cha62-0121m ndipo mbewu yako idzatenga chipata cha mdani …download.branham.org/pdf/cha/cha62-0121m...

46
NDIPO MBEWU Y A KO IDZATENGA CHIPATA CHA MDA NI W AKE Ine, mwachizolowezi, ndachedwa ndi ora kapena awiri. Abusa anaimirira, ndikuti, “Tsopano, ine ndikufuna kuti ndikudzutsireni inu nonse Bambo Branham wobwera mochedwa.” Chabwino, ine ndimakhala ndi zinthu zambiri zoti ndichite kotero i—ine ndimangochedwa apo ndi apo. Koma nthawi iyi ine sindikanatha kuchitira mwina. Izo zinali chifukwa cha nyengo ndi imene yachita izi nthawi iyi. Ine ndikhoza kuzikankhira izo kwa nyengo ndipo nkupulumukapo. Ndachita kuziika izo patsogolo, M’bale Rose, pang’ono pokha. Mmawa wabwino, Mlongo Rose. Ndipo wokondwa kukhala nawo mmawa uno pano, M’bale Rose ndi Mlongo Rose, ndi M’bale Sharritt, ndi abale ambiri, anthu abwino inu kunja uko. 2 Ine ndamva kuti, winawake amandiuza ine, “Pamene ikugwa mvula mu Phoenix, aliyense amangogona,” kusintha koteroko, inu mukudziwa. Limodzi la masiku amenewa ine ndidzadya chakudya chaulere. Iwo amandiuza ine kuti iwe ukhoza kudya chakudya chaulere tsiku lirilonse pamene dzuwa silikuwala. Ine ndiziwona izo lero, ndiwapangitsa iwo kuti alipire zimenezo. 3 Ine ndinali kulankhula usiku wathawu, uko ku mpingo wina. Ine ndithudi sindikukumbukira dzina la iwo. Ndipo kotero ife tinali ndi nthawi yopambana, usiku wathawu, uko ku msonkhano. Ndi uko kwa M’bale Outlaw, ndi uko ku Tempe, ndipo ife timangokhala ndi nthawi yabwino mu chiyanjano ichi. Ndipo ine ndikuyembekeza kuti ndikakomana nawo abale onse otumikira awa ku msonkhano wawukulu, kotero ife tidzakakhala nayo nthawi yomangocheza basi pozungulira, M’bale Rose, ndi kulankhulana wina ndi mzake. Ndipo ndi chimene ine ndabwerera, ndikuti tidzakhale ndi chiyanjano. Ndipo ife tinali…poyang’ana pa zoti tichite ndipo timapeza malo ambiri mbiri. Koma ine ndinaganiza uwu unali mwayi wopambana kwambiri, chifukwa ine ndiyenera—kuti ndidzakomane nawo osiyana siyana, kuti ndidzawawone iwo ndi kudzacheza nawo. 4 Nthawizina polalikira, mtumiki aliyense samamvetsetsedwa, mwanjira ina kapena imzake. Nthawi zambiri, anthu amatenga chinachake chimene iwe wanena ndipo amangokhala ngati… Icho chikatsamira pang’ono kwa iwowo, ndiye iwo akachinena icho mwanjira imeneyo. Ndiyeno winayo akachimva, icho chikhala chikutsamira mopitilira pang’ono. Chinthu choyamba inu mukudziwa, izo zangobalalikiratu.

Upload: others

Post on 05-Sep-2020

0 views

Category:

Documents


0 download

TRANSCRIPT

Page 1: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPOMBEWUYAKO IDZATENGA

CHIPATACHA MDANI WAKE

Ine, mwachizolowezi, ndachedwa ndi ora kapena awiri.Abusa anaimirira, ndikuti, “Tsopano, ine ndikufuna

kuti ndikudzutsireni inu nonse Bambo Branham wobweramochedwa.” Chabwino, ine ndimakhala ndi zinthu zambirizoti ndichite kotero i—ine ndimangochedwa apo ndi apo.Koma nthawi iyi ine sindikanatha kuchitira mwina. Izo zinalichifukwa cha nyengo ndi imene yachita izi nthawi iyi. Inendikhoza kuzikankhira izo kwa nyengo ndipo nkupulumukapo.Ndachita kuziika izo patsogolo, M’bale Rose, pang’ono pokha.Mmawa wabwino, Mlongo Rose. Ndipo wokondwa kukhalanawo mmawa uno pano, M’bale Rose ndi Mlongo Rose, ndiM’bale Sharritt, ndi abale ambiri, anthu abwino inu kunja uko.2 Ine ndamva kuti, winawake amandiuza ine, “Pamene ikugwamvula mu Phoenix, aliyense amangogona,” kusintha koteroko,inu mukudziwa. Limodzi la masiku amenewa ine ndidzadyachakudya chaulere. Iwo amandiuza ine kuti iwe ukhoza kudyachakudya chaulere tsiku lirilonse pamene dzuwa silikuwala. Inendiziwona izo lero, ndiwapangitsa iwo kuti alipire zimenezo.3 Ine ndinali kulankhula usiku wathawu, uko ku mpingowina. Ine ndithudi sindikukumbukira dzina la iwo. Ndipokotero ife tinali ndi nthawi yopambana, usiku wathawu,uko ku msonkhano. Ndi uko kwa M’bale Outlaw, ndi ukoku Tempe, ndipo ife timangokhala ndi nthawi yabwino muchiyanjano ichi. Ndipo ine ndikuyembekeza kuti ndikakomananawo abale onse otumikira awa ku msonkhano wawukulu,kotero ife tidzakakhala nayo nthawi yomangocheza basipozungulira, M’bale Rose, ndi kulankhulana wina ndi mzake.Ndipo ndi chimene ine ndabwerera, ndikuti tidzakhale ndichiyanjano. Ndipo ife tinali…poyang’ana pa zoti tichite ndipotimapeza malo ambiri mbiri. Koma ine ndinaganiza uwu unalimwayi wopambana kwambiri, chifukwa ine ndiyenera—kutindidzakomane nawo osiyana siyana, kuti ndidzawawone iwo ndikudzacheza nawo.4 Nthawizina polalikira,mtumiki aliyense samamvetsetsedwa,mwanjira ina kapena imzake. Nthawi zambiri, anthu amatengachinachake chimene iwe wanena ndipo amangokhala ngati…Icho chikatsamira pang’ono kwa iwowo, ndiye iwo akachinenaicho mwanjira imeneyo. Ndiyeno winayo akachimva, ichochikhala chikutsamira mopitilira pang’ono. Chinthu choyambainu mukudziwa, izo zangobalalikiratu.

Page 2: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

2 MAWU OLANKHULIDWA

5 Ko—kotero ife, nthawi zambiri, polalikira, ine ndimakhalangati ndikunyowetsa zipembedzo ndi mabungwe ndi zinthu.Nthawizina, anthu ndiye amati, “M’bale Branham amatsutsanandi bungwe.” Kumeneko ndi kulakwitsa. Ine sindimatsutsanandi bungwe. Koma ndi nthawi zambiri zimene anthuamangodalira pa bungwe limenelo, inu mukuona, ndiponkumakhazikitsa ziyembekezero zawo zonse pa izo mmalo mwapa Khristu.6 Iwo amafuna kuti awone ndi mamembala angati ameneangawatengere ku bungwe limenelo. Tsopano, zimenezo ndizabwino kwambiri. I—i…Izo nzoona. Ine ndikuganiza kutibungwe lirilonse liyenera kumupeza membala aliyense ameneilo lingathe kumupeza. Zimenezo ndi zabwino kwambiri.Koma pamene inu muyamba kuwatenga osatembenukandi kumakokomeza kwambiri pa izo kuposa momwe inumungamachitire pa kutsindika kwa Mzimu Woyera, mongaM’bale Rose amalankhulira apa kanthawi kapitako, ndi zinthu,ndiye inu—inu mumawapangitsa anthu kumaganiza kuti, “Ifendi a ichi, ndipo ife ndi a icho.” Ngakhale ziri choncho, ife tonsendi a Mulungu. Mukuona?7 Tsopano, ngati ine nditamuwona munthu akuyenda mumtsinje pa ngalawa. Ndipo ine ndimakhala pafupi ndi mtsinjeku Indiana, Mtsinje wa Ohio, ndipo ine ndimakhala pafupikumene ndi mathithi. Awo ndi malo oyipa kwambiri, mathithiamenewo, chifukwa iwo angakuphe iwe mosachedwetsa. Ngatiiwe utapita pa mathithi amenewo, palibepo ngalawa imeneingawakwere iwo, chifukwa iwo, ndi pafupifupi mapazi forte-kapena-fifite molunjika kugwera pansi, ndiyeno pamabwerakupotoloka kwa madzi kwakukulu kuchokera pansi pake,kumene kumakafika mpaka pa thanthwe, thanthwe loyalapamenepo. Ndipo ine ndikuganiza m—m—mafunde, mafundeoyera, amageyedwa kuchokera pansi pa mathithiwo pa usinkhuwa mapazi-forte, mukuona, pamene iwo amakamenya pansi, ndikudzawulukiranso mmwamba kachiwiri. Ndiyeno amangopitaakupidiguka monga choncho, ndipo amapita pansi mu chidzenjechachikulu chimene chiri pafupifupi kuya kwake mapazisikisite kapena sevente. Ndipo mmenemo muli dziwe lamadzi ozungulira limene limawazungulitsira iwo mbali iyi, ndikuwatulutsanso iwo ndi kumapita pansi podzera mkanjirako.Sipangakhalenso njira iliyonse kuti ungakhalenso moyo, inumukuona.8 Bambo wina anapita kumeneko nthawiina kale atavalajaketi ya mmadzi. Iwo anangochiwona chinthucho pameneiye amagweramo, monga choncho. [M’bale Branhamanakhwatchitsa chala chake—Mkonzi.] Ngakhale jaketi yammadziyo, liwilo la madzi lowopsya ilo linangomutengera iyeyopansi. Ndipo sanamupeze konse iye. Sanadziwe nkomwe kutizinamuthera bwanji iyeyo. Iye anakakodwa pa miyala kapena

Page 3: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 3

mmphepete pansi pamenepo, mwinamwake mailosi kapenaawiri kumeneko, monga choncho, ndipo panalibe njira imeneakanapulumukirapo.9 Ndipo ngati ine nditamuwona wina akuyenda mumtsinje mu ngalawa yaing’ono yakale, nditakhala pamenepondikuwerenga, akupita, ndipo ine ndingayambe kumukuwiraiye, “Chokamo mu ngalawa imeneyo. Ngalawa imeneyo siithakukwera mafunde amenewo.” Tsopano, zimenezo sikuti ndirinacho chirichonse chotsutsana naye munthuyo, ngakhalezitakhala kuti ndikuchita kumuzazira iye kuti achokekondi kulankhula mwaukali kwenikweni pa iye. Izo sikutindiri nacho chirichonse chotsutsana naye munthuyo. Inendikumukonda munthuyo, koma ine ndikudziwa kuti iyeakukafa kumeneko. Ndi chifukwa chake ine ndikumukuwira iye.Chifukwa iye siali…Ndi chifukwa chakuti ine ndikumukondaiye, ndi—ndi chifukwa chake ine ndikumukuwira. Ngati inendikadakhala kuti sindikusamala, ine ndikanati, “Chabwino,zake izo,” nkumapitirira, mukuona, ngati ine ndikadakhala kutisindikusamala za iyeyo.10 Koma chifukwa chimene ine ndimanenera zinthu zimenezondi chifukwa chakuti ine ndimakhalawokhudzidwa ndiMpingo.I—ine ndimakhudzidwa nawo Mpingo wa Mulungu. Ndipo i—ine ndimadana nazo kuwuwona Iwo ukungosanduka maganizoa chipembedzo. Ndipo ine ndikukadziwa kachitidwe kameneko,mmenemo ndimomwempingo uliwonse wapitira kumiyala, basimonga chomwecho, basi kudutsa mu kachitidwe komweko kachibungwe.11 Tangoganizani za chitsitsimutso mu nthawi ya Achilutera,taonani kumene icho chinapita. Ndipo mwamsanga pamene ichochifika kumeneko, icho sichimadzukanso nkomwe kachiwiri.Achilutera sanabwererenso. Tayang’anani pa a Methodisti aWesile, sanabwererenso. Tayang’anani pa a Pilgrim Holiness,Nazarenes, ena onse a iwo, Abaptisti, Presbateria. Iwo amatiakakhala ndi chitsitsimutso, ndiyeno munthu wina amawukapondi mphamvu ya Mulungu pa iye, iye amayambitsa chochitikamu Mzimu. Ndiye mwamsanga munthu ameneyo akangopita,ndiye iwo amayambitsa bungwe pa zimenezo.12 Monga Moody Bible Institute, malo abwino, koma iwosadzakhala konse monga momwe ankakhalira ali ndi Moody.Mukuona? Ndipo zinthu zimene Moody ankaima nazo, iwoachokako mamailosi milioni kwa izo, kotero ndi zimenezotupamenepo. Ndipo tsopano zonsezo zangotsala luntha, pameneMoody anali nazo izo mu Mzimu, inu mukuona. Ndipo koteroinu—inumupeza kuti, mu zinthu zimenezo.13 Tsopano, pamene ine ndinkayamba kumene, ndipo inendinadzabwera kuno ku Phoenix, zaka zapitazo, mu kuyendakwa Pentekoste, ndinali nawo mwayi woti ndiyambitse bungwe

Page 4: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

4 MAWU OLANKHULIDWA

inemwini. Abale a Mvula-Yamasika anabwera kwa ine,ndikudzati, “Ndi zimenezotu. Tiyeni tiyambepo. Bwanji, ifetikhala—chikhala chachikulu kuposa zina zonse za izo.”14 Ine ndinati, “Chifundo! Si zimenezo ayi. Chi—chinthuchosi chimenecho, abale. Inu—inu mwasochera mamailosimilioni—mwasochera pa njirayo. Mulungu sachidalitsa konsechimenecho.” Muwerenge mbiriyakale yanu. MuwerengeBaibulo. Sipadzakhala konse bungwe lina limene liti lidzatulukekuchokera mmenemo, limene linabwera kuchokera mu izi.Izo nzoona. Izi zichita bungwe ndipo zipita ku…Izo ziri muchikhalidwe cha Chilaodikaya tsopano. Koma ine ndikukuuzaniinu, m’bale, palibenso mabungwe odalitsidwa ndi Mulunguamene ati awukepo. Sipakhalanso kalikonse ka zimenezi. Ife tiripa Kubwera kwaAmbuye. Mukuona? NdipoMulungu adzatengaotsalira kuchokera mu kuyenda kwakukulu kwa ecumenicaluku, kumene kukuchitika pakali pano, kwa Mkwatibwi, komasipakhala konse kanthu kati kadzachite bungwe, mwauzimu,panonso. Mukuona? Izo zatha.15 Pamene ine ndiwawona abale anga, abale ofunikira,akutsamira mwanjira imeneyo, ndiye ine ndimangozitsanuliraizo ndi zonse zimene ine ndiri nazo. Ndipo nthawizina abaleamati, “Chabwino, M’bale Branham akutsutsana nafe ife.Ndife…” Uko ndi kulakwitsa. Mai! Icho—chimenecho ndichinthu cha patali kwambiri ndi malingaliro anga, kukhalandikutsutsana ndi aliyenseyo. Ndine—ndine wa inu. Ndinem’bale wanu, mukuona, ndipo ndikuyesetsa mwakukhozakwanga. Ndipo ndicho chifukwa ine sindinajowine konsebungwe lirilonse, kuti ine ndizitha kuima pakati ndikuti,“M’bale, musatero. Njira yake si imeneyo.”16 Iwo amati, “Ndife a Assemblies.” Zimenezo ndi zopambana.A Assemblies of God akhala ali mdalitso wopambana kwa ine.“Ndife a Foursquare.” Chabwino, taonani mdalitso umene iwoakhala kwa ine. “Ndife a Jesus Name.” Taonani mdalitso umeneiwo akhala kwa ine. “Ndife amenewo, enawo.” Chirichonsecho,iwo onse ndi mdalitso. Iwowo—iwowo ndi anthu a Mulungu.Mukuona?Ndipo anthu aMulungu akupezekamu zonsezo.17 Ndipo pamene ife tiyamba kumazisonkhanitsa tokha,ndikumati, “Ndife abwinoko pang’ono kuno kuposa a Churchof God,” inu mukuona, kapena, “Ndife abwinoko pang’onokuno kuposa a Foursquare kapena a Jesus’ Name,” kapenachinachake monga choncho. Pamene ndife basi…Ife tikhozakusiyana pang’ono chabe mmalingaliro. Ife tonse tinapitakukadya chakudya chamadzulo lero. Ife tonse timadyachitumbuwa chosiyana, koma ife timadya chitumbuwa basichimodzimodzi, inu mukuona. Lingaliro lake ndi limenelo.Kotero lingaliro la zimenezo, ndi lakuti, ngati—ife tizingokhozakuyang’ana chiyanjano chathucho. Kotero musamatsamire

Page 5: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 5

bungwe. Muzitsamira ku Kalvare. Mukhale akufa kwa zinthuzina izi. Mukuona? Ndipo ine ndikukhulupirira…18 Mundilole ine ndinene izi pamene izo zikadali pa mtimawanga. Ine ndikukhulupirira kuti bungwe lachita gawo labwino.Pakuti, ziripo nthawi zambiri, abale, zoipa basi monga ifezimatinyasira kuti tiziziganizira izo, zakhalapo zinthu zimenezakwawirapo pakati pathu, ndi zinthu monga choncho, zimenezakhala ziri mipatuko. Ndipo anthu amangotenga mipatukoimeneyo ndi kuwabalalitsira nayo anthu mulimonse. Ndipogulu la abale nkuzisonkhanitsa pamodzi amene…kuti ine…Chimene ine ndikutanthauza ndi chakuti kumatuluka mongaiwo ankachitira mu masiku oyambirira ndi mtundu wonse wazinthu. Ndi—ndipo ife tiri nazonso izo mpaka lero, mukuona,basi zikuyendabe. Ndi anthu amene angathe kudzisonkhanitsaokha pamodzi…19 Chithunzi chenicheni cha Pentekoste, mwa kulingalirakwanga, pamene izo zifika ku bungwe, ndi—mpingo, M’balePethrus, mpingo wa Filadelfia ku Sweden. Tsopano, iwosamasamala kuti iwe uli ndi chiphunzitso cha mtundu wanji,bola ngati icho chiri cha Mwamalemba. Ngati iwe ukufunakuti uziziwona izo mwanjira iyi, njira iyo, kapena chirichonse,bola ngati iwe uli ndi chiyanjano ndipo umakhala moyo woyeraweniweni. Ndi zimenezotu pamenepo. Zimenezo ndi zabwino.Ndipo ngati iwe ukufuna kunena kuti Yesu abwera pa kavalowoyera, ndipo winayo ndikumati Iye abwera pamtambowoyera,muzimuyembekezera Iye mwanjira imeneyo. Kazingopitanipatsogolo, bola ngati inu mukukhala moyo wabwino woyerandi kumakhala ndi chiyanjano. Njira yake ndi imeneyo. Ndizimenezotu.20 Icho, chabwino, tsopano, ndicho chifukwa chimodzi,abwenzi, chimene ine ndimakhalira ndi gulu la AmunaAzamalonda awa. Chifukwa, ine ndikudziwa kuti pali zinthuzambiri pamenepo zimene ziyenera kuti ziwongoledwe.Koma ndi—ndi zopambana zimene ife tiri nazo. Eya. Izonzoona. Eya. Pali zinthu zambiri zimene ine ndiyenera kutindizinene. Ndipo—ndipo inu, abale kuno akuuzani inu, inesindimabweza nkomwe nkhonya zirizonse pa iwo. Ine ndirikuno ngati wantchito wa Mulungu, kuti ndidzanene Choonadi.Ndipo ine ndidzayenera kuti ndidzakayankhire chifukwacha zimenezo. Izo nzoona. M’bale Rose anati, “Ndi chifukwachake ife timakukondani inu.” Chabwino, i—izo, chabwino,ife sitingathe…Ife, ife tiyenera basi kuti tizikhala ndi Mawuamenewa. Mukuona?21 Basi nthawi ina kale, ine ndikuganiza, munali inu mu…Inendinali kutsidya kwa nyanja, kapena uko ku chilumba chakachatha, ndipo iwo anali ndi msonkhano, ndipo abale enawoanali akubwekerera mu msonkhano wawukulu uwu kumeneiwo anali ndi amuna azamalonda, ozungulira kumeneko.

