira (dziko) lirilonse ndi dziko

la pansi. """""4. Kukupatsani zida zogwiritsira ntchito ndi upangiri wokuthandizani kuchulukitsa utumiki wanu. """"""5. Kupeza mabwenzi ndi ogwira nawo ntchito mmoyo wa chi Khristu ndi utumiki. """"""6. Kukhadzikitsa Sukulu Yochulukitsa Obzala Mipingo amene ali ndi kuthekera kophunzitsa

zikwi zikwi za ophunzira ochuluka, kuchulukitsa odzala mipingo ndi kuchulukitsa mipingo kuti itithandize kukwaniritsa ntchito yaikulu. """"""""""""

Tilipo chifukwa awa ndi masiku abwino omwe sanakhalepo kukhala ndi moyo monga Mkhristu!!"

TIYENERA kugwiritsa ntchito mwayi umene Mulungu watipatsa !kukwaniritsa zolinga zake pa ife!!"

�13

Page 14: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

TSIKU LOYAMBA, PHUNZIRO 2!STRATEGIC IMPACT - MTSOKHANO WA ATSOGOLERI!

“KUKHUDZIKA PA KHRISTU NDI MIYOYO YOTAYIKA”!""Timakula bwanji mukukhudzika kwathu pa khristu ndi otaika?!""I. LANDIRANI kukhudzika kwa chikondi cha Mulungu pa inu:!"" CHIKHALIDWE cha Mulungu ndi CHIKONDI. Umu ndi m’mene iye aliri.""" Mulungu ndi Atate okonda amene amakhuthula chikondi chake pa inu."""" “Mulungu watsanulira chikondi chake m’mitima yathu mwa !! ! mzimu oyera amene watipatsa ife.” - Aroma 5:5b""" "" Ndinu “kamwana ka m’diso" la diso lake. - Masalimo 17:8"""" Ndinu “olemekedzeka ndi amtengo wapatari” m’maso mwake. - Yesaya 43:4"""""II. YANKHANI (VOMERANI) pobwezera chikondi chanu kwa Mulungu:!"" Mau a Mulungu akuti: “tikonda ife chifukwa anayamba iye kutikonda.” - 1 Yohane 4:19"" " Pali chifukwa chokwanira kuti ifenso tiri pa ntchito yomukonda Mulungu "" " POVOMERA chikondi chimene iye anayambitsa."""" " “Mphunzitsi lamulo lalikulu ndi liti m’malamulo?” - Mateyu 22:36""" Yesu anafotokoza momveka: "! ! “UDZIKONDA AMBUYE MULUNGU WAKO NDI MTIMA WAKO ONSE !! ! NDI MOYO WAKO WONSE NDI NZERU ZAKO ZONSE .” ! ! ! ! ! ! ! ! ! ! ! ! - Mateyu 22:36!"! CHOPOSA ZONSE PA MOYO NDI CHIKONDI.""! Moyo wakhadzikia pati?!

1. KULANDIRA chikondi cha Mulungu.""2. KUKONDANSO Mulungu, ndi kenako:""3. KUGAWA chikondicho kwa ena.""

�14

Page 15: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

III. KUGAWA kukhudzika kwa Mulungu kwa omwe samudziwa:!"""" Pamene TALANDIRA kukhudzika kwa chikondi cha atate pa ife"" " ndi KUVOMERA pobwezera chikondi chathu kwa iye,"" " " “zidzamasulira ku” KUKHUDZIKA pa otaika.""""" “Chikondi cha Khristu chitikakamidza ife.” - 2 Akorinto 5:14""" "" Ndi chikondi cha khristu pa miyoyyo ya anthu "" " Chimene CHIMATISUNTHA IFE kupereka uthenga wa bwino kwa munthu aliyense "" " ofuna kumvera.""""" Mufunseni Mulungu akupatseni katundu wake pa otaika.""""""! Mulungu akukuitanani kukhala moyo wanu ndi !" " KUKHUDZIKA KOTENTHA pa khristu, ndipo kenako, kuposera apo, kukhala moyo " " wanu ndi KUKHUDZIKA KOTENTHA pa miyoyo ya otaika!!"""""""""""""""""""""""

�15

Page 16: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

TSIKU LOYAMBA, PHUNZIRO 3!STRATEGIC IMPACT - MTSOKHANO WA ATSOGOLERI!

“KHALIDWE: NGODYA YA ATSOGOLERI A CHIKHRISTU”!"I. Simungakhale mtsogoleri wachikhristu opanda khalidwe la Umulungu.!""

A. Pamene Mulungu akuyang’ana atsogoleri, amayang’ana poyamba ziyeneretso za khalidwe. (1 Timoteo 3:1-7; 1 Samuel 16:7)"""""

B. Khalidwe ndikuonetsa moyo wa Khristu ndipo ndiwofunikira pokwaniritsa cholinga chopanga ophunzira ochuluka. (Afilipi 3:17; 1 Atesalonika 1:6-9; 1 Akorinto 4:1-2; 11:1; 2 Timoteo 2:2)"""1. Kufunika kwa utumiki wathu ndi kubereka moyo wa khristu mwa ena amene akhoza

kupitiriza kwa ena, enawo kwa enanso etc."""2. Anthu a Mulungu sadzatsatira mtsogoleri ngati sakumukhulupilira mtsogoleri

ameneyo.""""" ** ichi nchifukwa chake mafunso a ungwiro a m’magulu m’masukulu ali ofunika kwambiri: "" " amakhudza makhalidwe!!"""""" " II. Khalidwe ndi lokhadzikika – kukhala mwamuna /mkazi wa Mulungu munyengo iliyonse

ndi munthu aliyense.!""A. Tanthauzo la khalidwe: “Kudalirika kumene kumatsatira ungwiro wowonetseredwa.”"""

1. Khalidwe la mkhristu wa umulungu liribe zinsinsi.""""2. Khalidwe la mhristu wa umulungu liribe sizitanthauza kufikapo, koma zitanthauza

ulendo. (1 Timoteo 4:15-16)""""�16

Page 17: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

III. Pali zinthu zinayi zofunika pa khalidwe la umulungu mwa atsogoleri a Chikhristu:!"""A. Lilime: Chitani chimene mwanena mudzachita (Masalimo 15:2-4; Yakobo 3:1-2)"""""B. Ndalama: “Thawani ku chikondi cha pa ndalama.” (Masalimo 15:5; 1 Timoteo 6:6-11)"""""C. Kugonana: “Thawani dama.” (1 Akorinto 6:18-20)"""""D. Mphamvu: “Funani kutumikra osati kutumikiridwa.” (Marko 10:42-45)""""""Simungakhale mtsogoleri wopambana opanda khalidwe la umulungu.!"""""""