Page 6: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

6 MAWU OLANKHULIDWA

Ndipo iwo anali akukambirana, “ine ndinali ndi ka malokakang’ono pangodya. Geni yanga siimayenda bwino. Ndipoine ndinali ndi nthawi yovuta. Ndipo chinthu choyamba inumukudziwa, i—ine ndinabwera kudzamulandira Khristu, ndi—ndipo, o, ine ndinapeza chirichonse tsopano.” Tsopano, zimenezondi zabwino. Ife tikuyamikira zimenezo. Ndi zabwino, komakulemera si nthawizonse kumatanthauza Khristu. Zimenezo,mwaona, ndipo ife timayenera kusamalitsa zimenezo. Tsopano,zimenezo ndi zabwino. Mukuona? I…Sindikutsutsana nazoizo.22 Koma ine ndinakhala ngati ndinawatsatira abale usikuumenewo. Ife tinapita ku motelo kumene—gulu la ife tinalikukhalako, ndi M’bale Shakarian ndi tonse a ife. Ndipo inendinati, “Chabwino,” ine ndinati, “abale, ine ndikuuzani inu.”Ine ndinati, “ine—ine ndikuganiza inu abale ndi gulu labwinokwambiri la amuna limene ine ndinayamba ndakomanapo nalo,mmoyo wanga. Koma,” ine ndinati, “chinthucho ndi chakuti,”ine ndinati…23 Ine sindiri wa bungwe lirilonse, koma ndine wa chiyanjanochimenecho ndi iwo. Ine ndimayenda ndi khadi la chiyanjanondi iwowo, khadi lokhalo limene ine ndiri nalo, chifukwailo limaimira mabungwe onsewa, inu mukuona. Ndipondicho chimene ine ndimachikonda. Ndicho chimene inendikumenyera.24 “Koma,” ine ndinati, “chinthu chimene chikundidandaulitsaine, ndi chakuti abale inu pamaso pa anthu aja kumeneko,amene ali olemera kuchulukitsa chikwi kuposa momwe inumuliri, ndiyeno mumayesera kuwauza iwo kuti Khristu ndichuma. Musamayesere kuti muziwanamiza iwo ndi zimenezo.”Mukuona?25 Musamayesere nkomwe kuti muzidzifanizitsa ndi dzikolapansi. Muzilisiya dzikolo kuti lizibwera kumbali yathu.Musamapite ku mbali yawo. Mukuona? Mukuona? Inumukapita ku mbali yawo, ife sitidzatha kunyezimira nawoiwo. Kuwonjezera apo, Uthenga sumanyezimira; iwo umawala.Hollywood imanyezimira. Uthenga umawala. Pali kusiyanakwakukulu pakati pa kuwala ndi kunyezimira.26 Ndipo kotero, tsopano, ndipo ine ndinati, “Abale oyambiriraa Pentekoste amene anali ndi zinthu, amayesera kumazichotsaizo, ndi kumakawadyetsera nazo osawuka, ndi zina zoteromonga choncho, ndipo amapita opanda kalikonse, mukuona,kuti azikalalikira Uthenga, kuti azikayanjana.” Ine ndinati,“Tsopano ife tikuyesera kumadzibwekerera pa kuchuluka kwazimene ife tiri nazo.” Ine ndinati, “Ndi zosiyana bwanjizimenezo!”27 Ndipo m’bale mmodzi wofunikira, patadutsa mphindipang’ono anaimirira, anati kwa ine, iye anati, “M’bale Branham,

Page 7: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 7

uko kunali kulakwitsa kwakukulu kwambiri kumene anthuanayamba achitapo.”28 Ndipo ine ndinati, “Tsopano, taonani, m’bale, ine sikutindimayesera kukhomerera kuti anthu agulitse zimene iwo alinazo. Koma ine ndikungoyesera kuti ndipange mfundo kwaamuna azamalonda awa.”

Iye anati, “Uko kunali kulakwitsa kwakukulu, anthuwo.”29 Ine ndinati, “Iwo ankachita zimenezo mwa Mzimu Woyera.Mzimu Woyera umawauza iwo kuti azichita zimenezo.” MzimuWoyera ukamuwuza aliyense kuti achite chinachake, inumuchite zimene Iwo ukukuwuzani inu kuti muchite.30 Ndipo iye anati, “Chabwino, uko kunali kulakwitsakoyipisitsa kumenempingo unayambawachitapo.”31 Ine ndinati, “Bwanji, m’bale?” Ndipo pomwe apo pamaso pamunthu yemwe ine ndinali kulankhulana naye.32 Iye anati, “Chifukwa, mwamsanga pamene panaukamkangano pang’ono mu mpingo kumeneko, panalikusagwirizana pakati pa Agriki ndi—ndi Ahebri, ndi zinazotero,” anati, “anthu amenewo analibe malo oti azipitako. Iwoanalibe ngakhale nyumba yoti apiteko.”

Ine ndinati, “Zinali ndendende basi chifuniro chaMulungu.”Iye anati, “Zingatheke bwanji kuti chimenecho chikhale

chifuniro cha Mulungu?”33 Ine ndinati, “Iwo amapita konsekonse, akumwaza Uthenga,chifukwa iwo analibe malo oti apiteko.”34 Mzimu Woyera sumalakwitsa kalikonse. Iwo sumachita basizimenezo. Ndizo zonse. Ndipo monga ine ndinali kulankhulirausiku wathawu, inu muyenera basi kumugwira Mulungu, ndikuwagwira Mawu Ake, ndi kugwiritsitsa basi kwa izo. Ziribekanthu kuti Iwo akukutsogolerani inu kuti, muzingowatsatirabasi Iwo. Kumangopitirirabe monga choncho.35 Koma ndine ndithudi—wothandizira wa chiyanjano chaAmuna Azamalonda ichi. Ndipo msonkhano wawukuluuliwonse umene ine ndingaitanidweko, ine nthawizonsendimapita ndi kukalankhulako, ndimakanenako chirichonsechimene ine ndingathe. Osati kukangoyesera kunenachinachake, chimene chingakamusangalatse winawake,Wakuti-ndi-wakuti. Koma nthawi iliyonse imene ine ndikupita kumsonkhano wanga, ine ndimayesetsa kuti ndiwerenge ndikupemphera ndi kusala kudya, ndikuti, “Ambuye Yesu, kodindinga—ndingakanene chiyani chimene chingakawathandizeanthu amenewo.”36 Aliyense akudziwa kuti sindine mlaliki. Sindinewolankhula. I—ndine…Aliyense amadziwa zimenezo. Sindinemlaliki. U—uthenga wanga ndi wopempherera odwala, ndi

Page 8: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

8 MAWU OLANKHULIDWA

zina zotero monga choncho. Koma, sindine mlaliki. Aliyenseangadziwe zimenezo, amene anandimvapo ine ndikulalikira.Koma zimene ine ndimanena, ine ndimafuna kukhomerera pachimenecho kuti chikachite chinachake.37 Osati kuti muziti, “Kodi iyeyo—si wolalikira wamphamvu?Kodi iye sakugwiritsa ntchito bwino galamala yake? Kodiiyeyo si wodabwitsa paguwa?” Ine sindimafuna zimenezo. I—ine sindingathe kuchita zimenezo. Mulungu sanandiitanire inezimenezo.38 Koma ine ndimayesera kuti ndipeze chinachake chimenechingakamuthandizire munthu ameneyo, ndi mpingo umenewokuti ukhale mpingo wabwinoko, kuwathandizira iwo kutiakakhale anthu abwinoko, kuwupempherera iwo.39 Tsopano, ine ndimakhala ngati ndimalankhula, inendikuganiza, chifukwa ine ndimawawona anthu pang’ono analiakubwerabe mkati, ndipo mvula ikuvumba. Ndi chifukwa chakeine ndimalankhula zinthu zimenezi. Tsopano, kotala pasiti.40 Ndipo tsopano ine ndikufuna kuti ndimuthokoze m’bale.Ine ndamudziwa M’bale Fuller kwa nthawi yaitali, nthawizonsendimamukonda iye, pansi pa mtima wanga. Ndipo ife tirinazo zinthu zambiri zimene timafanana, M’bale Fuller. Ndipokotero ife…ine ndamuwona M’bale Fuller tsopano kwazaka zambiri, ndipo ine ndamudziwa iye kuti ndi mwamunaweniweni wa Mulungu, ndipo ine ndimamukonda iye. Ndipoine ndiri pano mmawa uno kuti ndidzakhale ndi chiyanjano.Ndikupepesa kwambiri kuti ndinaphonya usiku wake pameneizo zinalengezedwa kuno, koma izo zinali chinachake chimeneine sindikadachitira mwina. Ndipo ndine wokondwa kutindiri pano mmawa uno, kuwuwona mpingo wake, wabwino,momwe Mulungu wawatukulira iwo ndi kuwadalitsa iwo. Ndi—ndi chirichonse chimene Iye wamuchitira iye, ine ndithudindikuyamikira zimenezo. Mulungu atapitiriza kumudalitsaiyeyo, ndi kudalitsa kachisi wake, ndi—ndi gulu la matrasti,madikoni, ndi mamembala onse a mpingo. Ndipo mutakula ndikuchita bwino mu chisomo cha Ambuye, ndiro pemphero langalodzichepetsa.41 Tsopano, tisanawayandikire Mawu, tiyeni timuyandikireMlembi, poyamba. Tiyeni tiweramitsemitu yathumphindi chabeku pemphero.42 Pamene ife takhala mwakachetechete tsopano muKukhalapo kwa Mulungu, titaweramitsa mitu yathu ndimitima, kodi chiripo chopempha mu mtima mwanu, chachirichonse chimene inu mukuchisowa, chimene inu mukufunakuti Ambuye apereke kwa inu, kuti ine ndikukumbukireni inumu pemphero langa mmawa uno pano pa tchalitchi? Kodi inumungachidziwitse icho pakukweza dzanja lanu?Mungochisunga

Page 9: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 9

icho mu mtima mwanu, chimene icho chiri. Ambuye akupatseniwina aliyense wa inu chopempha chanucho.43 Atate achisomo ndi oyera, Mulungu, Amene munalengazinthu zonse kudzera mwa Yesu Khristu, kwa ulemereroWake, ife tikubwera mu Kukhalapo Kwanu mmawa uno ndikuthokoza pa mtima wathu. Ndipo monga ife tayendetsakudutsa mu mvula, ndipo mphepo ikuwomba, mvula ikuvumba,ife tikupemphera, Atate Akumwamba, kuti Inumuvumbitsire paife mvula ya Kumwamba, mvula yauzimu, mvula yamasika ndimvula yanyundo, limodzi, mmitima yathu lero.44 Ife tikupemphera, Atate, kuti Inu muwudalitse mpingo uno.Ndife othokoza kwambiri chifukwa cha iwo, chifukwa cham’busa wake, chifukwa cha osonkhana ake, chifukwa cha…malo amene anthu akhoza kukomanapo okhala ndi denga pamutu pawo ndi pokhalapo pabwino pofewa kuti azikhalapo.45 Ife timabwerera mmbuyo mmalingaliro athu ku mbiriyakaleya Mpingo woyambirira uwu, wautumwi, Mpingo wa katolika,ndi kuwona momwe iwo ankakhalira pa masilabu a miyalakapena chirichonse chimene iwo akanakhoza, kuti azimvetseraMawu a Mulungu, ndipo kenako nkudzagwada pansi, ndipokumeneko kukuzizira ndi kwa miyala ndi fumbi, ndipopamenepo amakwezera manja awo moyang’anitsa Kumwambandi kumamva kukoma Kukhalapo kwa Mzimu Woyera.Mumawapatsa iwo kulimbikira koteroko mmoyo wawo mpakaiwo amakhoza kuyenda kupita mdzenje la mikango, samasunthampang’ono pomwe, koma ankamwetulira pa nkhope zawo,akuyang’ana Kumwamba, akudziwa, kuti mu maminitipang’ono, iwo akakhala ali mu Kukhalapo kwa Iye Ameneiwo ankamukonda.46 O, chikhulupiriro cha makolo athu, chikadali moyobe,ngakhale palibepo dzenje,moto ndi lupanga.Mutsitsimutsemwaife, O Ambuye, chikhulupiriro choterocho. Mupereke kwa ifemdalitso wawukuluwa utumwiwaMzimuWoyera.47 Mmodzi aliyense lero amene anakweza mmwamba manjaake, Inu mukudziwa chimene iwo akuchisowa, Ambuye. Inumukudziwa chimene chinali kuseri kwa dzanja limenelo,cholinga ndi chokhumba mu mtima umenewo. Inu nokhamukhoza kupereka chosowa chirichonse, Ambuye. Ndipoine ndikuwapempherera iwo, posadziwa zosowa zawo, komandikupereka pemphero langa ngati chowapemphera iwo. Ngatiwantchito Wanu, ine ndikumupempherera modzipereka winaaliyenseyo, kuti, chirichonse chimene iwo akuchipempha,muloleiwo alandire. Muwadalitse iwo, Atate.48 Ndipo tsopano pamene ife tikuwerenga Mawu Anu,ndi kuphunzitsa kalasi ya Sande Sukulu iyi, monga zinali,mmawawu, ine ndikupemphera kuti Inu muwatenge Mawu awandipo mukung’unulepo kusakhulupirira kulikonse kukuchotsa

Page 10: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

10 MAWU OLANKHULIDWA

pa iwo, Ambuye; kumene, mphamvu iliyonse ya Satanaingayesetse kuti itchinge, zimene zingawalepheretse Iwo kutiakule. Mulole iwo apite mu mtima uliwonse, ndipo mmenemoakakhale mitengo ya chipatso cha chirungamo, Ambuye.Chikhulupiriro, kubereka zimene Inu munawadzozeratuMawu Anu kuti adzachite, munati, “Iwo sadzabwerera kwaIne opanda kanthu, koma Iwo adzakwaniritsa chimene Iwoanakonzedwera.”49 Tsopano, Ambuye, mumuyeretse wantchito Wanu. MawuAnu anayeretsedwa kale. Ndipo, pamodzi, mulole ife tikathekudyetsa nkhosa zimene Mzimu Woyera watipatsa ife—kutitiziphunzitse. Ife tikupemphamuDzina la Yesu. Ameni.50 Tsopano, kwa inu amene mumakonda kuwerenganthawizina, limodzi ndi—Uthenga, i—ine ndikukufunsani inu,ngati inu mungatsegule mu Bukhu. Ndipo ine ndangokhala ndiUthenga wawung’ono wa Sande sukulu, monga choncho, wopitakwa anthu mmawa uno.51 Kodi inu mukukhoza kundimva ine bwino bwino,konse konse, pa malo ponse? Ine ndinasunthira mmwambacholankhulira ichi. Ine ndasasa mawu pang’ono. Ine,mosachedwa pamene ine ndinafika kuno, ine ndinatengachimfine. Mdierekezi anayesetsa mwakukhoza kwake kutiine ndisakhale kuno. Ine sindikudziwa. Ine ndikukhulupirirakuti ndithudi Mulungu atsanulira chinachake chachikulu pamsonkhano wawukulu uno nthawi iyi, chifukwa Satana wachitachirichonse chimene iye akanatha kuti ine ndisakhalepo pano.52 Koma tsopano ife tiwerenga kuchokera mu Genesis, mutuwa 22. Ndipo inu amene mukutsegula mu Baibulo lanu, tiyenitiwerenge gawo la Iwo, limodzi. Genesis 22, tiyeni tiyambire pandime ya 9.

Ndipo iwo anafika kumalo komwe Mulunguanamuuza iye; ndipo Abrahamu anamanga guwakumeneko, ndipo anaika nkhunizo mwa dongosolo,ndipo anammanga Isaki mwana wake, namuika iye paguwa pamwamba pa nkhunizo.

Ndipo Abrahamu anatambasula dzanja lake, ndipoanatenga mpeni kuti amuphe mwana wake.

Ndipo mngelo wa AMBUYE anamuitana iye kuchokerakumwamba ndi kuti, Abrahamu, Abrahamu: ndipo iyeanati, ine ndiri Pano.

Ndipo iye anati, Usaike dzanja lako pa mwanayo,usamchitire iye kanthu kalikonse: chifukwa tsopanoIne ndadziwa kuti iwe umamuwopa Mulungu, powonakuti iwe sunandikanize ine mwana wako, mwana wakoyekhayo.

Page 11: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 11

Ndipo Abrahamu anatukulira mmwamba maso ake,ndipo anayang’ana, ndipo taonani kumbuyo kwakenkhosa ya mphongo itagwidwa mu chiyangoyangondi nyanga zake, kapena ndi nyanga zake, kani:ndipo Abrahamu anapita ndipo anakatenga nkhosayamphongoyo, ndipo anaipereka nsembe pa…anaipereka nsembe yopsyereza mmalo mwa mwanawake.

Ndipo Abrahamu anatcha dzina la malowo Yehova-yire: monga amatchulidwira mpaka tsiku la lero, Muphiri la YEHOVA chidzawoneka.

Ndipo mngelo wa YEHOVA anamuitana Abrahamukuchokera kumwamba kachiwiri,

Ndipo anati, Pa ine ndekha ndalumbira, ateroYEHOVA,…pakuti iwe wachita chinthu ichi, ndiposunandikaniza mwana wako, mwana wako yekhayo:

Kudalitsa ndidzakudalitsa iwe, ndipo kuchurukitsandidzachurukitsa mbewu zako monga nyenyezi za…kumwamba, ndi monga mchenga…m’mphepete mwanyanja; ndipombewu yako idzatenga chipata chamdaniwake;

53 Ine ndikufuna kuti nditenge gawo lomaliza ilo ngati mutu:Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani Wake.Limenelo ndi—lonjezo lopambana.54 Tsopano, ife tonse tikuidziwa nkhani iyi, mwinamwaketaiwerengapo iyo mobwereza, bwereza, nthawi ndi nthawi, zaAbrahamu, ndi momwe Mulungu anamuitanira iye kuchokeraku dziko lake, ndi momwe iye anangokhalira munthu wamba,analibe chapadera. Koma Mulungu anamuitana iye ndipoanamupangira iye lonjezo.55 Tsopano, ine ndikufuna kuti inu muzindikire kuti lonjezoili limene Mulungu anamupangira Abrahamu silinali kwaAbrahamu yekha, koma ilo linali la kwa mbewu yakeya pambuyo pake. Tsopano, anthu ambiri amati, “O, inendikadangokhala ngati Abrahamu, ine ndikanafika pamaloakuti Mulungu ndi kulankhula ndi ine ndi—ndi kundipatsaine chitsimikiziro monga Iye anachitira naye Abrahamu,ndiye bwezi ine. I—ine ndikadakhala nachodi chikhulupiriro,M’bale Branham, ngati ine ndikadangokhala, ngati Mulunguakadalankhula ndi ine monga Iye anachitira ndi Abrahamu.”Koma inu muli nalo lonjezo lomwe lomwelo limene Abrahamuanali nalo, zimenezo ndi pamene, ngati inu muli Mbewu yaAbrahamu.56 Ndiye inu mukuti, “Koma, M’bale Branham, ndine waAmitundu. Ine sindingathe kukhala ndimbewu yaAbrahamu.”

Page 12: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

12 MAWU OLANKHULIDWA

57 Mbewu ya Abrahamu siinali mbewu ya chithupi. Iyoinali Mbewu yauzimu, pakuti mdulidwe wa zimenezo sunalikanthu. Lonjezolo, Iye anachita kumupatsa iye usanachitikemdulidwewo. Koma ilo linaperekedwa kwa iye usanachitikemdulidwe, ndipo izo sizinali chifukwa chakuti iye wadulidwandiye kuti akhala mu pangano ndi Mulungu mwanjiraimeneyo. Zinali chifukwa chakuti Abrahamu anamukhulupiriraMulungu.58 Ndipo Lemba limanena, kuti, “Pamene ife tifa mwa Khristu,ife timadzakhala Mbewu ya Abrahamu.” Paulo amalankhulaza zimenezo, “Ndipo iye amene ali Myuda samakhala Myudakunjaku, koma amakhala Myuda mkati.” Chotero, ngati inumunabadwa ndi Mzimu wa Mulungu, “ndinu Mbewu yaAbrahamu, ndipo ndinu olandira nawo limodzi ndi Abrahamumongamwa lonjezo.”Mukuona? Chotero lonjezo lirilonse limeneMulungu anamupatsa Abrahamu ndi lanu, chifukwa mwauzimundinu Mbewu ya Abrahamu.59 Ndipo ndinu Myuda mochuluka kwambiri kuposa momwemukadakhalira ngati inu mukadabadwira mumagazi Achiyuda,ndiyeno—ndiyeno nkukhala Myuda wa chiorthodox mu mpingoumenewo, ndiponso wokana Mzimu Woyera wofunikirauwu ndi Ambuye Yesu Khristu. Mukuona? Ndinu Myudamochuluka kwambiri, chifukwa inu ndi Myuda amenewabadwa ndi lonjezo lochokera Kumwamba, limene Mulunguanamupatsa Abrahamu, ndipo Abrahamu analilandira ilomwa chikhulupiriro, ndipo ndicho chimene chinamupanga iyechimene iye anali. Kuwonjezera apo, Myuda ndi kudzipatulachabe, ndi kuwolokerako, Mhebri, ndi zina zotero mongachoncho.60 Tsopano, koma pamene inu mwadzipatula nokha kuchokaku zinthu za dziko lapansi, kuwoloka kudutsa mzerewolekanitsa uwo, ndipo inu mukuyenda mu dziko lachirendo,dziko limene inu simunayambe mwakhalamo, pachiyambi, ndianthu amene simunayambe mwayanjanapo nawo pachiyambi,mukatero inu mumadzakhala Myuda wauzimu. Chifukwa,mwanjira yomweyo imene Abrahamu, mwa chikhulupiriro,anachoka ku dziko lake, anawasiya anthu ake, anapita kudziko lachilendo ndi anthu achilendo. Inu mwawasiya anthuanu, mwalisiya dziko mmbuyo, mwawasiya oyanjana nawo anummbuyo, mwawolokerako, kudzera m’Magazi a Yesu Khristu,ndipo ndinu alendo, mukufunafuna Mzinda WowumangaWake ndi Wowupanga ndi Mulungu, monga Abrahamuanali. Amwendamnjira, limodzi ndi Iyeyo, okhala mmahema,matchalitchi, mbadwa limodzi za Ufumu wa Kumwamba,olandira a zinthu zonse kudzera mwa Yesu Khristu. Mukuona?Ife tawolokerako, tadzipatula.61 Tsopano, Abrahamu, lonjezolo linapangidwa kwaAbrahamundi Mbewu yake ya pambuyo pake. Tsopano, Mulungu

Page 13: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 13

anapereka lonjezo ili kwa Abrahamu, kuti Mbewu yake,idzatenga chipata cha mdani wake Iye atatha kumuyesaAbrahamu, kumupima Abrahamu. Tsopano, kuyesedwakokutabwera, ndiye…62 Abrahamu anali atatembenuka kale, ife tingazitchule izo,kuchokera ku chikunja kupita kwa Mulungu. Ndipo atateroMulungu anamupatsa iye, ngati chizindikiro cha MzimuWoyera, mdulidwe. Kenako, utachitika mdulidwewo, ndiyepanadzabwera nthawi yomuyesa.63 Choimira chokongola kwambiri apa cha Mpingo, kuti, ifetitatha kupulumutsidwa, ndiye ife timapatsidwa chisindikizocha mdulidwe wolonjezedwa, umene si wa mnofu, koma waMzimu. Ndipo Mzimu Woyera ndiye mdulidwe wathu. Iwo ndimpeni wakuthwa wa Mulungu. Iwo umalekanitsa ndi kudulamnofu wosafunikirawo, wa chidziko, pa ife. Mawu a Mulungu,akuthwa kuposa lupanga lakuthwa-konsekonse! Kotero, inumukuona, kubwereranso mmbuyo kachiwiri. Mawu a Mulungundi chinthu chimene Mzimu Woyera umachigwiritsa ntchito;osati tizikhulupiriro, osati zipembedzo. Koma Mawu ndi ameneamatilekanitsa ife ku zinthu za dziko lapansi. Iwo amadula ndikuchotsapo malingaliro athu ndi zinthu, ndi kutipatulira ifekwathunthu kwa Mulungu.64 Yesu anati, “Ngati inu mukhala mwa Ine, ndipo Mawu Angamwa inu.” Ndi zimenezotu pamenepo. Ndiye, si mawu anuwo.AmakhalaMawu Ake. Ndiye, inu mukuona, “Ngati inu mukhalamwa Ine, ndi Mawu Anga mwa inu, inu mukhoza kupemphachimene inu mukufuna.” Uh-huh. Mukuona? Chimene ichochiri, inu simukulankhula mawu anu anu. Inu mukulankhulaMawu Ake.65 Kotero ndiye Mzimu Woyera ndi Yekhayo ameneamawatenga Mawu a Mulungu ndi kutilekanitsa ife kutichotsaku zinthu izi za dziko lapansi, mukuona, mdulidwe, kuzidulapo.Zikatero inu mumadutsa nthawi yoyesedwa.66 Tsopano, Abrahamu, iye atatha kuitanidwa atuluke, mdzikola Akaldia, mzinda wa Uri, iye anadzakhala mwendamnjira,mlendo. Kenako Mulungu anadzamuitana iye, iye atathakutsimikiziridwa kuti iye azipitirirabe mtsogolo ndipoazimutenga Mulungu pa Mawu Ake. Atatero, ndiye chimeneMulungu anachita, ndi kumupatsa iye chizindikiro, chakutiIye wamuvomereza iye, ndipo Iye anamuchita mdulidwe iyeyo.Ndipo iye anamuchita mdulidwe Ishmaeli ndi apanyumba akeonse.67 Ndipo tsopano inu muwona, pamene—pamene mwaitanidwakutimutuluke, poyamba inumumadutsammayesero, kuti awonengati inu mutapitiriredi chitsogolo. Ndipo kenako Mulunguamadzakupatsani inuMzimuWoyera, chimene chiri chizindikirochakuti Iye wavomereza chikhulupiriro chanu chimene inu

Page 14: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

14 MAWU OLANKHULIDWA

mukudzinenera kuti muli nacho mwa Iye. Inu mukunditsatiraine tsopano? [Osonkhana akuti, “Ameni.”—Mkonzi.] Iyeavomereza zimenezo.68 Tsopano, ine ndinali kulankhula ndi…Pakhoza kukhalaabale ena opambana a Baptisti akhala pano. Ndipo aliyenseakudziwa kuti ine ndinachokera ku mpingo wa Baptisti. Inendinali kulankhula ndi m’bale wanga wa Baptisti. Ndipoiye anati kwa ine, “M’bale Branham?” Iye anali Dokotalawa Zauzimu, bambo wabwino, Mkhristu weniweni. Iye anati,“Koma, M’bale Branham, kodi inu mumazipeza pati zakutiubatizo wa Mzimu Woyera uwo ndi chirichonse chosiyana ndichikhulupiriro mwa Khristu Yesu?”

Ine ndinati, “Izo ndi zosiyana,m’balewangawofunikira.”69 Iye anati, “Kodi inu simukuganiza kuti pamene iwewalandira Khristu, iwewalandiraMzimuWoyera?”70 Ine ndinati, “Kulondola. Koma,” ine ndinati, “inu mukuona,iwe umakhala ukungovomereza kuti iwe wamulandira Khristu,kufikira Iye atazizindikira zimenezo.”71 Iye anati, “M’bale Branham, Abrahamu anakhulupiriraMulungu, ndipo kunawerengedwa kwa iye kukhalachirungamo.”72 Ine ndinati, “Inde. Koma Mulungu anamupatsa iyechizindikiro, chakuti Iye anali atavomereza chikhulupirirochake, pamene Iye anampatsa iye chisindikizo cha mdulidwe,kuti Iye anali atachizindikira chikhulupiriro chake.” Ameni.73 Tsopano, pamene ife timulandira Khristu ngati Mpulumutsiwathu, ndiye, ngati ife tikhala otsimikizadi mu zimenezo,ndiye Mulungu amatipatsa ife chizindikiro, chakuti Iyewalandira chikhulupiriro chathu mwa Khristu, pakutipatsaife chisindikizo cha mdulidwe, chimene chiri MzimuWoyera. Chimenecho ndicho chisindikizo cha mdulidwe.“Musawukwiyitse ayi Mzimu Woyera wa Mulungu umene inumunasindikizidwa nawo mpaka Tsiku la Chiwombolo chanu.”Osati mpaka ku msonkhano winawo; koma mpaka ku Tsiku laChiwombolo chanu. Izo nzoona, Aefeso 4:30. Tsopano, umo ndimomwe ife timalandirira MzimuWoyera.74 Tsopano, ngati inu mukuti, “O, ndine wokhulupirira,”ndipo Mulungu sanakupatsenibe inu Mzimu Woyera, Iyesanazindikirebe zimenezo. Inu mukungovomereza kuti inumukukhulupirira. Koma pamene kukaikira konseko…Inesindikunena kuti sindinu wokhulupirira tsopano. Mwa kagawokena, inu ndi wokhulupirira.75 Koma pamene Mulungu wapeza chisomo, inu mukapezachisomo ndi Iyeyo, kani, ndipo Iyeyo ndi kukuzindikiraniinu kuti ndinu mwana Wake, ndipo Iye nkumadziwa mtimawanu, ndipo Iye nkumawona kudzipereka kwanu, Iye nkudziwa

Page 15: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 15

kuti zinthu zonse zadulidwapo kuchoka pa inu. ZikateroIye amakusindikizirani inu mu Ufumu wa Mulungu, mwaMzimu Woyera, kutsimikizira kwa dziko lapansi kuti Iyewavomereza chikhulupiriro chimene inu mukudzinenera kutimuli nacho mwa Iye. Mukumvetsa izo tsopano? [Osonkhanaakuti, “Ameni.”—Mkonzi.]76 Tsopano, mwamsanga zikachitika zimenezo, pamabweramayesero. “Mwana aliyense amene amabwera kwa Mulunguamayenera kukwapulidwa poyamba, amayesedwa.”77 Yesu, mwamsanga pamene Iye analandira chidzalo chaMzimu, pa mtsinje, pamene Yohane ankamubatiza Iye, nthawiyomweyo mdierekezi anamutengera Iye waku chipululu, kutiakadutse nthawi ya kuyesedwa. Koma pamene Iye anawatengaMawu a Mulungu ndi kumugonjetsera nawo mdierekezi,“Kwalembedwa. Kwalembedwa,” Iye anabwerera pamenepondiye ali wokonzekera utumiki Wake.78 Ndipo umo ndi mmene Mulungu anachitira ndi Abrahamu.Tsopano, Mulungu, atatha kumuitana iye kuti achoke ku dzikola kwawo, ndipo iye nadzipatula yekha kuchoka ku dziko lake,anthu ake, ndipo atatero Mulungu anamupatsa iye chisindikizocha mdulidwe, kenako anamupatsa iye mwana. Kenako iyeanapita ku yesero lomaliza lija, ndithudi mpaka kudzafika kunthawi imene iye ankayenera kuti akamupereke mwana wakeyemwe Isaki ngati nsembe. Ndipo Iye anati, “Powona kuti iwesunandikanize mwana wako yekhayo, Ine ndikudziwa kuti iweukundikonda Ine.” Iye anamupatsa iye yesero limenelo.79 Ndiye mwamsanga zitachitika zimenezo, nkhondoyoanapambana pamenepo, Iye anati, “Ndipo Mbewu yakoidzatenga chipata cha mdani wake.” Ameni. Ine ndikuzikondazimenezo. “Idzatenga chipata cha mdani wake.” Ife tifika kumfundo yomalizira imeneyo mu mphindi pang’ono chabe,Ambuye akalola. Tsopano Iye anapeza ichi, Abrahamuwokhulupirika. Iye atatha kupeza kuti Abrahamu analiwokhulupirika, kenako Iye anamupatsa iye lonjezo la kutengachipata cha mdani.80 Tsopano pamenepo, nthawi zambiri, ndi pamene ambiri aife a Chipentekoste timapangira kulakwitsa, ndipo timaganiza,“Chabwino, Mzimu Woyera watsanuliridwira pa ine. Ulemererokwa Mulungu! Ndizo zonse zimene ine ndiyenera kuti ndikhalenazo.” Ayi, bwana. Pamenepo inu mukungoyamba kumene. Inu,si pamenepo ayi. Ndi kuyesedwa kwanu ndi kupimidwa kwanu.81 Chimodzimodzi basi monga ife timazipeza mu—mu, chamu—c—Chipangano Chakale; kuyesa, kupima, ndipo kenakokumukhazikitsa mwanayo. Kuikidwa mmalo, kumukhazikitsamwanayo atatha kale kukhala mwana, atabadwira m’banjalo.Iyeyo ndi mwana, kenako iye amayesedwa ndi kupimidwa,ndi kuleredwa ndi aziphunzitsi, ndi kumawona momwe iye

Page 16: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

16 MAWU OLANKHULIDWA

akukulira. Ndipo akatero iye amadzakhazikitsidwa pamaloofanana, pafupifupi, ndi abambo akewo.82 Tsopano ndicho chimene chiri lero. Ife takhala nazopafupifupi zaka forte za kuyesedwa kwa Pentekoste, kapenazopitirira, mwaona, kuwuyesa mpingo, kuwona ngati iwo atiaime, kapena ayi. Kuwona chimene inu…Ndipo, onani, apo ndipamene ine ndikuzipeza izo kachiwiri. Mmalo mogwiritsitsa kumtanda ndi ku Mawu, ndi kumapita chitsogolo, ife timakhalaotengera za dziko lapansi, kumatsikira mbali iyi, kapenakumatsikira mbali iyi, kapena kumatsanzira izi.83 Monga ine nthawizonse ndalankhulira molimba kwambirikutsutsana nawo anthu mu kachitidwe kamakono aka lero,akazi kudula tsitsi lawo, ndi—ndipo amuna kumapitirirandi chirichonse, ndipo basi kumangovala zovala zopandamakhalidwe ndi zinthu. Ine ndimatsutsidwa mochulukakwambiri pa zimenezo. Koma kodi ndi chiyani chimenecho?Ndiko kuyesera kuti ndiwupulumutse mpingo umenewo. Ndikokuyesera kuti ndiwatengere iwo pamwamba apa, afike kuMawua Mulungu, mosalabadira zimene dziko linalo linganene za Iwo.Kukhala ndiMawu aMulungu. Ameni.Mukuona?Mukuona?84 Chinthu chake ndi chakuti, monga momwe ine ndimanenerausiku wathawu, Apentekoste akuyembekezera mphepo yankokomo wamphamvu, koma iwo analephera kuti alimveLiwu laling’ono la kayeziyezi lija. Mukuona? Zimenezo, ndikulakwitsa kuchita zinthu zimenezo. Iwo amaganiza kuti, “Bolangati mphepoyo ili ya nkonkomo, ziri bwino.”85 Koma zimenezo sizinakope tcheru cha mneneri.Mphepo ya nkokomo siinamudandaulitse mneneri Eliya mumphanga. Mabingu amphamvu ndi mphenzi, ndi kuvumbirapansi, sizinamukope konse iye, nkomwe. Koma chimenechinamudodometsa iye chinali liwu laling’ono la kayeziyezilija, chinachake chija chikulankhula mkati. “Mawu anga ndiChoonadi. Mulole mawu a munthu aliyense akhale bodza,ndipo Anga akhale owona.” Ndizo zimene zinamukopa mneneri.Mukuona?86 Ndipo iwo azichitabe zimenezo. Mawu a Mulungunthawizonse amakopa mtima wauzimu umenewo, chifukwaiwo ndi mtima wa Khristu mwa inu, umene umadziwa kutiMawu amenewo ndi owona.87 Ndipo inu mumadutsa mu nthawi yoyesedwa. Mpingoumadutsa mu nthawi yoyesedwa. Munthu aliyense payekhaamadutsa mu nthawi yoyesedwa iye asanatenge konse chipatacha mdani. Abrahamu anadutsa mu imeneyo. Khristu anadutsamu imeneyo. Khristu atatha kudzazidwa ndi Mzimu Woyera,kuja pa mtsinje wa Yorodani, Iye anadutsa mu nthawiyoyesedwa. Abrahamu atatha kuitanidwa kuti atuluke,anakaikidwa mu dziko lake kumene iye anali woti akakhale