ZOTIUNIKIRA: !1. 1."Kodi pali tchimo lobisika m’moyo wanu limene Mulungu akukuitanani kuti mulibvomereze

ndi kulisiya lero? (mawu anu, kusasamala ndalama dama, kufuna kutchuka ndi mphamvu?) Tsono ino ndi nthawi yolapa.""""""

2. Khalidwe la umulungu limaumbikrika pamene tikhala omasuka kwa anzathu ochepa odalirika (Ahebri 10:24-25). """""

3. Kodi muyamba kukumana ndi ndani kuyambitsa mafunso aungwiro a pagulu?""�17

Page 18: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

TSIKU LOYAMBA, PHUNZIRO 4!STRATEGIC IMPACT - MTSOKHANO WA ATSOGOLERI!

“MASOMPHENYA A ATSOGOLERI - FIKIRANI DZIKO LANU LOTAIKA”!"

Atsogoleri ambiri ali ndi masomphenya a zimene afuna kukwaniritsa. Koma monga atsogoleri a chi khristu tisoweka masomphenya azimene Mulungu afuna tikwaniritse.""

I. Masomphenya ndi chiyani? - Tanthauzo: Masomphenya ndi kutha “kuona” chimene palibe.!"""

A. Masomphenya athu alingane ndi masomphenya ndi Mulungu kuti akwaniritse ncthito yaikuru.""

1. Sitikusowa masomphenya atsopano – tifunika kuona ndi kudzipereka ku masomphenya oyamba a mpingo wake!""""

2. Mulungu akufuna munthu aliyense kumva uthenga wabwino ndipo padzakhala tsiku limene ichi chidzakwaniritsidwe. (1 Timoteo 2:4; 2 Petro 3:9; Mateyu 24:14; Chibvumbulotso 7:9-12)!"

" " 3. Nchifukwa chiyani tayenera kudzipereka tokha ku kulalikira dziko lonse m’moyo

mwathu?""""4. Inu ndi ine tayitanidwa pa nthawi ngati imeneyi ndi malo kuchita mbali yathu

m’masophenya a akuluwa!""""II. Mfunseni Mulungu pa, ndi kudzipereka kukwaniritsa masophenya ake kudzera

m’moyo wanu.!"A. Masomphenya amachokera pa mtima pa Mulungu. Simaloto amunthu ayi koma koma

zomveka bwino za ku mwamba.""1. Masomphenya a Mulungu sakhudzana ndi maloto anu!""""2. Masomphenya a Mulungu pa inu ndi m’mene IYE akugwiritsireni ntchito INU

kukwaniritsa zolinga zake . (Yeremiya 1:5)""""�18

Page 19: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

B. Muli ndi thandizo la padera lochita pa zolinga zake zosatha.""1. Turukirani tsogolo lanu lopanga ophunzira a maiko onse. (Mateyu 28:18-20)""2. Tukurani tsogolo lanu - tukurani mphatso zapa dera ndi maluso amene anakupatsani.""3. Fikirani tsogolo lanu. Kwaniritsani maitanidwe a Mulungu pa moyo wanu. "

" " " (Machitidwe 20:24; 2 Timoteo 4:7)" """ " III. Nchifukwa chiyani sitingathe kuchita popanda masomphenya?!"

A. Chifukwa chofunika kwambiri pa utsogoleri ndi masomphenya."""""""IV. Tingaikidze bwanji masomphenya kwa iwo timawatsogolera?!"

A. KHALANI MULOTO LA MULUNGU!""""""""""""""ZOTIUNIKIRA: !"1. Kodi masophenya a Mulungu ndi otani pa moyo wanu pokwaniritsa ntchito yake yaikuru? """"""2. 1." Lembani “uthenga umodzi” womveka, masophenya olwedzeka opatsidwa ndi Mulungu pa

moyo wanu ndi utumiki mu chiganizo chimodzi. """""�19

Page 20: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

TSIKU LOYAMBA, PHUNZIRO 5!STRATEGIC IMPACT - MTSOKHANO WA ATSOGOLERI!

“KUFUNIKA KWA YTHENGA WABWINO: PHUNZIRO LOLALIKIRA”!""

Chirichonse timachita pa SI chiyenera kutsatira kulalikira - !Kutengera uthenga wabwino wa Yesu Khristu ku dziko lotaika.!""

I. Kufunika kwa uthenga wabwino ndi CHIKHULUPILIRO mwa IMFA ya unsembe, kuikidwa M’MANDA ndi KUUKITSIDWA mthupi kwa Yesu Khristu. (1 Akorinto 15:1-4)!"

A. Paulo akumasulira zofunika zoyambira za uthenga wabwino umene anapereka ndi anthu otaika:""

1. Yesu Khristu anafera zochimwa zathu."""2. Anaikidwa m’manda."""3. Anaukitsidwa kwa akufa tsiku lachitatu."""4. Onse oika chikhulupiliro chawo mwa Yesu khristu ngati mpulumutsi wawo

adzakhulukidwa machimo awo ndi kulandira moyo wosatha. (1 Akorinto 15:1-2, 51-53)!""

" " B. Tisawasokoneze anthu pa zimene ayenera kukhulupilira kuti apulumutsidwe!"""""""

II. Tiyenera kupereka ZOFUNIKA ZONSE momveka kwa anthu za uthenga wabwino ndikuwapatsa mwayi wobvomeredza ndi chikhulupiliro mwa Yesu ngati njira yokhayo yokhala ndi moyo wosatha.!"

A. Paulo mwini anapempha mapemphero kuti akhale ndi mwayi wogawa uthenga wabwino ndikuti amveketse kwa iwo anawayankhula. (Ephesians 6:19-20; Colossians 4:3-4)"""

B. Ifenso tayenera kutengerapo mwayi uliwonse wogawa uthenga wabwino mophweka wa Yesu Khristu mochuluka m’mene tingathere.""

�20

Page 21: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

III. Chida cha ulaliki cha SI chakonzedwa kukuthandizani kugawa uthenga wophweka wabwinowu ndi kupereka kwa ena mwayi woyika chikhulupiriro chawo mwa Khristu.!""""""""""

IV. Lamulungu likubwerali likhale la “la Mulungu la uthenga wabwino” ku mpingo wanu.!"A. ABUSA: Gawani umboni wa momwe munakhulupirira mwa Khristu.""B. ABUSA: Gawani mophweka, uthenga womveka wa uthenga wabwino.""C. ABUSA: Perekani kwa anthu mwayi wolandira khristu mwa chikhulupiriro.""""""""""""""""""""""""""""""""""

�21

Page 22: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

TSIKU LOYAMBA, PHUNZIRO 5!STRATEGIC IMPACT - MTSOKHANO WA ATSOGOLERI!