Page 17: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 17

mwendamnjira, kenako anamupatsa mdulidwe, ndipo Mulunguamakomana naye iye, nthawi ndi nthawi, komabe iye amayenerakuti adutse nthawi yoti ayesedwe. Mbewu iliyonse ya Abrahamuimachita chinthu chomwe chomwecho, Abrahamu ndi Mbewuyake.88 Bungwe, mpingo, ndi chifukwa chake ife timawapezamabungwe athu akugwera mmphepete mwanjira, ndi chifukwachakuti pamene iwo anafika poti ayesedwe. Yesero lake liti?Mawu a Mulungu. Yesero lake ndi limenelo. Mawu a Mulungundi yesero. Kodi ife tichita zimene gulu la anthu likunena kutitichite, kapena kodi ife tichita zimene Mulungu akunena kutitichite? Kusiyana kwake ndi kumeneko.89 Apo panadzafika, masiku a Dwight Moody, masiku a Finney,Sankey, Knox, Calvin, Spurgeon, onse a iwo, amuna auzimuamenewo, mabungwe anawatsatira iwo. Amakhala nalo gulula amuna kumbuyo uko amene amadulira njira zawo mpakaamakafika ku zimenezo, wina aliyense kumakhulupirira izindi izo, ndi kumawonjezera pang’ono apa, ndi kuchotserapang’ono apo, ndi kuwonjezera pang’ono apa, mpaka potsirizaiwo amapanga bungwe kuchokeramu zimenezo.90 Ndipo pamene iwo atero, wokhulupirira woona weniweni,Mulungu amabwera pamenepo ndi kudzamtenga munthuwina wamng’ono, wodzichepetsa, nkudzachiswa chinthuchimenecho mzidutswa. Kulondola. Nthawizonse amachitazimenezo. Mulungu samasintha. Amangochikhadzulira chinthuchimenecho mzidutswa, anthu ena a malingaliro auzimu ameneangakhale molondola ndi Mawu amenewo.91 Mundirole ine ndikuuzeni inu. Ine ndiri ndi kalatakunyumba, ya chimodzi cha matchalitchi abwino kwambiri,mabungwe aakulu mu kuyenda kwa Chipentekoste. Mkaziwosauka wa mtima-wosweka uyo anandilembera ine kalata.Ndipo iye anati, “M’bale Branham, ine ndinali ndi tsitsi lalitalindipo ndimakhala ndi pafu kumbuyo kwa mutu wanga.” Iyeanati, “Ndipo…Mwamuna wanga ankalikonda ilo.” Ndipo iyeanati, “Ife tinasamuka kuchoka ku mzinda kumene ife tinali nditchalitchi chimene chinali chauzimu kwenikweni, tinapita kutchalitchi chachikulu ichi, tchalitchi choyamba cha mzindawo.”Ndipo anati, “Pamene ife tinafika kumeneko, alongo onseAchipentekoste anali atadula tsitsi lawo.” Ndipo anati, “Iwoanayamba kumandipanikiza ine chifukwa cha ilo. Ine ndinati,‘Ayi, ayi. Ine ndimakhulupirira kuti Baibulo limanena kutiife tisamachite zimenezo; ndi chamanyazi kuchita zimenezo.’”Ndipo kotero iye anangonena, “Ndipo iwo anapitirirabe…Iwo amakhoza kumamuseka iye, ndikuti, ‘Heyi, ta—tayara lanulikuphwa mmbuyomo, la sipeyalo,’ ndi zonse monga choncho.Ndipo anayamba kumawapanikiza amuna anga, mwanjiraimeneyo, mpaka iwo anandikakamiza ine kuti ndidule tsitsi

Page 18: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

18 MAWU OLANKHULIDWA

langa.” Ndipo anati, “ine ndakhala wotsutsika, chichitirenizimenezo.”92 Taganizani za zimenezo, mpingo wa Chipentekoste umeneuyenera kuti uziima ndi Mawu a Mulungu! Ndiko kumenebungwe lanu likukutengeraniko inu. Kulondola. Iwo akulepherakuti amvetsere Liwu laling’ono lija la Mawu a kayeziyezi,limene limawaitanira iwo ku choonadi. Iwo onse akumvetseramphepo za nkokomo wamphamvu, ndi kufuula kwambirindi kuvina, nkumanena kuti ali nayo mphamvu. Zimenezondi zabwino. Ine ndimakhulupirira mu zimenezo, inenso.Koma, m’bale, pamene iwe ungathe kuvina ndi kufuula, ndipokenako ndi kupotoloka ndi kuwakana Mawu a Mulungu,ndi kumakhala moyo monga dziko lapansi, pali chinachakecholakwika penapake. Kulondola.93 Mzimu wa Mulungu umatsika, Liwu laling’ono la kayeziyezilija, ndipo umakulondolerani inu molunjika waku Kalvare,kumene ife timakafa, ndipo moyo wathu umabisika mwaMulungu podzera mwa Khristu, ndi kusindikizidwa ndi MzimuWoyera. Zikatero, Mawu amenewo okha amakhala mmenemo.“Ndiye ngati inu mukhala mwa Ine, ndipo Mawu Angankukhala mwa inu, mupemphe chimene inu mungafune ndipochidzaperekedwa kwa inu.”Kusiyana kwake ndi kumeneko.94 Ine ndikuyembekeza kuti ine sindikuwoneka kwa inungati wotentheka. Ngati ine ndiri choncho, ndine—ndine—inesindikudziwa zimenezo. I—ine ndimakhulupirira kuti Mawu aMulungu ali Choonadi, ndipo Iwo ayenera kuti azikhala pomweapa. Ndipo ngati Iwo akukhala apa, Iwowo azidziwonetseraOkha kunjaku. Iwo ayenera kutero! Moyo wanu, mapangidweanu onsewo, adzakhala osiyana.95 Kotero pamene Mulungu anamupatsa Abrahamu yesero, iyeanadutsamo, handiredi peresenti. Ndipo akana…96 Mulungu sangathe kulipatsa bungwe yesero, chifukwa ilolonse ndi losokonezeka. Mulungu samachita mwanjira imeneyondi bungwe. Iye samachita ndi mafuko mwa anthu a Amitundu.“Iye anawatenga anthu kuchokera mwa Amitundu.” Israeli, Iyeanatenga fuko. Koma, mwa Amitundu, “Iye anatenga anthukuchokera mwa Amitundu chifukwa cha Dzina Lake.” Kotero,inu mukuona, zimenezo si bung-…Zimenezo si bungwe. Ndimunthu payekha amene Iye akumutenga kuchokera mwaAmitundu.97 Ndipo pamene yesero libwera, inu mukuwona zimenezimachitika? Ife tinadutsa mu kulungamitsidwa. Ife tinalandiraubatizo wa Mzimu Woyera mu kuyenda kwa pentekoste.Koma pamene zinadzafika ku nthawi ya kuyesedwa, tinatengaophunzira opukutidwa, tikufuna kuti tikhale monga dzikolapansi, chimodzimodzi basi monga izo zinali mu masiku azochitika za Wesile ndi ena onse a iwo. Iwo amapita ku sukulu.

Page 19: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 19

I—iwo amakaphunzira sayansi. Ndipo iwo amakaphunziramtundu wonse uwu wa zinthu zimene zimayendera limodzindi maphunziro. Ndipo iwo amayesera kuti aziphunzirakuwerenga maganizo. “Chinthu chopambana basi, chabwino,musanene izi. Muwasiye iwo achite izi ndi izo. Chifukwaizo zidzatero…” Mukuona, inu mukudziwunjikira ndipomukumanga. Chokhumba chanu—cha—chanu ndi cholakwika.Cholinga chanu ndi cholakwika. Inu mukumangira kwabungwe mmalo momangira kwa Kalvare. Inu mungathe bwanjikumangira kwaKalvare, nkusabwera podzeramnjira yaMawu?98 “Pakuti ife timachapidwa ndi madzi a Mawu.” “Inumukakhala mwa Ine ndi Mawu Anga akakhala mwa inu, ndiyemupemphe chimene inu mukuchifuna.”99 Apo ndi pamene ife tikuwona kugonjetsedwa kwa kuyendakwa Chipentekoste, chifukwa chakuti iwo anachokako kuMawu. Mawu akanena chinthu china; iwo amayesera kutialipange bungwe limenelo libwere mmenemo penapake. Ndipoiwo amachokako ku Mawu amenewo, ndipo nkumatsatirabungwelo. Ndipo inu mukuona kumene izo zapita? Izo zafikapofanana pafupifupi ndi matchalitchi onsewo. Komano ifetimavina ndi kufuula, ndi kumalankhula mmalirime, ndikumalumpha-lumpha, zimenezo ndi zabwino. Bungwe lawolondi labwino. Ine ndikuyembekeza kuti mwandimvetsa. Komachinthucho ndi chakuti, Liwu laling’ono la Mawu lija lakayeziyezi likulankhulabe. Ndi zimenezotu.100 Inu muzidutsa nkuyesedwa. Mulungu azikuyesani inumonga Iye anachitira ndi Abrahamu. Iye amaziyesa Mbewuza Abrahamu, za pambuyo pake. Ndipo tsopano, chifukwachimene ife sitikutengera chipata cha mdani, chifukwa chimenepali zochuluka kwambiri pakati pathu, ndi chifukwa chakutiife sitikutha kuima nako kuyesedwako. Ndipo mundilole inendikuuzeni inu chinachake, kuyesa kwaMawundi kolondola.101 Chifukwa chimene ife sitikukhalira nazo, ndipo ifesitidzakhala nazo nkomwe…mu bungwe. Ine ndikuganiza kutiChipentekoste chiri nalo bungwe lina labwino. Ena a amunaabwino kwambiri amene ine…alipo…akukhala pa nkhope yadziko lapansi, ali kumeneko—mabungwe amenewo.102 Assemblies of God, ine ndiri nawo azimzanga kumeneko.Mai! M’bale komwe uko ku Indiana, ine ndikupita, kutindikakhale ndi msonkhano, ine ndikukhulupirira, uko, kutaliuko. M’bale Roy Weed, iyeyo ndi mkulu wa boma wa mzindawa Indiana. Ine ndikukhulupirira kuti iyeyo ndi munthuwaumulungu. Komabe, iyeyo ndi mkulu wa bomalo waAssemblies of God.103 Foursquare, oh, mai, angati! Ralph McPherson ndi ambiri aabale amenewo, amene ali amuna aumulungu, palibe kalikonsepa miyoyo yawo. Iwowo ndi amuna abwino.

Page 20: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

20 MAWU OLANKHULIDWA

104 Uko kwa a Oneness, chimene iwo amadzitchulaokha, Oneness. Kapena, tsopano, ine sindikuganiza…Iwo amachitchula icho Jesus Name church. Jack Moore,ndikungotchula mmodzi mwa…Alipo mazana a iwo, amunaabwino, amuna abwino, amuna aumulungu.105 Koma chinthucho ndi chakuti, m’bale, ndi ichi, pameneinu mudzipachika kwa bungwe limenelo. Mukuona? Mulunguamatengamabungwe amenewo, ndipo—ndipo limodzi lirilonselondi lakugwa. Tayang’anani pa iwo, chidziko chikukwawiramo.Tayang’anani pa akazi awo. Tayang’anani pa amuna awo.Tayang’anani pa zikhalidwe zawo. Ine ndikhoza kukulozeraniinu, anthu a Assemblies of God amene ali ndi madikonimu bodi mwawo, amene akwatirapo kawiri kapena katatu,alaliki ongotengeka. Akazi okhala ndi tsitsi lodula, kumavalaakabudula, ozipentapenta, ndipo ndi kumadzinenerabe kuti alinawo Mzimu Woyera, kumadalira pa umboni wa kulankhulammalirime, kapena kulumpha-lumpha, kapena kufuula.106 Iwo akulilephera Liwu laling’ono la kayeziyezi lija la Mawu.Mawu amenewo amakuyendetsani inu bwino bwino mpaka kumtanda. Ndi kumene izo ziri. Ndi chifukwa chake ife tiribeaneneri enieni mumpingo lero, monga Agabasi.107 Ndi chifukwa chake, mpingo lero, i—iwo salemekezankomwe kulankhula mmalirime pamene wina akulankhula,chifukwa iwo amva zochuluka kwambiri zabodza ndi zotengeka,mpaka iwo sakudziwa chimene chiri cholondola ndi cholakwikamu zimenezo.108 Kutanthauzira kongokhala zosokonezeka basi, winawakeamangonena zinazake basi chifukwa chakuti iye akumvererakutsogozedwa. Kumeneko si kutanthauzira. Kutanthauzira; siwinawake kuimirira ndi kulankhula mmalirime, wina ndikuimirira mu maminiti pang’ono ndi kutanthauzira zimeneiye wanena. Pamene wina akulankhula, winayo amakhalaakutanthauzira pomwe apo, kumanena mawu pa mawu,kulankhula mofanana, chirichonse chimodzimodzi. Munthu uyuakhoza kukhala kuti akulosera, koma iko si kutanthauzira. Enaa iwo, liwu la mtundu uwu kumalankhula chinachake, uyukumbuyo kuno kumalankhula chinachake. Ndipo wina kunenamawu teni, wina kunena mawu fifite motsatira zimenezo, akutikutanthauzira.109 Kutanthauzira kumatanthauza “kunena, mawu-pa-mawu.”Ngati izo ziri Mawu a Mulungu, izo ziyenera kubwera, mawu pamawu; mzere pa mzere, mzere pa mzere. Umo ndi momweMawuayenera kumabwerera.110 Koma kodi ife tawona chiyani? Zonamizira zambiri! Ndipoiwo amachita zimenezo, ndi cholinga, mmalo moti azikhala ndiMawu, iwo aziika izo pamenepo. Mwamsanga pamene munthu

Page 21: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 21

achita zimenezo, iwo amamutcha iye wa Chipentekoste. Ndipoinu mukudziwa zimene zimachitika.111 Pamene mayesero abwera, nthawi yoyesedwa, ndiye Mbewuimayambapo, izo zimawonetsera imene ili Mbewu ndi imenesiili. Tsopano, mosalabadira zimene zinachitika, Abrahamuanakhala ndi Mawu, lonjezo.112 Koma lero bungwe silingathe kuchita zimenezo. Ndipo enaa inu abale ofunikira amene muli a mabungwe amenewo, inumukatsutsana nawo iwo kamodzi, iwe umadziwa kumene iweukupita. Ndi angati a inu?113 Ine sindikunena, mchipinda chino tsopano, koma ndi angatiakhalapo mu kuphunzitsa kwanga, ndi angati akhalapo ndiine, ndikuti, “M’bale Branham, ife tikudziwa kuti zimenezo ndiChoonadi. Koma ife tikathamangitsidwa kuno, kodi ife tichitachiyani?”114 M’bale, kodi ife tichita chiyani? Mukangamire kuKalvare, mukangamire ku lonjezolo, mukangamire ku mtanda,mulimonsemo.115 Ndipo kumeneko, iwo ali nawo ena a anthu abwinokwambiri. Mukuona? Koma chimene ine ndikuyesera kutindichite, ndi kunena kuti, zimenezo zidzayenera kulephera.Izo nthawizonse zakhala zikulephera ndipo nthawizonsezizilephera. Komano, kaya inumwamulepheraMulungu, kapenaayi, zisunganibe Mawu a Mulungu ndi lonjezo Lake, poyamba.Inu muziyesedwa ndi Iwowo.116 Inu mudzasaina zipepala, zakuti muchita izi kapenamuchita izo. Ngakhale zotsutsana ndi Mawu, inu mudzasainabezimenezo. Izo nzoona. Mu mtima mwanu, inu nkumadziwa kutindi zolakwika. Zimenezo ndi Liwu laling’ono la kayeziyezi lijalikulankhula, Mawu amenewo. Nzosadabwitsa ife tikulepherakuti tisunthire patsogolo, chifukwa chinachake chachitika.Inu munazichotsa nokha kwa Liwu laling’ono la kayeziyezilija. Inu mwathamanga mwaliwiro kwambiri. Mulunguanali kukuitanani inu, koma inu munathamanga kwambiri,chifukwa mabingu anabangula, mphenzi zinang’anima, mapirianagwedezeka.117 Izo sizinamusunthe nkomwe Eliya, mneneri uja. Iyeankafuna Liwu lija, poyamba. Iye anati, “Ine ndikhalabe pomwepano.”118 Ambiri lero, anayambitsa, misonkhano ya machiritso,kutsanzira kwa chithupithupi, mitundu yonse ya zinthu, ndizogirigisha zimene sizimawoneka nkomwemuMawu aMulungu.Izo nzoona. Ndi chiyani chimenecho? Ife tiyenera kuti tiimbenyimbo ija, “Iwo amene adikirira pa Ambuye. Mundirole inendidzichepetse kunyada kwanga ndipo ndiitanire pa DzinaLanu. Mundirole ine ndidikirire, Ambuye, kufikira ine ndimveLiwu laling’ono la kayeziyezi lija.” Ndipo Liwu limenelo

Page 22: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

22 MAWU OLANKHULIDWA

lidzakhala Liwu la Mwamalemba. Ilo lidzalankhula ndendendendi Mawu. Ameni. Chabwino.119 Tinampeza, Abrahamu iye atatha kuikidwapo, ataitanidwaatuluke, atalekanitsidwa kwa okondedwa ake, kwa banjalake, kuchoka kwawo, kwa mtundu wake, kupita ku dzikolachirendo. Mwa chikhulupiriro iye anachita zimenezo. Ndiye,chifukwa chakuti iye anachita zimenezo, Mulungu anamupatsaiye mdulidwe, pofuna kutsimikizira kuti iye anali mwanawamwamuna wa Mulungu, kuti iye amakhulupirira mwa Iyechifukwa iye anali kukhulupirira lonjezo. Komabe, iye samatha,iye samaziwona izo mwachithupi, koma iye amavomereza kuti,“Chirichonse chotsutsana ndi Mawu a Mulungu chinali bodza.”Ziribe kanthu kuti kaya pabwera umboni wochuluka bwanji,icho ndi bodzabe.120 Ine ndimadana nazo kunena izi, koma ine ndiyenera kutinditero. Taonani. Ndipo inu mukawatenga akazi, ine ndinenaizi chifukwa cha chinthu chimodzi chimene chiri chowoneka,mukhoza kuchiwona, amene amadzinenera kuti ali nawoMzimuWoyera, ndipo nkusakhala nalo khalidwe mokwanira kuti—kuti alisiye tsitsi lawo lizikula, pali chinachake cholakwikapenapake. Mkazi amene angavale chovala chimene chiri chamwamuna, ndi kuchivala icho, pamene Baibulo limanena kuti,“Ndi chonyansa kwa—kwa Mulungu, kuti mkazi avale chovalacha mwamuna.” Ndiyeno inu kumadzinenera kuti muli nawoMzimuWoyera ndi kumachita zimenezo?121 Ine ndinalankhulapo pa zimenezo tsiku lina ku Oregon. Ukokunali mkazi wina amene anandilembera ine kalata yaikulukwambiri. Iye anati, “M’bale Branham, inu muli ndi utumikiwabwino, koma inu ndithudi mukuwuwononga iwo.” Iye anati,“Tsopano, nanga bwanji…” Anati, “ine ndimavala ovololonthawi zonse.” Anati, “Nanga bwanji ndikamapita kumundakuti ndikathyole zina—za kumunda zina, ndipo nditavala diresi.Kodi inu simukuganiza kuti zingawoneke bwino kwambirinditavala ovololo kusiyana ndi momwe zingakhalire, kapenangoleka, chirichonsecho chimene chiri, kusiyana nditavaladiresi?” Ndipo anati, “Taonani, ine ndimakwera mmapiri ndianyamata pamene iwo akupita kuti akadyetse ng’ombe, ndipo,”anati, “ine ndimakafika ku malo audzudzu.” Anati, “Tsopano,ndipo—nditavala diresi, iwo ungandilumeko ine. Ndikavalaovololo iwo sumandivutitsa ine.”122 Ine ndinati, “Zimenezo ndi zopyapyala kuposa nsuzi wamthunzi wa nkhuku imene yafa chifukwa cha njala. Chifundo!Izo ziribe Mawu amodzi a Mulungu pa izo. Amenewo ndimaganizo anu anu.”123 Mulungu anati, “Mulole mawu aliwonse akhale bodza,ndipo Ake akhale owona.” Akazi anga amavala diresi. Iwoamakathyola kumunda. Iwo samakhala ndi vuto ndi zimenezo.

Page 23: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 23

Ndipo, komanso, mkaziyo alibe ntchito iliyonse kumakakhalandi gulu la amuna kunja uko, odyetsa ng’ombe, mulimonse.Iye ayenera kuti azikhala ku khitchini ndi kumene iye ayenerakumakhalako. Izo nzoona.124 Iwo akungoyesera kuti apeze chowiringula, koma palibepochirichonse. Mawu a Mulungu ndi achimvekere, ndipomkazi amene wabadwa ndi Mzimu wa Mulungu adzatero.Ndipo mwamuna amene wabadwa ndi Mzimu wa Mulungusangamulole mkazi wake kuti azichita monga choncho. KodiIye anati chiyani? “Iye amene atenga, ndi kudula tsitsi lake,anyozetsa mutu wake.” Ndipo mwamuna wake ndiye mutuwake. Iyeyo ndi wonyozetsa.125 Ine kulibwino ndikhale chete. Chabwino. Tsopano, mwaona,mwaona, zimenezo zakwanira. Inu mukudziwa zimene inendikunena.126 Ine sindikunena zimenezo chifukwa cha nkhwizi. Ngati inendikunena zimenezo chifukwa cha nkhwizi, Mulungu achitirechifundo mtima wanga wochimwa; andilole ine ndipite pansi paguwa ili, ndikalape.127 Ine ndikunena izi chifukwa, abwenzi, ine ndimakukondaniinu. Ndipo ine ndikuyesera kuti ndikuuzeni inu chimene chirichoonadi, ndipo zimenezo ndi Mawu a Mulungu. Ife tiyenerakumvetsera Liwu laling’ono la Mulungu lija, kuti zizikwaniranandiMawu. Ife tikudutsa nthawi ya kuyesedwa. Aleluya!128 Kodi inu munazindikira kuti nthawi yoyesedwayo ikatiyabwera, kuphunzitsa kwa mwana kuja amene anabadwiramu banja la chipembedzo? Ngati iye ayima nako kuyesedwakondipo nkukhalabe ndi chokhumba cha abambo ake, zikateromwana ameneyo amachotsedwapo ndipo amakavekedwachovala, ndiyeno pamakhala mwambo umene umanenedwa.Ndipo mwana ameneyo amakaikidwa ndiye m’banja limene iyeanabadwiramo.129 Ndiro limene liri vuto ndi Achipentekoste athu lero. Iwoamangolumpha apa ndi apo, ndipo mabungwe athu amakhozakuwakokera iwo mbali iyi ndi mbali iyo. Iwo sakumakhalandi Mawu.130 Ngati inu mutakhala ndi Mawu, ndiye Mulungu,akamayang’ana, “Ngati inu mukhala mwa Ine, ndi Mawu Angamwa inu,” Ake, Iye sangathe kuwakana Iwo. Amenewo ndiMawu Ake. Ndiye idzakhalapo nthawi, nthawi inayake, pameneinu muti mudzatengedwere panja ndi kudzaikidwa pambali, ndikudzapatsidwa chinachake chimene chiri chenicheni, aleluya,mphamvu yaMulunguWamphamvuzonse.131 Chimene, Mulungu akuyembekezera ana Ake, koma iwoakulephera basi kuti afole, pamene iwo afika pa nthawi iyoyakuti ayesedwe. Kodi inu muvomereza zimenezo? “Chabwino,mpingo undichotsa ine.” Chabwino. Ndi zimenezotu. Ndiye,

Page 24: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

24 MAWU OLANKHULIDWA

kazipitani. Imeneyo si Mbewu ya Abrahamu. Mbewu yaAbrahamu siimachita monga choncho.132 Mbewu ya Abrahamu! Tsopano, ine sindikusamala zotsutsazimene zinabwera kwa Abrahamu, iye anakhalabe molondolandi Mawu a lonjezo amenewo, amangokhala molondolandi zimenezo. Zinalibe kanthu momwe Sarah amabwerera,enawo amabwerera, ena osiyanasiyanawo, chirichonse, iyeamaziwerengera izo ngati kuti panalibepo. Iye amayang’ana,iye amakhulupirira kuti iye adzakhoza kudzaliwona lonjezolo,chifukwa Mulungu anali atalonjeza izo kwa iye, ndipo izozinali zonse zimene zinalipo kwa izo. Amenewo anali Mawua Mulungu, anakhaladi mwa iye.133 Kenako Iye anamupatsa yesero lomaliza lija. “Inendimupatsa iye magawo awiri, ndipo ndimuyesa iye.” Tsopano,iye walandira kale mwanayo. Iye akuwona kuti iye ali nayemwanayo. “Koma tsopano Ine ndimuuza iye, ‘Umutengeremwana ameneyo uko ndipo ukamuphe iye.’ Ndipo akamusiyemwanayo, pamene iye akawona…Kodi iye amupha mwanaameneyo? Ine ndimuyesa iye tsopano.”134 Abrahamu, woona kuMawu!Motani, pamene iwe walandiralonjezo, iwe ungathe bwanji kuchiimitsa chinthucho? Motani,ungachite motani?135 “Iwe ukuyembekeza kuti udzakhala motani tate wa mafuko,ndipo apa iwe uli usinkhu wa zaka handiredi ndi fifitinizakubadwa tsopano? Abra-…Isaki wamng’ono, pafupifupiusinkhu wa zaka fortini, fifitini. Iwe udzakhala motani tatewa mafuko pamene ndiwe wa usinkhu wa zaka handiredi ndififitini? Mwana wako yekhayo ndi uyu, ndipo iwe ukuwonongaumboni wakowokhawo umene iwe uli nawo.” Ameni.136 “Ine zindithera bwanji ngati ine ndichokamo mu bungwelanga? Ine zindithera bwanji ine ndikachita izi?” O, mvetseraniku Liwu laling’ono la kayeziyezi ilo ndipo mubwere kuMawu, Mawu.137 Inu mukuti, “ine ndinamva liwu likundiuza ine izi.” Ngatiizo ziri zotsutsana ndiMawu, izo sizinali Liwu laMulungu. Liwula Mulungu limabwera ku Mawu.138 Ndiye Abrahamu anayenda kumapita ku Liwu limenelo,ndipo Liwu, laling’ono la kayeziyezi la Mulungu, amapita kuMawu a Mulungu, ayenera kuti akachotse moyo wa mwanawake yemwe.139 Iye anati, “Letsa dzanja lako, Abrahamu. Ine ndikudziwakuti iwe umandikonda Ine tsopano. Ndipo onse apambuyo pako,aleluya, onse okutsatira iweyo, amene ali ololera kuti atengeMawu Anga, iwowo adzakhala Mbewu yako, ndipo kumenekoiye adzatenga chipata cha mdani.”

Page 25: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 25

140 Ndikukhumba ine ndikanakhala nayo nthawi kutindikuuzeni inu chinachake chimene chinachitika masikupang’ono apitawo,mukuona, za zimene zinachitika. O,mai!141 “Idzatenga chipata cha mdani; Mbewu yako ya pambuyopako. Abrahamu, amene adalitsa iwe adzadalitsidwa, ndipoamene adzatemberera iwe adzatembereredwa.” Yesu anati,“Zikanakhala bwino ngati mphero ikanamangiriridwa pa khosipako, ndi kumizidwamu kuya kwa nyanja.”142 Ndipo mabungwe awa amene amawakana amunaaumulungu awo, chifukwa chakuti iwo aima ndi Choonadi,Mawu, ndi Mzimu ndi mphamvu ya Mulungu, ndipo amakhalandi Mawu, inumukuona zimene zimachitika? Iwo amaponyedwamnyanja ya kuiwala.143 “Kukanakhala bwino ngati mphero ikanamangiriridwapakhosi pako, ndi kumizidwa mkuya kwa nyanja, kusiyanandikuti ukhumudwitse wochepetsetsa wa odzozedwa Awa.”Kodi iwowo ndi ndani? Mbewu ya Abrahamu yokhala ndi Mawua lonjezo.144 Ina ya mipingo yathu ikufika pa malo okana. Iyo ikukanamachiritso Auzimu. Iwo sakuwafuna iwo mu tchalitchi chawopanonso. Uko nkulondola. Mabungwe athu Achipentekostesakufunanso machiritso Auzimu. Ndi chiyani chimenecho? Kodiinu simukuwona momwe mdierekezi wagwirira ntchito? Iyewapita kumeneko ndipo wakanenako zinthu zina zabodzakumeneko monga choncho. Ndipo anthu aluntha basikumaganiza kuti iwowo ndi auzimu, ndi kumayang’anapa izo, ndikuti, “Tamuwonani uyo. Tamuwonani uyo.” Inesindikuyang’ana pa zimenezo.145 Ngati iwe uli Mbewu ya Abrahamu, iwe uziyang’ana palonjezo la Mulungu, zimene Mulungu ananena kuti uzidzachitandi zimenezo. Ndi zimenezotu. Mbewu ya Abrahamu, ifetimayang’ana pa lonjezo. Ine ndiribe nazo kanthu kuti ndiangati akugwera mbali iyi ndipo ndi angati akugwera mbali iyo.Lonjezolo likukhalabe loona.146 Inu muyenera kudutsa mayesero amenewo. Mukuona?Inde. Abrahamu, poyamba anayesedwa, ndipo kenakoanasindikizidwa, mtsogolomo anadzapatsidwa lonjezo lakuti“Mbewu yake iyenera kutenga chipata cha mdani.” Inendikuzikonda zimenezo. Ndiye, iwo anatenga zipata za mdaniwawo iwo atatha kuyesedwa.147 Chinthu chake ndi chakuti, ife tikulephera kuti tipambanemayesero. Ndi chifukwa chake mabungwe athu akulephera kutiapambanemayesero. Izo si chifuniro chaMulungu. Izo, Mulunguwazidalitsa izo, koma izo si chifuniro cha Mulungu. Chifukwa,mukuona, inu muli nalo gulu lonse la amuna apa amene alindi magulu onse a malingaliro, ndipo iwo amawakokera iwopamodzi ndi kutulukapo ndi zopambana zimene iwo angathe.

Page 26: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

26 MAWU OLANKHULIDWA

Ena a iwo amati, “Uyu ndi munthu wachikulire. Inu simungathekutsutsa zolankhula zake.” Chabwino, ndi njira yomweyoimene mpingo wa Katolika unachitira bungwe, chinthu chomwechomwecho, pa gulu la okhulupirira aluntha. Aluntha, iwoamayang’ana pa icho, nkuchifanizitsa icho ndi nthawi. Inusimungachite zimenezo. China chirichonsecho ndi bodza komaMawu a Mulungu.148 Abrahamu samayang’ana konse pa chinthu china komalonjezo la Mulungu. Mosalabadira chimene izo zinali, iyeanakhala nalo lonjezo la Mulungu.149 Ndiye ndicho chifukwa chake ife sitikumapeza zochuluka.Bungwe silingathe kutenga chipata cha mdani. Muli malingaliroambiri opusa mmenemo.150 Ziyenera kutengera munthu payekha, amene akutengachipata cha mdani. Inu mukhoza kuchita zimenezo ngati inumukufuna kutero. Inde, bwana.151 Tiyeni tiyesere pang’ono, kwa maminiti pang’ono, tiwonengati iwo akukhala mu Lemba.152 Tsopano, inalipo nthawi uko ku Babeloni pamene ukokunali—kunaimikidwa fano, choimira chokongola cha mpingowa Katolika, ndipo onse amene samagwadira fano limeneloamawotchedwa mu ng’anjo ya moto. Tsopano, icho chinalichiwonetsero, chakuti kodi iwo atsalira, pamene Mulunguanati, “Inu simudzakhala nayo milungu ina pambali pa Ine,kapena kupanga fano lina la chirichonse.” Ndi zimene Mulunguananena. Chiwonetsero chinabwera.153 Israeli yense anagwadira pomwepo. Ndipo pamene lipengalinawomba, ndi—ndipo azeze atawomba, ndi—ndipo chitolirochitawomba, bwanji, iwo onse anagwadira fano ili.154 Koma analipo atatu a iwo amene anati, “Sizingathekekuchita zimenezo.” Iwo anamva Liwu laling’ono la kayeziyezilija, ndipo iwo anakhala mumzere ndi Mawu. Kodi iwo anachitachiyani? Anakhala nawo Mawu.155 Ndipo atatha, i—i—iwo anati, “Ngati inu simuchitazimenezo…Ife tikupatsani inu mwayi wina, kapena ifetikuponyerani inu mu ng’anjo ya moto.”156 Anati, “Mulungu wathu ndi wokhoza kutiwombola ifeku ng’anjo ya moto imeneyo.” [Malo osajambulidwa patepi—Mkonzi.] “Koma, ngakhale ziri chomwecho, ife tikhalabendi Mawu.”157 Tsopano, m’bale, nanga bwanji inu? “Kodi ine ndichitechiyani, M’bale Branham?” Mukhale ndi Mawu. Mukhale ndilonjezo. “Mpingo wanga wonse undichokera ine.” Mukhale ndilonjezo. Iwo ayenera kuzimirira, adzangochokapo tsiku lina,mulimonse. Koma, Mulungu sangatero. Mukhale ndi lonjezo.“Chabwino, ine ndikukuuzani inu, iwo andithamangitsapo ine.”

Page 27: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 27

Mukhale ndi lonjezo, chimodzimodzi basi. Inu mungokhalabasi ndi lonjezolo. Tsopano, ngati inu mungathe kukhala ndilonjezolo ndi kukhala pamenepo, ndiyemukhale nawo iwowo.158 Muzikhala pa chiyanjano ndi aliyense. Koma tsopanoapa, tsopano, inu simudzatha konse kupambana mwanjiraina iliyonse pambali pa kukhala pa chiyanjano ndi aliyense.Inu muyenera kutero. Tsopano, pamene iwo ayipa kwambiri,iwowommakhalidwe, ndiyemukhale kutali ndi zimenezo. Ndikokulondola. Musamafike ku dera la mdani. Koma bola ngatiinu mukuyesera kuti mumpindule m’bale wanuyo, zimenezo ndizosiyana. Mukuona?159 Tsopano penyani. Koma inu simungathe konse kuligonjetsalingaliro la bungwe, munthu mmodzi. Ayi, bwana. Pamene,iwo akhazikitsa kachitidwe kawo, “Ife timakhulupirira izi,fulusitopu!” Ngati inu mukanamalemba chiphunzitso chanuchomwakuti, “Ife timakhulupirira izi,” komaa, izo zingakhalezosiyana. Fulusitopu amatanthauza kuti, “Ife timakhulupiriraizi, ndipo inu muyenera kuti mubwere ku izi ndi kudzasainapepala ili, kapena ndizo zonse za izo.”160 Koma ngati inu mutamanena kuti, “Ife timakhulupirira izi,”komaa, “kuwonjezera zonse zimene ife tingaphunzire kuchokerakwa Mulungu. Ndife otseguka kwa Mzimu Woyera,” ndiyekuti inu mukupitirira, m’bale. Inde. Zimenezo zikhala zosiyanatsopano.161 Koma, inu mukuona, ngati inu mwazilemba izo ndifulusitopu, ndipo Mulungu akakupatsani chinachake chimzake,icho nkutsimikizika kuti ndi Mawu Ake, Choonadi, inusimungathe kusuntha, chifukwa munaikapo “fulusitopu.” Iyoikuthetsa zimenezo. Ndi pamene Achilutera anafera. Ndipamene Amethodisti anafera. Ndi pamene Abaptisti anafera.Ndi pamene Apuresbateria anafera. Ndipo apo ndi pameneApentekoste akufera. Ndiko kulondola. Ndiko kulondola.Iwo akufera pomwe apo, tangoyang’anani, chifukwa ndi—izozinalembedwa kale. Palibepo kanthu kamene inu—inumungathekuwonjezerapo kwa izo kapena kuchotserapo kwa izo. I—izo ziripamenepo. Chimenecho ndi chiphunzitso chanu.162 Achilutera sakanatha kuvomereza kuyeretsedwa. Ayi,bwana. Iye anali atanena kale kuti, “Olungama adzakhalamoyo mwa chikhulupiriro.” Osati Marteni Lutera; koma gulu ilolimene linkamutsatira iye. Izo nzoona.163 Osati John Wesley; koma gulu limene linkamutsatira iye.Ndiko kulondola.