“CHIDA CHOLALIKIRA CHA SI”!"

"TINGAGWIRITSE BWANJI CHIDA CHOLALIKIRA CHA STRATEGIC IMPACT!"

� !1. Gawani umboni wanu wa: "

• Kodi moyo wanu udali bwanji musanakhulupirire Yesu, "

• Kodi mudatani poika chikhulupiriro chanu mwa Yesu ngati mpulumutsi wanu,"

• Kodi moyo wanu udasiyana bwanji mdi wakale pamene/mutatha mudakhulupirira mea Yesu pa chipulumutso. " "Awonetseni mbali ya patsogolo ya

chipangizocho. !Nenani: “Ndingakufunseni mafunso ochepa pa za chomwe mumakhulupirira ndi kukuonetsani kuchokera m’baibulo momwe mungazitsimikizir kuti muli ndi moyo wosatha?”!

2. Aonetseni chithunzi cha ngodya zitatu kuti, chikuimirira Mulungu. Afunseni , “Kodi mukukhulupirira kuti iye amakukondani?” Dikirani kuti munthuyo akuyankheni. Mafunso awa achititsa kuti muzikambirana osati kumangoyankhula nokha pa iwo."""

3. Ndi kofunika kuwerenga ndimeyo kuchokera m’baibulo motsatana ndi chithunzi chirichonse. Yamabani ndi Yohane 3:16. (1)"

• Funsani ngati munthuyo ali ndi Baibulo. Ngati alinalo, awuzeni alitenge ndi kuwathandiza kuyang’ana ndimezi m’baiibulomo."

• Zingakhale bwino ngati munthuyu awerenge ndimezo. Komabe, muwazindikire ngati sangathe kuwerenga. Ngati azengereze kapena kunena kenakake monga: “ndilibe magalasi,” pamenepo awerengereni."""

4. Awonetseni chithunzi cha munthu chomwe chilli m’munsi pa gawo loyambalo. Afunse, “Kodi chinthunzichi mukugaaniza kuti chikuimira chiyani?” Atha kunena kuti ‘‘anthu’’ kapena ‘‘satana’’ kapena munthu wina wake. Auzeni kuti chithunzichi chikuimirira wina aliyense pa dziko lapansi; inu, ine ndi aliyense. Lozani chipata chaduda chimene chikuonetsa kuti anthu alekanitsidwa ndi Mulungu. Werengani Aroma 3:23 (2) ndi kufunsa, “Baibulo limati ife tidalekanitsidwa ndi Mulungu chifukwa aliyense wa ife adachimwa. Kodi mukhulupira kuti mudachimwira Mulungu?”!""

5. Werengani Aroma 6:23 (3) Werengani Aroma 6:23 (3) mkati mwa chimpata chakuda chomwe chikuonetsa anthu olekanitsidwa ndi Mulungu. Afunseni kuti, “kodi mumakhulupirira kuti machisomo anu amabweretsa imfa kulekana ndi Mulungu kwa muyaya?”"

�22

Page 23: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

� !""""

� !"

6. Pitani pagawo lotsatira lomwe likuonetsa mtanda. Werengani Aroma 5:8 (4) ndi kunena kuti, “Mulungu amatikonda ndipo adapereka njira kwa ife kuti timziwe iye potumiza mwana wake, Yesu Khristu kuti afe pamtanda polipira machismo athu. Kodi mukhulupirira kuti Yesu adafera pa mtanda chifukwa cha inu?”!"

7. Werengani Yohane 14:6 (5) ndi kunfunsa kuti, “kodi mukukhulupirira kuti Yesu Khristu ndi njira yokhayo yopezera moyo wosatha mwa Mulungu?”!"

8. Werengani 1 Akorinto 15:3-8 (6) ndi kunfunsa kuti, “kodi mukukhulupirira kuti Mulungu adamuukitsa Yesu kwa akufa?”!""

9. Pitani pa gawo lotsatira lomwe likuonetsa chithunzi cha mphatso ndi kunenea kuti, “Mulungu akufuna inu kuti mukhale ndi moyo wosatha komanso iye amapereka moyo wosatha ngati mphatso yaulere.” Kenaka werengani Aefeso 2:8-9 (7) nenani, “Ngati mukukhulupirira pa dzina la Yesu, Mulungu akupangani kukhala mwana wa Mulungu” Kenaka werengani Yohane 1:12 (8). !"

10.“Mulungu akanena izi kwa iwo amene akukana mphatso yake:” werengani (2 Atesalonika 1:8-10) (9). Koma ngati muvomereza kuti mudakhala ndi moyo wosatha ndi iye (1 Yohane 5:11-12) (10). !"

11. FUNSANI: “Kodi mukufun akulandira mphatso ya moyo wosatha mwa chikhulupiliro mwa Yesu Kristu lero?” !"

12.Ngati ayankhe kuti “Inde,” werengani Aroma10:9-10 (11). mutha kulandira Khristu mwa kukhulupirira mumtima mwanu ndi kuvomereza ndi pakamwa panu. Pemphero silingakupulumutseni. Ndi chikhulupiriro chanu mwa Yesu Khristu chomwe chingakupulumutseni.Mawu a pemphero atha kukuthandizani kufotokoza chikhulupiriro chanu. Apa pa pemphero losavuta: “Ambuye Yesu, ndikusowani, ndikumvomereza kuti ndakuchimwirani, chonde khululukirani machimo anga, ndikulandira mphatso yanu ya chikhululukiro cha machimo ndi moyo wosatha lero mwa Chikhulupiriro . M’dzina la Yesu, Amen.”!

�23

Page 24: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

"""""

� !

"""""13.Atatha wina kulandira mphatso yaulere ya

Mulungu ya moyo wosatha mwa chikhulupiriro, mfunseni, “Kodi mudakhulupirira mwa Khristu kuti atikhululukireni ndi kukupatsani moyo wosatha?” Kenaka alimbikitseni m’chikhulupiriro ndi kuwapempherera.""""

14.Ng’ambani gawo lotsiriza la chipangizocho. Lembani dzina keyala ndi foni zawo m’malo oyenenera. """"

15.Ngati nkotheka khazikitsani nthawi yokomana nawo mawa kuti mnyambe kuwaphunzitsa pogwiritsa ntchito chipangizo cha Strategic Impact.""""

16.Perekani dzina, keyala kapenanso foni nambala za munthu yemwe walandira kumene Yesu Khristu kwa Mtsogoleri wa Seko ya mpingo imene idabzalidwa.""""

""

� !"�24

Page 25: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""

�25

Page 26: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

TSIKU LACHIWIRI, PHUNZIRO 1!STRATEGIC IMPACT - MTSOKHANO WA ATSOGOLERI!