Osati Calvin; koma gulu limene linkamutsatira iye.164 Osati John Smith wa mpingo wa Baptisti, ameneanapemphera mwamphamvu kwambiri, nthawi ya usiku,mpaka maso ake anatupa nkutsekeka, kupempherera mpingowake; ndipo mkazi wake amachita kumamutsogolera iye ndi

Page 28: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

28 MAWU OLANKHULIDWA

kumamudyetsa iye ndi supuni, pa tebulo. Osati iyeyo; komagulu ili la Abaptisti amene akumutsatira iye, bungwe limenelinabwera pambuyo pa iyeyo.

Osati Alexander Campbell; koma iwo amene anamutsatiraiye.165 Osati kuyenda kwa chipentekoste pachiyambi, amene analinazo zinthu zonse mofanana, ndipo ankayanjana ndi aliyense;koma magulu amene anadzabwera ndikumadzanena kuti, “Ayi.Ndife ichi, ndipo ndife ichi. Ndipo zinkhani zake ndi izi, ndipondi zimenezo!” (“Amadzipatula okha, zimachita kuwoneka kutianalibe Chikhulupiriro.”) Kulondola. Ndi chimene chinachitazimenezo. Ndi chimenecho chinthu choipacho. Ameni. Inendikumverera mwachipembedzo, mmawa uno.166 Ana a Chihebri, atatha kuima ndi mayesero, kuti kodi iwoaima ndi mawu a lonjezo, kapena ayi, iwo anaikidwa pa yesero.Ndipo kodi iwo anachita chiyani? Iwo anatenga chipata chamdani. Ameni. Bwanji? Iwo anakhala paMawu.

Muzikhala ndi Mawu, Liwu la Mulungu lija limenelimalankhula ndi inu.167 Tsopano, maganizo onse anati, “Tsopano, taonani. Babeloni,izo sizikhala zosiyana ayi. Chifukwa, ife, pamene ife tizigwadirafano ili, ife tikhala kuti tikumupembedza Mulungu, mulimonse.Chabwino, ngati ife titachite izi mwanjira iyi, ife tikhala kutitikutanthauza izo mwanjira iyi.”

Muchite izo momweMulungu ananenera.168 Nanga bwanji ngati Mulungu anati, “Mose, vula nsapatozako, Mose. Iwe uli pa malo oyera.”169 Iye nkuti, “Zikomo Inu, Ambuye. Ine ndithudindimakukhulupirirani Inu. Ine ndingovula chipewa changa,mmalo mwake. Ndi zotangwanitsa kwambiri kuti ndivulezingwe za nsapato zanga.” Uh-huh. Huh! Izo sizikanagwirantchito.

Iye anati, “Nsapato.” Iye sananene kuti “chipewa.”Kulondola.170 Inu muyenera kubwera, mzere pa mzere, zimene Mulunguakunena, ndipomukhale pamzere ndiMawuAke.171 Tsopano, iwo atatha kukhala ndi yeserolo, iwo anatengachipata cha mdani cha moto. Iwo anadzapeza, pamene iwoanapita mpaka kumathero, akukhalabe ndi Mawu a Mulungu,iwo anatenga chipata. Izo ndi zoona. Atatha…172 Daniele. Panali kulengeza kumene kumapita, ndikusainidwa ndi a Medi-o-Persia, kumene sikukanathakusinthidwa, konena kuti, “Ngati wina apemphera kwamulungu wina aliyense, iyeyo aponyedwe mu dzenje lamikango.” Ndipo Daniele ankadziwa kuti Mawu a Mulungu

Page 29: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 29

anali, akuti azipemphera kwa Iye yekha, kotero iyeanangotsegula mazenera ndi kumapemphera mulimonse.Tsopano, iye sanapite pobisika. Iye anatsegula mazenerankuyang’ana cha ku kachisi. Iye sanachite nazo manyazizimenezo.173 Ndipo ife sitimafuna kuchita chipembedzo chathuLamlungu, ndipo Lolemba ndi kuchita chinachake. Kapena,kukhulupirira mu mtima mwathu chinthu china, kubwerapamaso pa winawake ndikuzati, “Chabwino, ine sindikudziwa.Eya, ine ndikuganiza inu mukulondola.” Muzikhala chimeneinu muli. Ngati simuli, chokanipo pa guwapo, muchokemo mutchalitchimo. Izo nzoona. Chifukwa, ndinu chobwerekera kwazonse ziwirizo. Mukhale chimene inu muli. Muzinena zimeneinu mumakhulupirira, mukatero inu simukhala nacho chotichizikubwezani mmbuyo. Inu mukungoima ndendende ndichimene chiri choona. Aliyense nkumadziwa manga manga anu.Anthu adzakuyamikirani inu, munthu aliyense.174 Mkazi akhoza kukhala wosawoneka bwino monga enaonse amene timawawonawa. Iye akhoza kukhala wamkulu,wonenepa, wamng’ono, wowonda, wamutu-wakuda, wa maso abulauni, wa maso a buluu, wa maso otuwa; lina, mbali ina, ndilina mbali ina. Koma ngati mkazi ameneyo ali woyera, dona,palibepo mwamuna mu dziko koma amene angavulire chipewachake kwa iwo, iyeyo ali ndi umunthu mwa iye. Kulondola.Chifukwa, i—iye akuwonetsera chimene iye ali, ndipo anthuamayamikira zimenezo.175 Chomwechonso Mulungu angayamikire munthu ameneangakhale chimene iye ali, kapena amuna amene amadzineneraChikhristu. Tiyeni tikhale Mkhristu, wodzazidwa ndi MzimuWoyera, wokhala ndi Mawu a Mulungu, kapena tiiwaleza zimenezo. Kulondola. Chifukwa, ngati si choncho, inumungokhala wachinyengo, ndi kumakhala moyo wosiyana.Ndipo anthu azikuwonani inu mukuthamangira ukokokavina, ndi kumakasuta, ndi zinthu monga choncho, ndiponkumadzinenera kuti ndinu Mkhristu, ndiye, mukuona, inumukuika chokhumudwitsa mu njira ya ena.176 Kukuwonani akazi inu, nthawizina, momwe iwo amaduliratsitsi lawo ndi kuvala ndi kumachita atavala madiresi aang’onoakale awa, kumawoneka ngati kanyimbi wosendedwa kapenachinachake, ndi kumapita uko pa msewu, kumakayendayenda,zitendene pafupifupi kutalika choncho, kumazivinitsa mumsewu. Kodi chimenecho ndi chipentekoste? Ndiye—mipingoinayo kumanena kuti, “Iwo amadzinenera kuti ali nachochinachake chimene iwo alibe.”177 Inu munasindikizidwa ndipo munaikidwa chilembo ndiMzimu Woyera. Inu simuli mu holo ya dansi usikuuno ndipomutakumbatiridwa mmanja mwa mwamuna wina, yemwe si

Page 30: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

30 MAWU OLANKHULIDWA

mwamuna wanu; usiku winawo, ndi kubwereranso ku tchalitchindi kudzavina pa malo ponsepo. Chimenecho si chipentekoste.Chimenecho ndi chinyengo. Zimenezo ndi nyansi.178 Ine sindikunena mochuluka kwambiri izo kwa inu. Koma,inu mukuzindikira, matepi awa amene amapangidwa panoamapita pa dziko lonse, kotero ine ndikungolalikira ngati kutindi za kwa dziko lonse. Pamene ine ndikumverera Mulunguakuti, “Nena chinachake,” ine ndimangonena icho, chifukwaine sindimadziwa kumene izo zikupita. Zimenezo ziri ndi Iyekuti azisamalire zimenezo. Muzingokhala ndi Mawu. Ndikokulondola. Chabwino.179 Ayi, Daniele sibwenzi atagwadira kwa zonena zawo, kayaiye atulutsidwa mu bungwe lawo kapena ayi. Iye anangokhalapa zenera pomwepo, ndipo anakhala ndi Mawu a Mulungu. Iyesankachita manyazi ndi Iwo.180 Chinachitika ndi chiyani? Iwo anamuponyera iye mu dzenjela mikango, koma iye anatenga zipata za dzenje la mikango.Bwanji? Ulemerero! Chifukwa chakuti Mulungu anati yake…“Mbewu yako idzatenga chipata cha mdani.” Kaya mdaniyo ndindani, inu mwatenga chipata. O, ndi nthawi zingati zimene ifetikana…?181 Tayang’anani pa Mose, akutsatira mu mzere wa malamuloa Mulungu, anapita ku Igupto, zinkawoneka ngati chirichonsechinali mosiyana. Iye anali ndi otsanzira ena amene anapita nayeiye. Iye anapita uko ndi—zizindikiro zingapo, kuti akasonyezekuti iye anali atatumidwa. Anaponyera pansi njoka, ndi zinazotero monga choncho.182 Ndipo apa panabwera otsanzira pomwepo, anaponyera zawopansi. Kodi iye akanachita chiyani? Palibe. Mulungu sanamuuzekonse iye kuti iwo akanadzachita zimenezo. Iye ankafuna kutiamuyese Mose. Iye anali Mmodzi Amene anawaloleza Ayanendi Ayambre kuti aponyere pansi njoka zawo, kapena ndodozawozo.183 Kotero apo panaima Mose ali pa mzere wa ntchito.Anaponyera pansi ndodo yake. Iyo inasanduka njoka. Iye anati,“Tawona zimenezo, Farao. Ndi zimene Ambuye wanga wandiuzaine kuti ndibwere, ndidzachite pamaso pako.”184 Farao anati, “Bwerani kuno, Ayambre ndi Ayane.” Iwoanaponyera ndodo zawo pansi. Izo zinasanduka njoka, zimeneMose anachita.185 Kodi nkhope yake inafiira? Ayi, bwana. Iyeanakhulupirirabe kuti Mulungu anamutuma iye. Iye anakhalanalo lonjezo limenelo. Ndipo chinachitika ndi chiyani?186 Ndi pamene inu mukhala pamaso pa ina ya misonkhanoyanu. Nkhope yanu ikhoza kufiira, pang’ono pokha. Mukhalendi Mawu.

Page 31: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 31

187 Chinachitika ndi chiyani? Nthawi yomweyo, mamba yaikuluiyi ya Mose inabwera pamenepo ndipo inadzazimedza zimenezo.Mulungu anatsimikizira. Atatha mayesero ake, iye anati,“ine ndikufuna iwe, mwa chizindikiro ichi, kuti uwalole anaamenewo azipita. Ine ndikufuna kuti iwe uwatumize iwo azipitakwawo, kumene iwo ayenera kukakhalako. Mulungu anabwerakuno kudzanena, wandituma ine kuno kuti ndidzawatulutseiwo. Ine ndikufuna kuti iwo azipita kwawo.” Iye anaiponyera iyopansi pamenepo.188 O, mayesero anabwera. Mose, kodi iwe uchita chiyani,utembenukapo, ndi kuchokapo, ndikuti, “Chabwino, inemwinamwake ndalakwitsa”? Ayi, bwana.

Mose anaima pomwepo, “Mulungu anamutuma zimenezi.”Ulemerero!189 Mulungu akalankhula chirichonse, mukhale nacho Icho.Ziribe kanthu kuti kukuchitika chiani, mukhale nacho Icho.Ngati iwo akutulutsanimo inu ndikuti, “Ife sitingagwire nanuntchito, sitichita izi,” mukhale nacho Icho.190 Mose anakhala nachobe icho. Chinachitika ndi chiyani?Iye anatenga chipata cha mdani wake. Aleluya. Mdierekezianati, “ine ndiifunyulula Nyanja Yakufa patsogolo panu,” komaiyo inatseguka. Iwo sakanatha kuwasungabe iwo mu Iguptokenanso. Iye anatenga chipata cha mdani. Bwanji? Chifukwaiye anakhala ndi kutuma kumene Mulungu anamupatsa iye.Malamulo a Mulungu, iye anakhala ndi Mawu a Mulungu ndipoiye anatenga zipata za mdani.191 Yoswa, atatha kudutsa mayesero. Iye anali ali kumeneko,mwinamwake, ndipo anasambira powoloka Yorodani, iyeyo ndiKalebu, ali ndi azondi. Pamene iye amabwerera kuchokera kuYorodani, iwo anakafika ku Kadeshi-Barnea. Ndipo onse a iwoanati, “O, ngati ife tiyamba, zimenezo ziswa mabungwe athumzidutswa. Ife sitingathe basi kuti tipite kumeneko.”192 Mzimu umenewo siumafa. “O, ife sitingathe kukhala nazoZimenezo. Ngati ife titaphunzitsa Zimenezo kwa anthu athu,kodi ife tichita chiyani? Ife ndithudi tingawatulutsire pafupifupitheka lamadikoni, mu tchalitchimo, panja. Iwowo anakwatirapokawiri, katatu. Kodi ife tichita chiyani? Ife, bwanji, ngatiife titawauza akazi athu kuti azikhala ndi tsitsi lalitali, inumukudziwa zimene iwo angachite? Iwo achisiya tchalitchicho.Ndipo kodi ife tichita chiyani? Bwanji, ife tingatengedwe basingati ndife akachitidwe kachikale.” Yesu anali wa kachitidwekachikale, nayenso. “Ife sitingathe kuchita zimenezo. Ifesitingathe kuchita zimenezo. Zimenezo zatikulira ife.”193 Inu mukudziwa kumene wokhulupirira wa mmalireamakafika. Ahebri, mutu wa 6, amafotokoza zimenezo. “Iyeamene anayamba wawunikiridwapo, anapangidwapo kukhalaotenga nawombali ndi MzimuWoyera, kenako nkugwera kwina,

Page 32: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

32 MAWU OLANKHULIDWA

kuti adzikonzere iyemwini kachiwiri.” Iye anafika pa mzerewa mmalirewo ndipo anakana kuti awoloke, ndi zimenezotu,anakana kuti akhulupirire kwathunthu.194 Chifukwa, kodi Kalebu anachita chiyani? Kodi Yoswaanachita chiyani? Iye anati, “Ife tiri oposa agonjetsi kuchita izo.”Bwanji? Iwo anakhala ndi chimeneMulungu analonjeza.195 Bwanji, iwo anati, iwo enawo anati, “Chabwino, iwowo ndizimphona. Iwo onse ali mkati mwamakoma. Iwowo alimwakuti.Bwanji, ife sitingathe kuwakhudza iwo,mwanjira iliyonse.”196 Yoswa anati, “Ndife oposa agonjetsi kuchita izo. Khalanichete, anthunu!Musalankhule! Khalani pansi!” Ameni.197 Ine ndikukuuzani inu, chikhulupiriro chimakhala muchinthu chachikulu champhamvu, izo zikakhala za Mawu aMulungu. Iye samachita mantha pamenepo. Chikhulupirirochimakhala ndi ubweya pa chidali, akatumba aakulu. Ichochimati, “Khala chete!” China chirichonse chimathamangirapa ngodya, ndiko kulondola, pamene Mulungu alankhula. “Inumukakhala mwa Ine, ndi Mawu Anga mwa inu, munenechimene inu mukufuna.” Ndi zimenezotu. O, ine ndimakondazimenezo. Hum!

Adierekezi adzanjenjemera, ndipo ochimwaadzadzuka;

Chikhulupiriro mwa Yehova chidzagwedezachirichonsecho.

198 Iwe ungakhale nacho bwanji chikhulupiriro pamene iweukudziwa kuti sukugwira ntchito, sukuyenda mu Mawu Ake,pamene iwe ukudziwa kuti pali zinthu pamenepo zimene iweuyenera kuti uzinene ndipo iwe sukuzinena izo? Pali zinthupamenepo zimene iwe uyenera kuti uziphunzitse ndipo iwesukuphunzitsa izo. Pali zinthu pamenepo zimene iwe sukuthakuzinena, ndipo iwe ungakhale nacho bwanji chikhulupiriropamene iwe ukudziwa kuti ukulakwitsa?199 “Ngati mtima wathu sukutitsutsa ife.” Ndi zimenezotu.Ndi zimenezotu. Koma mukhale ndi Mawu amenewo, pamenepalibe chirichonse chikutsutsidwa. “Palibe kutsutsika kwa iwoamene ali mwa Khristu Yesu, amene samayenda monga mwathupi koma monga mwa Mzimu.” Mzimu umatsogolera ndiMawu, chifukwa Mzimu ungakhoze kokha kutuluka kuchokeramu Mawu, chifukwa Mawu Ake ndi Mzimu. Ndipo Iwoumakhoza kokha…Mzimu weniweni wa Mulungu umakhozakokha kulankhulaMawu aMulungu. O, mai!Mai, mai!

Pita kutali, dziko. Satana, tisiye ife.200 Musamachite mantha kunena kwa phiri ili, “Suntha.”Muzinena izo. Muzikhala pamenepo, nkuliwona ilolikuphwanyika. Ndiko kulondola.

Page 33: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 33

201 Koma kodi inu muli ndi kutsutsika kulikonse mmenemo, inubola—bolamungokhala chete. Inumukungobwebweta ndiye. Inusimukunena zoona. Inu simukunena zinthu zimene inumuyenerakunena. Chabwino.202 Ife tikupeza ndiye kuti Yoswa, iye atatha kudutsammayeseroamenewo, iye anawona umboni wa dziko labwinolo, ndipo iyeanaima pamenepo pa Kadeshi-Barnea ndipo anawadandauliraonse a iwo, ndipo anati, “Ndife oposa agonjetsi kulitenga ilo. Ifetitha kulitenga ilo.”Kodi lingalilolo linali chiyani? Awoloke.203 Kodi lingaliro la Mose linali chiyani? “Kasonyezechizindikiro ichi ndipo ukawatulutseko anawo.” Ndipozinkawoneka ngati zikulephera. Koma iye anakhala ndi Mawu,ndipo chipata cha Nyanja ya Kufa sichikanatha kumugwira iye.Iye anadutsabe zimenezo. Iye anatenga chipata chamdani.204 Yoswa, akuyang’ana pa lonjezo la Mulungu, anati, “Ndifeoposa agonjetsi kulitenga ilo.” Izo nzoona. Ndipo pameneiye anadzafika ku Yorodani, kodi iyo inachita chiyani? Iyoinapereka njira. Ameni. Ndi zimenezotu. Iye anatenga chipatacha mdani. Yorodani ameneyo anali kumutchinga iye kutiasawoloke ndi kukatenga lonjezo limenelo. Koma pamene iyeanakafika kumeneko, iye anali Mbewu ya Abrahamu. Bwanji?Iye anakhulupirira Mawu a Mulungu. Ndiyo njira yokhayoimene inu mungathe kukhalira Mbewu ya Abrahamu, ndipakukhulupirira Mawu a Mulungu. Ndiyeno kodi iye anachitachiyani pamene iye anadzafika uko pamene iye anali atakonzekakuti amutenge mdani? Mulungu anatsegula chipatacho, ndipoiye anachitenga icho, anachitenga icho, anapita nacho.205 Pamene nkhondo yoyamba, kulimbana kwake koyambakumene iye anali nako ndi iwo, makomawo anali aakulu zediiwo ankakhoza kuchita mjaha pamwamba pa iwo. Iye alowamobwanji kuti akawapeze iwo? Iwo anamuthawa iye, anabwereramkatimo. Mdani adzateroso, aponso. “Koma inu mudzatengachipata cha mdani.”206 Anati, “Ambuye, kodi ine ndichite chiyani?” Iyeanayendayenda, madzulo ena, akusinkhasinkha. Iyeanamuwona Munthu ataima ali ndi lupanga Lake atalisolola.Yoswa anasolola lupanga lake, anati, “Kodi Ndiwe wa ife? KodiNdiwe wa mdani wathu?”