“KODI ATSOGOLERI NDI CHIYANI?”!""I. Kodi Atsogoleri ndi Chiyani? - “Utsogoleri ndi kutakasa anthu kuti akwaniritse cholinga.”""""II. M’tsogoleri ndi Ndani?!"

A. M’tsogoleri ndi munthu amene:!"1. Amadziwa kopita [MASOMPHENYA]""2. Amadziwa mafikidwe a kumalowo [DONGOSOLO / pulani]""3. Amadziwa kutakasa ena kuti apite naye [KUTAKASA]""""

B. Choncho zinthu zopanga utsogoleri ndi:!"1. Masomphenya: Kopita.""2. Dongosolo (pulani): Tikafikako bwanji.""3. Kutakasa: Tingadzutse bwanji chikhumbokhumbo mwa ena kuti atenge nawo mbali.""4. Koma m’tsogoleri wa chikhristu pali chofunika cha chinayi (4): Khalidwe: Chidaliro

chotsatira ungwiro wovomerezeka.!"""III. Atsogoleri kodi amatani? Kodi atsogoleri a Chikhristu adzitani powonjezera chikoka

chawo pa anthu a Mulungu kuti akwaniritse ntchito yake yaikuru?!"A. Kuikidza (kugawa) MASOMPHENYA.!"""B. Akhale ODALIRIKA.!

1. Kudalirika ndi chiyeneretso chimodzi sitingachiphunzire, chayenera KUPEZEKA nthawi zonse kudzera mu khalidwe LOKHAZIKIKA ndi ZOLINGA zabwino."""""""

�26

Page 27: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

C. Kupereka CHIWERUZO CHOZAMA.!1. Chiweruzo chozama tingachitukule ndi:"

a) Kupeza chidziwitso cha mawu a Mulungu."b) Kupeza nzeru zoumbidwa kuchokera mu zomwe tinadutsamo kale."c) Malangizo ochokera kumbali zosiyanasiyana amene ali akuru ndi anzeru.

“Pochuruka aphungu pali chigonjetso .” Miyambo 15:22""" "

D. Kuchita DONGOSOLO.!"""E. Kuwonetsa KUKHUDZIKA:!"""F. Kukhala OLIMBA MTIMA.!

1. Atsogoleri amatenthetsa anzawo ndi malingaliro a “tikhoza kukwanitsa”."""" "

G. Kuonetsa CHIKONDI momasuka.!1. 1 Timoteo 4:5, “pothera pa langizo lathu ndi chikondi.” (Cholinga cha utumiki,

POGONERA (target) pa ntchito yathu ndi CHIKONDI).""2. “M’tsogoleri ndi wokonda, ndipo wokonda nthawi zonse adzakhala m’tsogoleri.”""""

H. Nenani “ZIKOMO” kawirikawiri ndi mobwereza bwereza.!1. ONETSETSANI KUYAMIKIRA. Anthu “amafera” kukhululupiridwa ndi kuyamikiridwa!""""

I. YENDANI ndi Mulungu.!1. Chilichonse mumachitandi chipatso cha kuyenda ndi mulungu moyo wonse."""

! !J. Kuchita mu mphatso yanu yomwe munapatsidwa: “Khalani wabwino pachimene

mumachita bwino.”!"""ZOTIUNIKIRA: !1. Ndi ziyeneretso zitatu zimene mukhalire chidwi podzitukura nokha miyezi isanu ndi umodzi

(6) ikubwerayi kuonetsetsa kuti mukuwakopa anthu kukwaniritsa zolinga za Mulungu?"""2. Mutukura ziyeneretso zimenezi motani?""

�27

Page 28: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

TSIKU LACHIWIRI, PHUNZIRO 2!STRATEGIC IMPACT - MTSOKHANO WA ATSOGOLERI!

“DONGOSOLO [PULANI] LOFIKIRA DZIKO LANU LOTAYIKA (NJIRA 10)”!""Kodi Mulungu akufuna chiyani? (1 Timoteo 4:5)!""Mulungu amakwanitsa khumbo lake motani? (Mateyu 28:18-20; Machitidwe 1:8)"""Kodi dongosolo la Mulungu ndi lotani? !! (Machitidwe 20:24, 19:9; 2 Timoteo 2:2; Akolose 1:8, 4:12; Machitidwe 19:10; Akolose 1:7)""""

NJIRA KHUMI ZOTSUKUNULIRA DERA LANU NDI!UTHENGA WABWINO WA YESU KHRISTU!"

GAWO 1: SITHANI kuganiza KWANU kuchokera ku chilinga ‘’cholinga mpingo wanga’’ ndi ! ! "" kupita ku ‘’kufukira dera langa, dziko langa ndi dziko lapanzi’’ lotayika. "" (Mateyu 16:18; 28:18-20)""""""GAWO 2: PEMPHERO! Pempherani likutire ndi kulowerera pa dongosolo lonse lodzala mpingo "" (Machitidwe 13:1-3)"""""""GAWO 3: Kugawa MASOMPHENA kwa anthu a Mulungu pa ntchito yodzala mipingo. "" " (Machitidwe 1:8; 13:1-3)"""""""GAWO 4: Zindikirani, sankhani, sonkhanitsani ndi kutsula (kukonzekeretsa) gulu lodzala mpingo "" osachepera chaka chimodzi. "" (Machitidwe 14:21-28; 19:9-10; Akolose 1:7; 2 Timoteo 2:2)"""""

�28

Page 29: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

GAWO 5: Mwapemphero sankhani dera kumene mudzaleko mpingo wa m’nyumba (cell "" Church). "" (Machitidwe 16:6-40)""""""GAWO 6: LALIKILANI anthu m’dera lane people in the area. "" (Machitidwe 5:42; 14:21, 25; 20:20)""""""GAWO 7: PHUNZITSANI otembenuka mtima mwatsopano kumene ali.!! (Machitidwe 14:22; 20:20)""""""GAWO 8: SONKHANITSANI otembenuka mtima mwatsopano mu mpingo wam’nyumba " "" watsopano. "" (Machitidwe 2:42, 46; 12:12; 16:40; Aroma 16:15; 1 Akornito 16:19; Akolose 4:15)""""""GAWO 9: CHULUKITSANI ophunzira ndi mpingo watsopano wa m’nyumba . !! ! (1 Atesalonika 1:7-8; 2 Timoteo 2:2)"""""""GAWO 10: Kugeirana manja ndi abusa ena kapena atsogoleri kukhazikitsa mayendedwe odzala "" kukwaniritsa ntchito yaikuru."""""""""" " "

�29

Page 30: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

TSIKU LACHIWIRI, PHUNZIRO 3!STRATEGIC IMPACT - MTSOKHANO WA ATSOGOLERI!

“KUDZIPEREKA KU NTCHITO YAIKURU”!"

Ntchito yaikuru ikhale patsogolo la utumiki pa moyo wanu wonse. !""1. Ulamuliro wa yesu umatikokera ife kuchita chimene iye afuna. Mateyu 28:18!"""""""2. Lamulo la Yesu limafotokoza za zimene tayenera kuchita. Mateyu 28:19!"

a. Lamulo limodzi mu vesi limeneli ndi kupanga ophunzira ndiponso kutifokozera m’mene tingapangire ophunzira. ""i. Timapanga izi pamene tipita kwa anthu osiyana.""ii. Timawabatiza kuwayambitsa chikhulupiriro cha utatu woyera.""iii. Timawaphunzitsa kumvera zonse iye watiphunzitsa.""""

b. Izi zisaleke mpaka Yesu atabweranso. !""Lamulo Ophunzira ndi machitidwe opatsidwa kupanga zimenezo !

zikhale zoyambirira zathu mu utumiki wathu!!""3. Kupezeka kwa Yesu kumatipatsa chilimbukitso kuti tikwaniritse lamulo lake. vesi 20!""""Ngatimunayamba mwapita ku fakitale yopanga nsapato ndiye mwapeza anthu opanga zinthu zambirimbiri zokongola koma sapanga nsapato – kukhala kulephera."""Ngati mpingo wanu sukuturutsa ophunzira ochuluka sitikupanga zimene Khristu watilamulira. (Akolose 1:23-29)!""""

�30

Page 31: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""�31

Page 32: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

TSIKU LACHIWIRI, PHUNZIRO 4!STRATEGIC IMPACT - MTSOKHANO WA ATSOGOLERI!

“KUFUNIKA KWA KUPHUNZITSA: KUPANGA OPHUNZIRA”!""I. Tiyenera kuwayendera otembenuka mtima kumene, kuwaphunzitsa kumene

amakhala, komwe amagwira ntchito ndi kupita pa moyo wawo wa tsiku ndi tsiku.!"

A. Tiyenera kuwapitira kwawo osadikira kuti iwo atiyendere.""""""II. Yambani kugwiritsa ntchito zotitsogolera ndi mitu 4 pa maulendo 4 kumbuyo

kwa chida cholalikila cha SI (onani m’mene mugwiritsire ntchito chgida cholalikira cha SI potsatira phunziroli).!""""""

III. Mutatha kuyendera kanayi (4) koyambirira, funsani ophunzira okhulupirika kuti apitirize kukumana ndi inu popitiriza kukula ndi kuphunzira.!"""""""""""

Sizokwanira kungolalikira ndikuwapanga kuvomereza chikhulupiriro mwa Khristu. Yesu sanatilamulira ife kupita ndi kukapanga ziganizo koma kupita ndi kukapanga ophunzira. """Sizokwanira kuwaitanira otembenuka mtima kumene kuli mpingo wanu, muyenera kuwathandiza panokha mwachikhulupiriro chawo chatsopano. Tiyenera kusamalira aliyense payekha kwa otembenuka mtima kumene kuwathandiza kukula kufikira kukhwima ndi kuchurukitsa ophunzira!"""

�32

Page 33: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

TSIKU LACHIWIRI, PHUNZIRO 5!STRATEGIC IMPACT - MTSOKHANO WA ATSOGOLERI!

“MAGWIRITZIDWE NTCHITO A CHIDA CHOPHUNZITSIRA CHA SI”!"

Tsatirani njira 5 izi pamene mwakumana pamodzi:!"1. UBALE: Funsani m’mene akuchitira ndikudziwa chimene chakhala chikuchitika mu miyoyo yawo mu

kukumana kwanu kwapita.""2. LIMBIKITSANI: Yambani nthawi yanu mokhwima kuyankha mafunso achilimbikitso / ungwiro: "

a. Kodi munapereka nthawi panokha ndi Mulungu mu mawu ake ndi pemphero kucokera m’mene tinakumana? Mulungu anakuyankhula chiyani?""

b. Kodi mwayenda mu chikondi m’maubale anu ofunika ndi ena m’banja lanu, m’maubwenzi, anansi ndi mpingo?""

c. Kodi mwachitapo khalidwe lonyansa?""d. Kodi munakwaniritsa malonjezo munapanga nthawi yathu yosanthula baibulo? Motani?""

� !"3. KAMBIRANANI: Werengai ndi kukambirana

ndime ya Baibulo yoperekedwa kokumana kalikonse pa phunziro pogwiritsa ntchiti funso 6 (Malangizo ali pa chida chikuoneka pamwamba):"

""a. Mukhale ndi ophunzira atsopano agawike

m,agulu a atatu (3) ndipo gwiritsani ntchito mafunso 6 (akuoneka m’musi kuchita).""

� "

�33

Page 34: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

� "

""""b. Onaninso ulendo 1 “Kudziwa Yesu?”

molingana ndi Yohane 1:1-18. """"c. Onetsetsani kuti aliyense akumva bwino

kukambirana mafunso pamodzi molingana ndi ndime ya malembo. [Dziwani kuti awa si malo a chiphunzitso koma kumuthandiza otembenuka mtima kumene m,mene angawerengere ndi kugwiritsa ntchito malembo m,miyoyo yawo]!""""

"""4. PLAN (DONGOSOLO): Gwirizanani pa mawu ochepa kuti aliyense awerenge payekha mkatikati

mwa sabata (Ma chaputala 3 pa tsiku ndi oyerekeza).""a. Khalani a chidwi pa omwe sadziwa kuwerenga""b. Pezani njira zina monga ma baibulo oyankhula ngati nkotheka""c. Onetsetsani kulemba mayankho ochokera m,mafunso 5 ndi 6 kuti mudzawatsatire bwino

mudzakakumananso""d. Pangani dongosolo la kukumana kwanu pa kuphunzitsa kwina""e. Dziwani amene amadzipereka ndi okhulupirika kutenga nawo mbali kuwerenga kwawo, ndi

okonzeka kuphunzira mochuluka za khristu ndi kufalitsa yesu ndi ena. Amenewa ndi anthu amene mupitirire nawo ndi ubale wa chiphunzitso pakatha kukumana ka 4""""

5. PEMPHERANI: Tsirizani nthawi yanu popemphera pamodzi pa wina ndi mzake kudzipereka kumene kwapangidwa kuchokera mafunso 5 ndi 6."""""

�34

Page 35: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""""�35

Page 36: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

TSIKU LACHITATU, PHUNZIRO 1!STRATEGIC IMPACT - MTSOKHANO WA ATSOGOLERI!

“MAWU A UTUMIKI A SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO NDI SUKULU YOCHULUKITSA ATSOGOLERI - KUITANIDWA KULEMBETSA”!