Iye anati, “Ndine Kapitao wa khamu ili.”“Kodi ine ndichite chiani?”

207 “Mugube kuzungulira pamenepo, ka satini. Mudzawombelipenga. Inu mutenga chipata cha mdani.”208 Ilo linagwa pansi. Inde, bwana. Bwanji? Iye anali Mbewuya Abrahamu, imene inasunga Mawu a Mulungu. Iye anatengachipata chirichonse chimene chinabwera kwa iye. Ndithudi.

Tayamba kuchedwa. Ine ndiyenera kuti ndichokepo.

Page 34: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

34 MAWU OLANKHULIDWA

209 Taonani, ngwazi zonse zofunikira izi, ndiri ndi tsambalozadza ndi izo ndalemba apa. Koma ngwazi zonse zofunikiraizi, zinthu zimene iwo anachita, iwo potsiriza anafa.210 Koma mtsogolomo panadzabwera Mbewu yeniyeni yachikhulupiriro, Mbewu Yachifumu ya Abrahamu, Yesu, lonjezo.Abrahamu anali ndi Isaki, woona, wa thupi, koma Mbewuyeniyeni siinali mu kachitidwe ka bungwe limenelo. Iyo inali mulonjezo ilo la Mawu a Mulungu, kuti Iye adzamupanga iye tatewamafuko, osati kudzeramwa Isaki, koma kudzeramwaMbewuYachifumu, Yesu. Imeneyo inali Mbewu Yachifumu, imene,kwenikweni,Mbewu yaAbrahamu. Yesu sanaliMyuda, komansoIye sanaliWamitundu. Iye analiMulungu.Mukuona? A…211 Inu Akatolika apa, adalitse mtima wanu. Koma pamene inumumupembedza Maria ngati mulungu wamkazi, vuto lanu ndichiyani, mulimonse? Maria sanali china koma mkazi. Mulunguanamusankha iye. Iye anali chotengera. Ndi zokhazo basi.Chotengera, ndi chimene mkazi ali, koma iyeyo amakhudzidwandi mbewu ya mwamuna.212 Koma, ndife gulu losakanizikana, koma ine ndiyenera kutindinene izi kuchitira kuti inu mukhoze kumvetsa zimene inendikuzikamba. Tsopano, inu mumamvetsera kwa—adokotalaanu, ndipo ndinem’bale wanu. Ndithudi, inumukhoza.213 Maria analibe umuna mwa Khristu. Panalibepo kumvererakwa kugonana pamene Mzimu Woyera unadzamufungatiraiye, ayi nkomwe. Koma Mulungu Wamphamvuzonse, Mlengi,analenga khungu la Magazi ndi umuna. Hum! Ngati ukanakhalaumunawochokera kwaMaria, ndiye kuti akufa sadzauka.

Ulemelero! Zimenezo zangobwera mwatsopano. Inendazigwira kumene zimenezo.214 Ndiye ngati inu mukunena kuti palibepo kusiyana, zimeneife tikuchitazi, ndiye nchifukwa chiyani Mulungu anatiuza ifekuti tizipewa zoipa? Nchifukwa chiyani Mulungu anadzutsathupi la Yesu, ngati izo siziri chomwecho? Kotero, inu mukuona,sipangakhale mkazi kuti anali ndi chochita mu zimenezo. Ngatizinachitikadi, ndiye kuti thupi Lake linali la amayi Ake, Maria,chifukwa iye anali nako kugonana pa kufungatiridwa ndimzimuumene unamupangitsa iye kuti—kuti atulutse umuna, ndipouko nkulakwitsa. Mzimu Woyera, mwa kutenga mimba kwachiyero, aleluya, pamenepo Iye analenga umuna uwiri wonse wamwamuna ndi wamkazi.215 Kodi Yesu ankamutcha iye “amayi”? Mufufuze zimenezo muLemba. Iye anamutcha iye “mkazi.” Aleluya! Mkazi! (Zimenezondi zatsopano. Ndi chifukwa chake izo zikuchita momweizo zikuchitiramu.) “Mkazi, taona mwana wako.” Mamailosimillioni kuyandikira kwa iye kuposamomwe Iye analiri.216 Iye anali Mulungu. Iye sanali Myuda kapena Wamitundu.Iye anali Mulungu, zonse mnofu ndi thupi, Mulungu akukhala

Page 35: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 35

mwa Iye. Mulungu kukhala mu umuna wa mkazi? Sakanakhozakuchita zimenezo. Umuna wa mkazi ukanakhala nachochinachake chochita ndi thupi lathuli. Koma izo zinali Magazikuphatikizirapo umuna, zimeneMulungu anazifungatira.

217 Iye akanakhoza kuziika izo pa chitsa ngati Iye akanafunakutero. Inde, bwana. Iye akanakhoza kuziika izo paliponsepamene Iye akanafuna kutero.

218 Koma Iye anazibweretsa izo chifukwa mkaziyo anali mukugwa. Pamenepo panadzabwera Mwana wa Mulungu wamoyowachiyero, wolengedwa, wobadwa kwa namwali, zonse thupindi moyo.

219 Nchifukwa chiyani Davide anati, “Ine sindidzawonaWoyera Wanga…kumulola Woyera Wanga Uyo kuti awonechivundi, WoyeraWanga Uyo kuti awone chivundi. Komanso InesindidzasiyamoyoWakemu gehena”?Davide ananena zimenezo.Mukuona? Zonsezo moyo, thupi, ndi mzimu, zinalengedwa ndiMulungu, mwa Iye.

220 Mkaziyo sanali amake. Iye anali mkazi. Inendikukhulupirira kuti iye anali mkazi wabwino, woyera.Mwamtheradi. Iye anali asanayambe wakhalapo chotengera.Mulungu sibwenzi atasankha chotengera chauve. Ambuyeakalola, inu ndilalikira pa zimenezo usikuuno, koma,“Chotengera chauve chakalecho ndi chiti?” Pofuna kutiamubweretse Wake, kuti amubweretse Mwana Wake ku dzikolapansi, Iye anasankha “namwali wosadziwa mwamuna.”Komanso iye sanatulutse umuna uliwonse kapena chinachirichonsecho pamene Mzimu Woyera unadzamufungatiraiye. Chifukwa, Mulungu, mu chiyero Chake, njira yakeyopandamalire, analenga mwa iye: moyo, thupi, ndi mzimu,wa Yesu Khristu. Izo nzoona. Iye anali Mwana wa Mulunguwobadwa kwa namwali.

221 Kodi zimenezo zinachita chiyani? Izo zinadzaswa chipatacha mdani. Aleluya! Psyii! Izi zikundikomera, ine. Taonani.Bwanji? Iye anaswa chipata cha mdani pomwe apo, kutimunthu aliyense wobadwa mu dziko lino mwa chilakolako chakugonana, yemwe sakanadzatha kupita Kumwamba chifukwakugonana ndi chimene chinayamba pachiyambi, mmunda waEdeni, chifukwa chimene iwo anaziphimbira okha. PameneIye anachita zimenezo, Iye anaching’amba chinthucho pawiripomwe apo, ndipo anatenga chipata cha mdani. Ndi chiyani?Potenga Mbewu Yachifumu ya Abrahamu, pa nthawi yoyambakumene, ndipo anachisasantha icho mpaka pansi. MbewuYachifumu ya chikhulupiriro ndi lonjezo, osati kutenga pakatikwa Maria, koma kwa Mulungu, anaswa zipata. Potero,anamulola munthu kuti adutse pa chipata. Ulemelero kwaMulungu!

Page 36: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

36 MAWU OLANKHULIDWA

222 Kodi Iye anachita chiyani? Atatero anatenga zipata zonseza mdani. Iye anatenga chipata cha matenda. Matenda samathakukhalapo mu Kukhalapo Kwake. Ayi, bwana. Komansochirichonse sichimakhalapo mu Kukhalapo Kwake. Mwambowa maliro sumakhalapo mu Kukhalapo Kwake. Ayi. Kodi Iyeanachita chiyani?223 Yoswa anafa. Mose anafa. Ena onse a iwo anafa, komaosati Mbewu Yachifumu iyi. Imfa siimatha kuima kumenekunali Moyo.224 Mkazi uja wochokera ku Naini, akubwera ndi mwana wake.Anaima ndipo anati, “Dzuka, mwana.”225 Mtsikana uja amene anali atafa, mwana wamkazi wa aYairo, Iye analankhula mawu mmbuyo kutali kupita ku dzikolosadziwika kunja uko, ndipo anati, “Mwanawamkazi, dzuka.”226 Lazaro, atafa masiku anai ndipo thupi lake litavunda, ndipomoyo wake unali utachoka kwa ilo, kwa masiku anai. Iye anati,“Lazaro, dzuka.” Ulemerero!227 Ndi Ameneyo apo. Kodi Iye anachita chiyani? Iye anamatulazisindikizo za chirichonse. Aleluya!228 Pamene Iye ankati afe pamenepo, Iye sakanatha kuwusungamoyo umenewo. Iye sibwenzi atafa, koma Iye amayenera kutiawupereke moyo umenewo. Ndipo pamene Iye anawuperekamoyo umenewo, Iye anafa imfa. Ndipo moyo Wake wofunikira,monga Baibulo limanenera, unatsikira ku gehena, kuti ukatengemalo anga ndi malo anu. Mbewu Yachifumu ya Abrahamu!Chiyani? Iye anali MbewuYachifumu. O, ulemelero!229 Tsopano ndife Mbewu Yachifumu, ndani, amene amakhalandi Mawu, ndendende basi monga Iye analiri. “Pakutipachiyambi panali Mawu, ndipo Mawu anali ndi Mulungu;ndipo Mawu, anasanduka thupi, ndipo anadzakhala pakatipathu.” Kodi inu simukuwona kumene kuli Mbewu Yachifumu?MbewuYachifumu ndi imeneyo imene imakhala ndiMawu.230 Inu ofooka amene mumalolera kuti muzimusisitamdierekezi, ndi mafashoni ake a chidziko. (Ine sindikulankhulandi inu pano.) Kunja uko, inu alaliki amene mukudziwakuti mumalalikira kuti masiku a zozizwitsa anapita, inumumalalikira kuti kulibeko chinthu chonga ubatizo wa MzimuWoyera, manyazi pa inu, ndipo nkumadzitcha nokha Mbewu yaAbrahamu.231 Mbewu Yachifumu imakhala ndi Mawu. Mbewu Yachifumu,osati yobadwa mwa mayi, panalibe chochita ndi mwamunakapena mkazi. Mkazi ndi mpingo; palibe kanthu kochita ndimpingo. Maria analibe kanthu kochita nayo Mbewu. Komansompingo, wotchedwa bungwe, ulibe kalikonse kochita ndiMbewu. Iyo ndi yobadwa ndi chiyani? Osati mwa bungwe, osatiMethodisti, Baptisti, Presbateria, Katolika, Lutera, zina zotero.

Page 37: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 37

232 Koma, yobadwa mwa Mbewu Yachifumu ya lonjezo laMulungu, amenewo ndi amene akutenga chipata chamdani. Ichochinatengedwa kale kwa iyeyo. “Pakuti ngati inu mukhala mwaIne, ndi Mawu Anga mwa inu, mufunse chimene inu mukufuna,icho chidzachitidwa kwa inu.” Ndi zimenezotu. Ilo ndi lonjezo.Izo zinachitika kale.233 Moyo Wake wofunikira unatsikira ku gehena, kumene inendinkayenera kuti ndipiteko. Koma pa tsiku lachitatu lija…Samson atasenza chipata cha mzindawo pa nsana wake, analibechochita chirichonse ndi icho. Iye anatenga zipata za gehena,zipata za kumanda, ndi china chirichonse. Iye sanazisenzere izowa ku phiri, koma Iye anaziwononga izo. Aleluya! Iye anatengachipata cha mdani.234 Milengalenga imene inadzaza ndi mphamvu za mdierekezi,mmwamba, mwakuti Angelo kapena kalikonseko sikamakhozakutsika. Zimalephereka kuti pakhale kukhalira pakati,chifukwa magazi a mbuzi amalephera kuti achotse tchimo.KomaMagazi Ake omwe anachotsa tchimo.235 Ndipo Iye anakwera Mmwamba, anatsogolera undende akundende. Iye anapereka mphatso kwa anthu. Tsopano, aliyensewa Mbewu ya Abrahamu amene ali wololera kuti alipiremtengo, kuti abwere pansipa ndi kudzalapa machimo awo,adzabatizidwe mu Dzina la Yesu Khristu kwa chikhululukirocha tchimo lawo, adzazazidwenso ndi Mzimu Woyera, ndikudzatha kugonjetsa mayesero.236 Ndipo pamene iwo alichotsamo dzikolo mwa inu,zinthu zimene zapita, chirichonse chimene chiri cholakwika,chirichonse chimene chikuwoneka kuti ndi cholakwika,monga akazi ndi tsitsi lawo, amuna ndi zotengeka zawo, ndimatchalitchi ndi mabungwe awo, ndi—ndi m’busa woikirakumbuyo madikoni ake, ndi—ndi zinthu za mtundu umenewo.Gulu lina la chidziko la chinachake chimzake kulowammenemo ndi kumpangitsa m’busa wosauka, kuti amutulutsemtchalitchimo.237 Pitirirani, abusa. Mulungu akudalitseni inu. Mukhale ndiMawu. Musatenge kalikonse.238 Iye anakwera Mmwamba. Kodi Iye anakachitako chiyani?Iye anakaboolako dzenje, chipata, kuti, pemphero la Mbewu iyiya Abrahamu. Bwanji? Bwanji? Ngati ife tiri Thupi la Khristu,ngati ife tifa, ife tikadzitenga tokha kuti ndife akufa ndiponkuikidwa mmanda mwa Khristu, ndi kuwuka naye Iye muchiukitsiro. Iyeyo akhala Mutu wa Thupi. Kumene kuli Mutu,Thupi limakhala nawo Iwo. Ndiyeno, mmawa uno, kumenealiyense amene anayamba wachitapo zimenezo, “akukhalalimodzi ndi Iye mmalo a mmwambamwamba,” limodzi ndiMbewu Yachifumu. Mulungu alemekezeke.

Page 38: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

38 MAWU OLANKHULIDWA

239 Kulibeko zipata. Inu simungathe kupemphera mpakaapa, ndikuti, “O, o, mawu ndi amenewo.” Huh-uh. Iwoakutsekeraniko inu, pomwe apo.240 Koma ngati mtima wathu sukutitsutsa ife; ngati ifetikudziwa kuti ife tikuyenda mmalamulo a Mulungu; ifenkumawona miyoyo yathu ikuyeretsedwa; ife nkumaziwonaizo; Mawu aliwonse amene Mulungu anawalamulira, ifenkumawasunga Iwo; tikatero zipata za mdani aliyensezitengedwa. “Ndiye mupemphe chimene inu mukufuna, ichochichitidwa kwa inu.” “Iye adzatenga chipata cha mdani wake.”O, m’bale, ungakhale mpingo wotani umenewo!241 Pamene ine nditi ndidzabwerenso ku Phoenix, ngati Ambuyeadzandiloleze ine, ine ndikuyembekeza kuti, pamene ine nditindidzalowe mu kachisi muno, kuti mipando iyi idzakhalaitazadza, ndipo mpando uliwonse wa kuyenda kwa a full Gospelmu mzinda uno udzakhala utazadza ndi oyera a Mulunguwamoyo: kumawoneka monga Mkhristu; kumalankhula mongaMkhristu; kumachita monga Akhristu; ndi Mzimu wa Mulunguukuyenda pakati pawo, kumene, ngati wina wachimwa, MzimuWoyera nkumutchula iye pomwepo.242 Iwo udzachita zimenezo. Inumwaziwonapo izo mumzere wapemphero, monga pamwamba apa pa guwa. Pamene, umati, “Inumubwerere uko ndipo mukakonze izo ndi amuna anu. Mupite,mukawawuze akazi anu kuti inu munachokapo, usiku dzanailo, ndi mkazi uyo, wakhala pa malo akuti-akutiyo.” Ngati Iwoukuchita izo pano, pakuyenda mu Mawu, pomvetsera ku Liwulaling’ono la kayeziyezi lija, Iwo ungachite zimenezo mwa inu.NdinuMbewu ya Abrahamu. Ndiye, mulibe tchimo.243 Mlaliki, kodi iwe sungakonde kuziwona izo mu mpingowako? Kuyenda mu mpingo uwu, ndi kuyang’ana pansiukamadutsa apa, kuwawona onse amuna ndi akazi, aumulungu,oyera, atakhala pamenepo atadzazidwa ndi mphamvu yaMulungu. Tchimo silingathe kulowamo. Munthu akalowamo ndikukhala pansi, Mzimu nkuwuka ndi kuti, “John Jones, iweukuchokera kwakuti-ndi-kwakuti, mzinda wake, malo akuti-akuti. Iye ali pano kuti adzapeze machiritso a thupi lake.Mukuona? Iye anachita chinthu chakuti pa malo akuti. Iyeanachita ichi. Iye ayenera kuti akabweze ichi, ndipo akakonzeichi, akatero Mulungu amuchiza iye khansa imeneyo. PAKUTIATERO AMBUYE.” Mai, mai!244 Mundipatse ine mpingo, mundipatse ine amuna khumi,amene, ali ngale zenizeni za Mulungu, Mbewu Yachifumu,muwaike amuna amenewo pamodzi, ndipo muwone chimenechingachitike. Mundipatse ine nyumba yozadza ndi anthumonga amenewo, ndipo ine ndikusonyezani inu Kuwala kumenedziko lingakuthamangireko. Ndiko kulondola. Ndi chimeneMulungu akufuna kuti ife tikhale. “Ndinu mzinda utakhala pa

Page 39: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 39

phiri.” Ndinu Mbewu Yachifumu ya Abrahamu. “Iyo idzatengachipata cha mdani wake.”245 Matenda, chiripo choyambitsa matenda. Chiripochoyambitsa zinthu izi. Ndipo Mulungu, Mzimu Woyera, ulipano kuti uwulule chinthu chimenecho ndi kudzakuuzani inuchifukwa chimene inu simukulandirira izo. Vuto ndi chiyani ndiife? Ife sitikusowa kuti tizidabwa, “Kodi Iwo uchita izo.” Iwoukuchita kale zimenezo. Kodi inumumachita chiyani?246 Tamuwonani mneneri uja. Iye sanamvetsere kwa mkokomowamphepo, “Ulemelero kwaMulungu! Aleluya!”247 Zimenezo ndi zabwino. Tsopano, kumbukirani, ine sikutindikutsutsa zimenezo. Ine ndikuyembekeza aliyense akumvetsazimenezo. Winawake anati, “M’bale Branham samakhulupiriramu kunena, ‘Ulemelero kwa Mulungu! Aleluya!’” Chabwino,tandiyang’anani ine pano tsopano. Ine ndimakhulupirira mukufuula, kulankhula ndimalirime, kuvinamuMzimu.248 Koma, m’bale, pamene inu mulephera kuti mumvetsereLiwu laling’ono la kayeziyezi lija la Mawu, chinthu chake ndichimenecho chimene chimakutengani inu. Chinthu chake ndichimenecho.249 Eliya amadziwa kuti chitsitsimutso chonsechi chikuchitikakunjako. Koma iye anali…Icho sichinamukope iye kunja uko.Koma pamene iye anamvetsera Liwu laling’ono la kayeziyezi lijala Mulungu, pamenepo iye anakopedwa. Ndipo iye anaphimbankhope yake, natulukira panja. Bwanji? Eliya anali Mbewu yaAbrahamu, amatsatira Mawu.250 “Ngati inu mukhala mwa Ine ndipo Mawu Anga nkukhalamwa inu, ndiye mupemphe zimene inu mukufuna, izozidzachitidwa kwa inu.”