""“Kodi timapereka motani kwamunthu aliyense mu mzinda wathu, dziko, fuko lathu, chigawo chathu mwayi woyankhula inde kwa Yesu?”"""I. Paulo amaphunzitsa anthu mu mzinda umodzi (Aefeso) ndikufikira fuko lonse (Asiya)

ndi uthenga wabwino mu zaka ziwiri ! (Machitidwe 19:8-10)!"""""" "

Tsono izi tingazitsatire bwanji, ndipo tingadzichitenso motani?!"""II. Paulo anatsatira chitsanzo cha 2 Timoteo 2:2 amaphunzitsa aphunnzitsi aphunzitsi

ochulukitsa, amene anapanga ophunzira ochulukitsa amene anayambitsa mipigo yochulukutsitsa. CHITSANZO:!""

" Paulo1 —> Epafara2 (Aefeso?)"" " " """ " " Epafara2 —> Akipa3 and Afiya3 (Akolose)"""" " " " " Akipa3 and Afiya3 —> Nympha4? (Laodekiya?)""""III. TIYENERA kutsatira chitsanzo chimenechi ngati tikufuna kuona zotsatira mu mzinda

wathu, dziko ndi chigawo chathu!!"A. Dongosolo loyamba: Lalikirani, Phunzitsani, Sulani Komanso Chulukitsani.""""B. Mapu a Utumiki!""""

" " �36

Page 37: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

IV. Ngati muli okhulupirira kulembetsa ndi kutsatira dongosolo zinthu izi zidzachitika:!""A. Mudzakula mu chikhulupiriro chanu ndi kukhala wodzala mpingo wokhwima ndi

m’tsogoleri."""B. Mudzapeza maubwenzi apafupi ndi okulimbikitsani mukuyenda kwanu ndi utumiki wa

Khristu."""C. Mudzapindula ena ku chikhulupiriro mwa yesu Yesu Khristu."""D. Mudzayambitsa ndi kutsogolera osalephera mpingo wam,nyumba umodzi."""E. Mudzaphunzitsa ochulukitsa kudzala mipingo ena ndi atsogoleri ku m,badwo wa chinayi.""""""""""""""""""

"Sitiri pano kungokhala ndi msonkhano wabwino.!

"Tiripo kukhazikitsa mayendedwe ofikira dziko lapansi !

ndi uthenga wabwino wa yesu Khristu.!"""

Chokubetcherani (challenge) kwainu ndi kudzipereka "kukhala wophunzira wochurukitsa ena polembetsa mu"

SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO.!"�37

Page 38: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

""" " "

�38

Page 39: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

� !" "

�39

Page 40: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

� !�40

Page 41: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

� !"�41

Page 42: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

TSIKU LACHITATU, PHUNZIRO 2!STRATEGIC IMPACT - MTSOKHANO WA ATSOGOLERI!

“NTCHITO 1 YA SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO”!""

SYOM ndi chida chokuthandizani kukula kukhala wochulukitsa amene mulungu akhoza kumugwiritsa ntchito kukwaniritsa zolinga zake painu kumene muli mu

m’badwo uno.!""DZIWANI: Sukulu Yochulukitsa Obzala Mipingo isoweka Nkhalapakati wa chigawo chirichonse.!"Udindo wa Nkhalapakati ndi uwu:""1. 1! Kukhazikitsa tsiku ndi nthawi imene sukulu idzakumane.! !

a. Sukulu idzikumana sabata lirilonse kwa masabata 14 pa gawo irilonse la SYOM. Ngati gulu laganiza zodumpha sabata limodzi pazifukwa zina, ayenera kudzayambira pamene analekeza osadumpha ntchito. ""

2. Kuyambitsa ndi kutseka msonkhano pa nthawi yomwe anapangana. (Aefeso 5:15-16; Yakobo 5:12)!a. Kukumana kulikonse kuyenera kutha ora limodzi kapena ora ndi theka.

Nkhalapakati ayenerakuyambitsa msonkhano pa nthawi yake ndi kuonetsetsa kuti watha pa nthawi yache.""

3. Onetsetsani kuti anzanu otenga nawo mbali pa mafunso a ungwiro ali gulu la anthu atatu kapena asanu.!a. Chimodzi mwa zofunika pa sukuluyi ndi magulu a anthu atatu kapena asanu.

Maguluwa amakumana pamodzi, poyamba kwa kukumana kulikonsekwa mphindi 20 kapena 30 kufunsana mafunso a ungwiro. Ichi ndi chofunika ndipo nkhalapakati awonetsetse kuti aliyense watengapo mbali pa magulu amenewa ndipo kuti magulu akukumana pachiyambi pa phunziro lirilonse.""

4. 1! Kutsogolera gulu kuyankha ntchito (mafunso).!a. Patatha nthawi yaungwiro ndi magulu osintha moyo,asonkhanitse aliyense pamodzi

kuwerenga ntchito ndi kuyankhula kudzera kukambirana mafunso.""5. 1! Kusunga mbiri ya anthu opezeka.!

a. Nkhalapakatiazidziwa ndani amene akupezeka pa kukumana kulikonse, ndipo ngati anachita ntchito ya pa sabata. Kalata yovomereza (certificate) iyenera kuperekedwa pakutha pa sukulu yochulukitsa odzala mipingo. Okhawo anakhulupirika pa kutenga nawo mbali kupezeka ndi kumaliza ntchito ya pa sabata adzalandira kalatayi.""

" "�42

Page 43: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

Pali MFUNDO 5 ZOFUNIKA kwambiri pa SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO:!"1. CHIYANJANO, UNGWIRO NDI KUWERENGA BAIBULO - Commit to the Life

Transformation Group (Ahebri 10:24-25, Yakobo 5:16).!a. Uwu ndi mtima wa SYA kumeneku ndi kupanga ophunzira. Ndikulimbikitsana wina ndi

mzake m’chikondi ndi m’ntchito. Ndi kuvomereza tchimo ndi kusungirana ungwiro pa kuyenda kwathu ndi Khristu. Sichikuyenera kukhala lamulo koma chiyanjano cha chikondi chimene chimathandiza yense wa ife kukhala chimene Mulungu afuna tikhale. ""

2. KUPHUNZIRA - Kuwerenga ndi kukambirana ntchito ya sabata iliyonse.!a. Zochitazi zapangidwa kuti zidutse kuganiza kwanu ndi kukambirana maganizo pamodzi

ndi amene akukuthandizani kukula pa mutu uliwonse. Tangowerengani nkhaniyo ndi kuyankha mafunso okambirana. Kukambirana kwanu wina ndi mzake kudzakuthandizani koposa kupeza ndi kuphunzira mutuwo.""