Tiyeni tiweramitse mitu yathu mphindi chabe kwapemphero.251 O, mpingo, momwe, pamene ine ndatsiriza kulalikira mongachonchi, momwe ine ndimamverera! Mzimu umandichokeraine, ndipo ine ndimayang’ana mmbuyo. Ine ndimawawonaanthu amene ndithudi amachita kupisa mthumba mwawo ndikutenga chakudya kuchokera kwa ana awo, kuti achiperekeicho kwa ine. Ine ndimawawona akazi achichepere muno,mwinamwake okhala ndi tsitsi lalifupi. Kodi iwo angachitechiyani? Iwo akhoza kundichitira ine chirichonse mu dziko,chimene iwo angathe. Bambo kumakhala ndi mkazake mongachoncho, ndipo ine basi kungomudula iye mzidutswa, ndiMawu amenewo, kumupweteketsa iye, chikumbumtima chakekugwera pansi. Ndipo komabe bambo ameneyo amapitauko ndi kukavutikira, ndi kunditumizira ine chakhumichake. Kulondola. Zimenezo zimandipangitsa ine kumverera,mukuona, pamenepo ndiye kuti ndabwereranso ku thupi,

Page 40: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

40 MAWU OLANKHULIDWA

inu mukuona, chiyani, kodi ine ndinanena chiyani? Inesindimatanthauza kuti ndikupweteketseni. Si zimenezo ayi.252 Koma, o, m’bale, ndi mlongo wanga wamng’ono ndim’bale wokondedwa, ngati amenewo ali Mawu a Mulungu,ndipo uwu ndikukhala Mzimu Wake umene ukuwapangitsaMawu amenewo kuti abwere ku moyo, kwa inu, kodizidzakhala bwanji pa Tsiku la Chiweruzo? Ine ndikuyeserakuti ndikukonzeketsereni inu tsiku limenelo. Chonde, chondemungotenga Mawu Ake. Ngati ine ndidzalalikire chirichonsechimene sichiri Mawu, lonjezo la Mulungu, ndiye inu muli nawoufulu kuti mudzabwere kwa ine. Koma amenewo ndi Mawu.Ndipo zimenezo ndi chifukwa chakuti ine ndimakukondani inu.253 Si chifukwa chakuti i—ine sindikukufunani inu mungalawayo. Ndi chifukwa chakuti ngalawayo sikakufikitsaniinu. Inumuchita ngozi, limodzi la masiku amenewa.254 Inu mudzayenera kuti mudzafike pa Chiweruzo.“Kuchimwira chaching’ono ndi kuchimwira chonsecho.” Ndipopamene inu mukudziwa kuchita chabwino, nkukhala kutindi Mawu a Mulungu ndiponso ndi lonjezo kuti muchitechimenecho, ndiye inu nkusachichita icho, ndiye nangabwanji zimenezo? Inu mudzafunsidwa kuti mupereke chifukwachake, ndiye mudzatani? Pamene Uthenga uwu mmawa unoudzakomanizane nanu inu kutsidya pa kanema, pa Tsiku laChiweruzo, nanga bwanji pamenepo? Taganizani za zimenezo,abwenzi. Inu mukhoza kufa tsiku lisanathe. Tonse a ife tikhoza.Ndipo chinthu chimodzi chotsimikizika, inumudzafa.255 Ine ndinaima tsiku lina ndikuwayang’ana amayianga, ine nditawagwirizira iwo mmanja mwanga. Inendinawagwirizira adadi pang’ono zisanachitike zimenezo, ndipondinawapenyerera iwo akupita.256 Ine ndawawonapo iwo akufika kumathero a msewu, ameneankaganiza kuti anali abwino kwenikweni. Mukuti, “O, M’baleBranham, o, ngati ine ndingakhale kanthawi pang’ono chabe!”Zidzakhala mutachedwa pamenepo. Ndipo kumbukirani, imfasiimasintha moyo. Iyo imangosintha malo okhalako. Ndipongati inu mukuwona zimenezo, chinachake mkati mwanu.Mukhale oganiza bwino tsopano. Ngati inu mukuwona kuti,chinachake mkati mwanu chikukupangitsani inu kumachitamwanjira imeneyo ndi kumamverera mwanjira imeneyo, mongamomwe inu simuyenera kuti muzimverera, mulape mmawa uno,mutero inu, mzanga? Bwerani. Mukhale…Inu simukusowa kutimuzikhala mwanjira imeneyo. Ndinumunthu womvetsa chisoni.Muzikhala moyo woona wa Mbewu Yachifumu. Mulunguakukufunani inu lero.257 Kodi inu mungakweze dzanja lanu, pamene mwaweramitsamutu wanu, ndi mtima. Ndikuti, “M’bale Branham, inendikukwezera dzanja langa kwa Mulungu. Moona mtima,

Page 41: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 41

kuchokera mu mtima mwanga, ndicho chimene ine ndikufunakuti ndikhale. Ndicho kwenikweni chimene ine ndikufuna kutindikhale. Ine nda—ndaziipitsa kuno ndi china chirichonse,koma kwenikweni i—ine sindikufuna kuti ndikhale mongachoncho. Ine ndikufuna kuti ndikhale chimene inu mwakhalamukulankhula mmawa uno. Mundipempherere ine, M’baleBranham. Ine ndikukwezera manja anga kwa Mulungu, osatikwa inu,M’bale Branham, koma kwaMulungu. Ndipomumtimamwanga, Iye akuwudziwa mtima wanga. Ine ndikufunitsitsakuti ndikhale Mkhristu yemwe inu mukumukambayo, Mbewuyachifumu ya Abrahamu, kudzera mwa Yesu Khristu.” Kwezanidzanja lanu tsopano ndipo munene kuti, “Ine nditero…Mundipempherere ine, M’bale Branham.” Mulungu akudalitseniinu. Mulungu akudalitseni inu. Ndithudi Iye akuchitirani inuzimenezo.258 Atate athu Akumwamba, mu Kuwala kwa Mawu Anu, mumphamvu ya chiukitsiro Chanu! Ndipo ine ndikuzindikira,Ambuye, kuti anthu osauka nthawi zambiri amapotozedwakuno, chifukwa cha zosokonezeka. Anthuwo samadziwankomwe kuti achite chiyani; wina akabwera, anena chinthuchina; ndipo wina akabwera, anena china.259 Ndipo kuno ku Phoenix, mzinda wawukulu uwu wa—wa,wabwino, ozawona malo, kumene chirichonse chochokera kumafukowo chimadzakochezako mmenemo, zonse ziwiri zathupindi zauzimu. Nditaima pa phiri, tsiku lina, ndipo ndimaganizandi nthawi zingati zimene Dzina la Mulungu limagwiritsidwantchito pachabe pa tsiku kuno, ndi zigololo zingati zimenezimachitidwa, ndi tchimo lochuluka bwanji ndi uve mmisewukuno, ndi mnyumba za mowa ndi anthu oswela ku mowa, ndichirichonse, ambiri a iwo kumadzinenera kuti ndi okhulupirira,Mkhristu!260 Akazi kumapita mu msewu, ali ndi ndudu mmanja mwawo.Akumayenda atavala zovala zopanda makhalidwe, pamene Inumunati izo zimakununkhirani Inu, “Izo ndi chonyansa,” ngatichimbudzi chakale, chauve, chautchisi, chonunkha penapake.O Mulungu, angathe bwanji mkazi amene amadzinenera kutiali nawo Mzimu Woyera kumachita chinthu monga chimenecho,ndipo nkumadziwa kuti m’mphuno za Mpulumutsi, zimenezoziri ndi fungo monga choncho, kununkha? Iye angathe bwanjikudzakhala ndi chinthu ngati chimenecho mu Ufumu Wake?Atate, ngati iwo akanangodziwa, iwo ali mamailosi millionikwa Iwo.261 Ine ndikupemphera, Mulungu, tichitireni chifundo. Palibeamene angafune kuti adzapite ku madera awo a otaika. Palibeamene akufuna kuti adzapite kumeneko, Atate. Izo zikhalekutali kuti aliyense wa ife tingadzapiteko. Komabe pansipamenepo muli mtima wabwino mwa munthu ameneyo, bambouyo, mayi uyo, mwamuna kapena mkazi amene ali wachikondi

Page 42: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

42 MAWU OLANKHULIDWA

ndi wabwino ndi wachifundo, ndipo wangonyengedwa ndimdierekezi. Mdierekezi wachita zimenezo.262 Satana, ine ndikukutsutsa iwe, chifukwa ndiwe mdaniwa Ambuye wanga. Ndiwe mdani wa Mawu Ake. Ndipo inendikukulamulira iwe, mwa Yesu Khristu, Mwana wa Mulungu,ngati munthu wachivundi, pozindikira kuti ndiribe mphamvumwa inemwini. Ine ndiribe mphamvu yokuletsera iwe. Inendiribe mphamvu yowapangitsira aliyense wa akazi awa kutiazikonze, aliyense wa amuna awa, amene akumvetsera ku tepiiyi, ka—kapena kulikonseko. Ine ndiribe njira yowapangitsaiwo kuti aziyeretse. Ndine wopanda mphamvu. Koma ine ndirinawo ulamuliro wa Mawu a Mulungu, ngati wantchito, kutindiwalalikire Izi, ndipo ndine wokakamizidwira ku ulamuliroumenewo. Ngakhalenso wa polisi uyu kuno alibe mphamvuzoimitsira galimoto, koma iye ali nawo ulamulirowochitira izo.263 Ndipo, Satana, iwe ukhoza kumapita kukaliza mabulekiako, chifukwa ine ndikukulamulira iwe, mwa Yesu Khristu,kuti iwe uwamasule anthu awa, kudutsa pa dziko lonse,kulikonse kumene Uthenga uwu ungapiteko. Uwamasule iwo.Ine ndikuwatenga iwo, kuti iwo anagulidwa. Iwo si a iwo okha.Iwo anagulidwa ndi mtengo, Mbewu Yachifumu ya Abrahamu,Ambuye Yesu.264 Iwe ndi wachinyengo wauve, wautchisi, wonunkha,wonyengeza anthu, ukuwatsogolera iwo mwakhungu mpakaku maenje a gehena, amasule iwo. Ine ndikukulamuliraiwe, mwa Mulungu wamoyo, mwa Nsembe ya MwanaWake, Yesu, kuti iwe uwamasule iwo, kuti miyoyo yawoikafulumizitsidwe ndi mdalitso Wake ndi Kukhalapo Kwake,kuti iwo akakhoze kutenga chipata cha mdani aliyense. [Maloosajambulidwa pa tepi—Mkonzi.] Iwe wawadikiritsa iwo ichi,icho, kapena chinacho, kapena kukhudza kwina koyera, kapenachinachakenso, koma ine ndikuti iwe usiya kugwira kwako.265 Kodi matenda angathe bwanji kuima mu kudzoza ngatiuku? Pokhapo pamene iwo akukana kuti ayang’ane kutsidyapa lonjezo monga atate Abrahamu anachitira, pamene iyeamakhoza kumuwona Iye mchiwerengero cha zaka mazanakutali, akubwera.266 Amasule iwo. Mu Dzina la Yesu Khristu, uwasiye anthuamenewo azipita.267 Itateromphamvu yaMulungu, kumvetsa kwaMawu, pameneiwo akutsukidwa mmawa uno ndi Iwo, mutalola kumvetsakwa kusunga Mawu a Mulungu ndi malonjezo Ake moona,kugwire mwakuti zizilephereka kuswedwa ndi Satana. Mulolewina aliyense agwire lonjezo limenelo, ndikuti, “Ndi Ili limenelo.Ine ndagwiritsitsa kwa Ilo. Mulungu anapanga lonjezo. Ndinembewu ya Abrahamu. Ine ndingathe bwanji kukaikira lonjezo

Page 43: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPO MBEWU YAKO IDZATENGA CHIPATA CHA MDANI WAKE 43

Lake?” Ndi kumapita chitsogolo, kudzera mwa Yesu Khristu,Ambuye wathu. Ameni.

Ndimkonda Iye…268 Zakhala zodula mmawa uno, abwenzi. Tiyeni tipembedzetsopano mokoma.

Pakuti Iye anayamba kundikonda ineAnandigulira chipulumutso changaPa mtengo wa Kalvare.

269 Kodi zingakhale zotheka, osati mosinjirira, ndithudi ayi…Izi ndi—ndi zachipembedzo. Tiyeni tikwezere manja athu kwaIye amene timamukonda. Ndikuti:

Ndimkonda Iye, ndimkonda IyePakuti Iye anayamba kundikonda ineAnandigulira chipulumutso changaPa mtengo wa Kalvare.

270 Tsopano, kwa mkazi aliyense kapena mtsikana muno, ilindi dzanja langa. Mulungu amakukondani inu. Kwa mwamunaaliyense kapena mnyamata muno, Mulungu amakukondani inu.Ine ndimakukondani inu. Tsopano, ine sindingathe kufikira ndikukugwira lirilonse la manja anu, koma Mulungu afotokozekwa inu chimene ine ndikutanthauza. Pamene ife tikuimbaimeneyo kachiwiri, mungotembenuka ndi kugwirana chanza ndiwinawake. “Ndi ichi anthu onse adziwa kuti ndinu akuphunziraAnga, pamene inu mukhala ndi chikondi, kwa wina ndimzake.” Ine…

Anagula chipulumutso changaPa mtengo wa Kalvare.Ndimkonda Iye, ndimkonda IyePakuti Iye anayamba kundikonda ineAnandigulira chipulumutso changaPa mtengo wa Kalvare.

271 Kodi inu simukumukonda Iye? [Osonkhana akuti,“Ameni.”—Mkonzi.] Kumverera kokoma kuja kwa MzimuWoyera! Mawu ndi kuchita koyeretsa, amangokukhulani inu,amakupangani inu cholengedwa chatsopano, amachotseratuzonse. Mawu ndi akuthwa kuposa lupanga lakuthwakonsekonse, kuchita mdulidwe, kudulapo zinthu zonse zamdziko. Mukuona? Zikatero ife timamverera kuti tayera,timakhala titakhulidwa, kumuvomereza ndi kumukhulupiriraIye. Ndi momwe ife tingathe kuimbira:

Ndimkonda Iye, ndimkonda IyePakuti Iye anayamba kundikonda ineAnandigulira chipulumutso changaPa mtengo wa Kalvare.

272 Ndi zokongola zimenezo? [Osonkhana akuti,“Ameni.”—Mkonzi.] Ine ndimangozikonda izo ndi mtima wanga

Page 44: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

44 MAWU OLANKHULIDWA

wonse. Mukuona? Tiyeni tiiyeserenso iyo kachiwiri, aliyensetsopano, kwenikweni, mokwezamawu anu tsopano.

Ndimkonda Iye, ndimkonda IyePakuti Iye anayamba kundikonda ineAnandigulira chipulumutso changaPa mtengo wa Kalvare.

Page 45: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

NDIPOMBEWUYAKO IDZATENGACHIPATACHA MDANI WAKE CHA62-0121M(And Thy Seed Shall Possess The Gate Of His Enemy)

Uthenga uwu wa M’bale William Marrion Branham, woperekedwa muChingerezi Lamlungu mmawa, Januwale 21, 1962, ku Faith Tabernacle muPhoenix, Arizona, U.S.A., unatengedwa kuchokera pa matepi ojambulidwa ndimaginito nudindidwa mosachotsera mawu ena mu Chingerezi. Kumasulira kwaChichewa uku kunadindidwa ndi kugawidwa ndi Voice Of God Recordings.

CHICHEWA

©2015 VGR, ALL RIGHTS RESERVED

VOICE OF GOD RECORDINGS, MALAWI OFFICE

P.O. BOX 51453, LIMBE, MALAWI

VOICE OF GOD RECORDINGS

P.O. BOX 950, JEFFERSONVILLE, INDIANA 47131 U.S.A.www.branham.org

Page 46: CHA62-0121M Ndipo Mbewu Yako Idzatenga Chipata Cha Mdani …download.branham.org/pdf/CHA/CHA62-0121M And Thy Seed... · 2018. 5. 23. · 2 MAWUOLANKHULIDWA 5 Ko—koteroife,nthawizambiri,polalikira,inendimakhala

Chidziwitso kwa ofuna kusindikiza

Maufulu onse ndi osungidwa. Bukhu ili mukhoza ku printa kunyumba kwanu ngati mutafuna kuti mugwiritse ntchito inuyo kapena kuti mukawapatse ena, ulere, ngati chida chofalitsira Uthenga wa Yesu Khristu. Bukhu ili simungathe kuligulitsa, kulichulukitsa kuti akhalepo ambiri, kuikidwa pa intaneti, kukaliika pakuti ena azitengapo, kumasuliridwa mu zinenero zina, kapena kugwiritsidwa ntchito ngati njira yopezera ndalama popanda chilolezo chochita kulembedwa ndi a Voice Of God Recordings®.

Ngati mukufuna kuti mumve zambiri kapena ngati mukufuna zipangizo zina zimene tiri nazo, chonde mulembere ku:

Voice of God RecoRdinGsP.o. Box 950, JeffeRsonVille, indiana 47131 U.s.a.

www.branham.org