3. KUTURUKA KUNJA - Funani kufalitsa uthenga wabwino ndi wina sabata lirilonse. (2 Akorinto 5:20)!a. Cholinga chathu nthawi zonse ndi kuchita nawo powauza wena omwe akhoza

kukhulupirira Khristu. Mbali ya SYOM ndi kuchita kwanu pafupi pafupi zimenezi zikhoza kuchitika mosiyana siyana : kufunsa mafunso a uzimu, kunena umboni wanu , kunena m’mene Mulungu wagwirira ntchito m’moyo wanu posachedwa, kupereka mayankho ku pemphero, kugawa mau a uthenga wabwino. Mukamachita izi; mudzapeza amene ali omasuka ndi ofuna kulandira Ambuye Yesu.""

4. KULAMBIRA KOMVERA - Chitani ntchito sabata iliyonse. (Yakobo 1:22-25 - Dalitso limadza pakuchita)!a. Mukachita ntchito zimenezi mudzapanga ophunzira amene afikire dziko . Zapangidwa

kukhazikitsa ulendo opanga ophunzira opanga ophunzira amene adzle mpingo. Osati ya nzeru / ntchito yodziwitsa, koma yosintha miyoyo. "

" " 5. PEMPHERO ndi KUCHULUKITSA - Pempherani, lembani ndi kutsogolera oxzala

mipingo kudzera mu SYOM pakathagawo loyamba. (2 Timoteo 2:2)!a. Ngati mulibe wina woti muyamba kumutsogolera kudzera mu buku la gawo 1

simudzaloledwa kupitiriza mu buku la gawo 3 ndi gulu lanu lenileni. Iyi ndi sukulu yochulukitsa atsogoleri ngati simuli oknzeka kuthandiza ena , musapitirire. Mukaonetsetsa kuti mwakonzeka kuthandiza ena,pamenepo mukhonza kupitilira."""

NTCHITO YA KUKUMANA KWA PA SABATA:!1. Mafunso a ungwiro"

a. Apa sipoweruzana, koma pa chilimbikitso cha Chikondi kufikira ku Chilungamo. ""2. Ntchito"

a. Werengani gawo loyamba"b. a." Tengani mbali pa zokambirana za gulu"

i. DZIWANI: Iyi sinthawi yolalikira. Iyi ndi nthawi yophunzira kwa wina ndi mzake. "c. Pitirizani mpaka mwatsiriza ntchito""

3. Zochita pa Sabata Lililonse"a. Pakutha pa masiku 7, CHITANI ntchito. "b. SYOM si yongophunzira kokha-koma KUCHITA. "

�43

Page 44: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

TSIKU LACHITATU, PHUNZIRO 4!STRATEGIC IMPACT - MTSOKHANO WA ATSOGOLERI!

“PANGANO LOGWIRANA MANJA”!""Yesu anadza pacholinga choyanjanitsa dziko lapansi kwa iye mwini! (Luka 19:10)!"""Iye safuna kuti wina asemphane ndi mwai wonene inde kwa Yesu! (2 Petro 3:9)!"""Njira yake yokwaniritsa chimenechi ndi ife. Taturutsidwa mu m’dima ndikulowetsedwamu kuunika kotero kuti ife tilalikire zoposa zake ku m’badwo uno! (1 Petro 2:9)!""""Ndife akazembe ake ku dzikoli, ndife antchito ake (oumuimilira) kufikira m’badwo uno ndi chiyembekezo chokhacho cha chipulumutso mwa Yesu Khristu! (2 Akorinto 5:20)""""John Knox, mlaliki wa CCAP ochokera ku Scotland, analira kwa Mulungu: !"

“Ndipatseni ine Scotland… kapena ndife” """Kufuna kusinthasintha moyo wake chifukwa cha miyoyo yawo yosatha. Mulungu amalemekeza pemphero loswekalo, ndi kugwiritsa John Knox mwamphamvu kulalikira dziko lake. ""Tikuyang’anira muyezo omwewo wodzipereka! """"

Ngati muli oona mtima 100% pamaso pa Mulungu "wamphamvu zonse ndikukuitani kupanga pangano limenelo ndi ife pakali pano: ""

“Ambuye, mwa chisomo chanu, ndikudzipereka ndekha KWA INU.!Ndipo pamodzi ndi John Knox, tikupemphera:!"

‘Ndipatseni ______________________… kapena ndife’!"Ndikulonjeza kwa inu, atate wakumwamba, kudzipereka ndekha kufikira m’badwo wanga

ndi uthenga wa Yesu Khristu kapena kufa poyesera. !"M’dzina la Yesu, Amen.”!

" �44

Page 45: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

NOTES!___________________________________________!___________________________________________!___________________________________________!_______________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________"

___________________________________________"

______________________________________________________________________________________!"

�45

Page 46: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

� ! MAU A CHIKHULUPIRIRO A SI! "MULUNGU!Genesis 1:1; Dueteronomo 6:4; Mateyu 28:19; Yohane 4:24, 10:30; 2 Akorinto 13:14!Timakhulupirira kuti pali Mulungu m’modzi owona, oyera, wopezeka kosatha mwa atatu atate, mwana ndi Mzimu Woyera ali ndi ndi ziyeneretso zofanana za u Mulungu makhalidwe a umunthu. Pachiyambi Mulungu analenga popanda kanthu dziko lapansi ndi zinthu zonse ziri m’mwemo, kumeneko kuonetsera ulemelero wa mphamvu yake, nzeru ndi ukoma. Mwa mphamvu yake ya umulungu akupitiriza kukhazikitsa chilengedwe chake. Mwa kupereka kwake akugwira ntchito kudzera mu mbiri kukwaniritsa zolinga zake zakuombola.""YESU KHRISTU!Mateyu 20:28; Machitidwe 4:12; Aroma 5:10; 2 Akorinto 5:18-19; 1 Yohane 2:2!Yesu Khristu ndi munthu wamuyaya wachiwiri wa utatu amene analumikizidwa kosatha ndi chibadwidwe cha munthu mwa kuima kodabwitsa mwa namwali. Anakhala moyo womvera kwathunthu kwa atate ndipo mwaulere anatetezera (analipira) machismo a onse pakufa pa mtanda ngati mlowam’malo wawo, kumeneko kukwaniritsa chilungamo cha kumwamba ndi kukwaniritsa chipulumutso ndi moyo wosatha wa onse amene akhulupirira mwa iye yekha. Anauka kwa akufa mu thupi lomwelo, ngakhale alemekezedwa, m’mene iye anakhala ndi moyo nafa anakwera kumwamba, nakhala pa dzanja lamanja la Mulungu la atate, komweko iye nakhala pakati pa Mulungu ndi munthu, akupitiriza kupembedzeraake a yekha. Adzabwera ku dziko lapansi, yekha maso ndi maso, kukwaniritsa zochitika zonse ndi dongolsolo losatha la Mulungu.""MZIMU WOYERA mdi MOYO WA CHIKHRISTU!Yohane 15:26, 16:8-11!Mgwirizano wa chilengedwe wa kutumikira kwenikweni mu ubale ndi Yesu Khristu ndi moyo wa chiyero ndi kumvera, umapezedwa ndi okhulupirira pamene agonjera kwa M’zimu woyera, munthu wachitatu mu utatu. Anatumidwa pa dziko ndi atate ndimwana kuonetsera kwa munthu ntchito yopulumutsa ya Khristu. Amawalitsa maganizo a ochimwa, kuwatsutsa kuti azindikire kusowa kusowa kusowa kwawo mpulumutsi ndi kuwapatsa moyo watsopano . Pa mfundo ya chipulumutso amakhazikika mwa okhulupirira aliyense kukhala njira ya chitsimikizo, mphamvu ndi nzeru ndipo amaveka okhulupirira aliyense ndi mphatso kukumangirira thupi. M’zimu woyera amatsogolera okhulupirira mu kumvetsetsa malembo. Mphamvu yake ndi ulamuliro zimachitidwa mwa chikhulupiriro, kuzipanga zotheka kuti wokhulupirira akhale m’moyo wa chikhalidwe cha chikhristu bndikubereka chipatso kuulemelero wa Atate.""BAIBULO!2 Timoteo 3:16; 2 Petro 1:21!Chiyambi ( maziko) a chikhulupiriro chathu ndi Baibulo, lapangidwa ndi mabuku 66 a chipangano chakale ndi chatsopano. Timakhulupirira kuti malemba (mau) onse anachokera kwa Mulungu ndi kuti anapatsidwa ku zotengera za anthu osankhika. Lemba limodzinthawi yomweyolimayankhula ndi ulamuliro wa Mulungu ndipo amawonetsera chiyambi, machitidwe ndi chilankhulo cha anthu olemba. Timagwiritsa kuti malemba salakwitsa, ndi opanda cholakwa kuchokera pachiyambi, ndi

�46

Page 47: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

apadera, odzala ndi kukhala ndi ulamulirto omaliza pa nkhani zonse za chikhulupiriro ndi zochita, ndipo palibe zolembedwa zina zofanana mphavu ndi Mulungu.""CHIPULUMUTSO!Aroma 3:23; 5:8; Aefeso 2:1, 8-9!Pachimake pa cholinga cha vumbulutso la Mulungu m’malembo ndi kuitana anthu onse ku chiyanjano cha mwini wake. Olengedwa pachiyambi kukhala m’chiyanjano ndi mulungu, muthu anipisa Mulungu nasankha kuyenda njira yayekha, ndip[o anlekanitsidwa kwa Mulungu navutika pa chivundi cha chibadwidwe, nalephera kukondweretsa Mulungu. Kugwa kwa munthu kunachitika pachiyambi pa mbiri ya munthu, ndipo pakuti wina aliyense wavutika ndi zotsatirazi ndipo akufuna chisomo chopulumutsa cha Mulungu. Chipulumutso cha munthu tsono, ndi ntchito ya thunthu ya chisomo chaulere ya Mulungu, osati zotsatira mu uphumphu kapena gawo la ntchito za munthu kapena ubwino, ndipo zoyenera kulandiridwa mwa chikhulupiriro yense payekha. Pamene Muluingu wayamba ntchito ya chipulumutso mu m’tima wa munthu aliyense, amapereka chitsimikizo m‘mawu ake kuti apitiriza kuwachita mpaka tsiku lake lakukwaniritsidwa.""TSOGOLO LA MUNTHU!1 Atesalonika 4:16-17; Ahebri 9:27!Imfa ikusindikiza tsogolo losatha la munthu aliyense. Pakuti anthu onse, padzakhala kuuka kwa akufa kwa akufa matupi kku dziko lauzimu, ndi chiweruzo chimene chifotokoza zochita za aliyense. Pali kulanga kosatha pa osapulumuka ndi dalitso losatha pa opulumuka onse amene amakhulupirira Khristu adzalandiridwa mu chiyanjano chosatha ndi Mulungu ndipo adzapatsidwa mphoto pa ntchito yomwe anagwira m’moyo.""MPINGO!Machitidwe 2:42; Aroma 12:1-6!Zotsatira za chiyanjano ndi Yesu Khristu ndi choti onse okhulupirira amakhala ziwalo za thupi lake, Mpingo. Pali mpingo umodzi owona dziko lonse, womangidwa ndi onse amene akhulupirira Yesu Khristu ngati mbuye ndi mpulumutsi wawo. Malemba akulamulira okhulupirira kusonkhana pamodzi kudzipereka okha ku kulambira, pemphero, chiphunzitso cha mawu, ubatizo ndi m’gonero monga zoikika zinakhazikitsidwa ndi Yesu Khristu, chiyanjano, kutumikirana ku thupi kudzera mu kutukulana ndi kugwiritsa ntchito maluso ndi mphatso ndi kufikira ku dziko lapansi. Kulikonse anthu a Mulungu akumana pafupipafupi mu kukwera lamuloli, pali kfotokozeka kwa mpingo. Pansi pa chisamaliro cha akuru ndi ma utsogoleri ena,, mamembala ake adzigwira ntchito pamodzi mu chikondi ndi umodzi, chifuniro pa cholinga chokweza Khristu ku ulemelero wa Mulungu ndi kukwaniritsa ntchito yaikulu ya Khristu.""CHIKHULUPIRIRO mdi NTCHITO!1 Akorinto 10:24, 31; 2 Timoteo 3:16-17!Malemba ndi lamulo lomaliza mu ntchito zonse za chikhulupiriro. Tikudziwa kuti sangamange chikumbu mtima cha ena m’madera amene lemba lakhala chete. Komabe, wokhulupirira aliyense ayenera kutsogozedwa m’madera amenewo ndi Ambuye, kwa iye amene ali mdindo.""""

�47

Page 48: 01a-Basic LT PARTICIPANT Manual v2.0 - Chichewa chifupi kwa yesu ndi kwa winw ndi mzake. Tiseka pamodzi, tilira pamodzi pamene tidziturukira Madera a kukula kwa ife eni, kutukura utsogoleri

"""""""""""""""""""""""""""""""""""""

� !STRATEGIC IMPACT!P.O. BOX 830337!

RICHARDSON, TX 75083!WWW.TOUCHINGEVERYNATION.COM!

© Zowonera, Strategic Impact.  Pasakhale kusintha kulikonse kwa bukhuli, "koma mukhoza kukopera mwaulere ndi kugawa osasintha kanthu.""

© Copyright, Strategic Impact.  No changes may be made to this manual, but you"may freely copy and distribute without making changes to content.

�48